< Salmos 126 >

1 Cuando el Señor hizo un cambio en el destino de Sión, éramos como hombres en un sueño.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati amene akulota.
2 Entonces nuestras bocas se llenaron de risa, y nuestras lenguas dieron un alegre clamor; dijeron entre las naciones: Jehová hizo grandes cosas por ellos.
Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka; malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe. Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti, “Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”
3 El Señor hizo grandes cosas por nosotros; por lo cual estamos contentos.
Yehova watichitira zinthu zazikulu, ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.
4 Deja que nuestro destino sea cambiado, Señor, como las corrientes en el sur.
Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova, monga mitsinje ya ku Negevi.
5 Los que sembraron con llanto, cosecharan en el grano con gritos de alegría.
Iwo amene amafesa akulira, adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.
6 Aunque un hombre salga llorando, llevando consigo su bolsa de semilla; él vendrá de nuevo en alegría, con los tallos de grano en sus brazos.
Iye amene amayendayenda nalira, atanyamula mbewu yokafesa, adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe, atanyamula mitolo yake.

< Salmos 126 >