< Éxodo 36 >
1 Dejen que Bezaleel y Aholiab se pongan a trabajar, con todo hombre de corazón sabio a quien el Señor ha dado sabiduría y conocimiento, para hacer lo que sea necesario para ordenar el lugar santo, tal como el Señor ha dado órdenes.
Choncho Bezaleli, Oholiabu pamodzi ndi anthu aluso onse amene Yehova anawapatsa luso ndi nzeru zodziwira kupanga zofunika zonse zomangira malo opatulika, adzapanga zonse iwowo, monga momwe Yehova analamulira.”
2 Entonces Moisés envió a buscar a Bezaleel y a Aholiab, y a todos los hombres de corazón sabio a quienes el Señor había dado sabiduría, incluso a todos los que se sintieron movidos por el impulso de su corazón a venir y tomar parte en la obra:
Ndipo Mose anayitana Bezaleli ndi Oholiabu ndiponso munthu aliyense waluso amene Yehova anamupatsa luso ndiponso amene anali ndi mtima wofuna kugwira ntchito.
3 Y tomaron de Moisés todas las ofrendas que los hijos de Israel habían dado para la edificación del lugar santo. Y aún así continuaron dándole más ofrendas gratuitas todas las mañanas.
Iwo analandira kuchokera kwa Mose zopereka zonse Aisraeli anabweretsa kuti agwirire ntchito yomanga malo wopatulika. Ndipo anthu anapitirira kupereka zopereka zaufulu mmawa uliwonse.
4 Entonces los sabios, que estaban haciendo todo el trabajo del lugar santo, vinieron de su trabajo;
Kotero amisiri onse amene amagwira ntchito yonse ya malo wopatulika anasiya ntchitoyo
5 Y dijo a Moisés: La gente está dando mucho más de lo que se necesita para la obra que el Señor nos ha dado que debemos hacer.
ndipo anati kwa Mose, “Anthu akubweretsa kuposa zimene zikufunika kugwirira ntchito imene Yehova analamulira kuti ichitike.”
6 Entonces Moisés hizo un mandamiento y lo repartió entre todas las tiendas, diciendo: Ninguno de los hombres ofrezca más ofrendas por el lugar santo. Entonces se evitó que la gente diera más.
Choncho Mose analamulira ndipo analengeza mu msasa onse, “Mwamuna kapena mayi aliyense asaperekenso chopereka chilichonse cha ku malo wopatulika.” Choncho anthu analetsedwa kubweretsa zambiri,
7 Porque el material que tenían era suficiente y más que suficiente para todo el trabajo que había que hacer.
chifukwa zimene anali nazo zinali zoposera zimene zimafunika kugwirira ntchito yonse.
8 Entonces todos los obreros expertos entre ellos hicieron la Casa con sus diez cortinas; del mejor lino, azul y morado y rojo, los hicieron, con querubines bordados por diseñadores expertos.
Anthu onse aluso pakati pa anthu ogwira ntchitoyo anapanga chihema pogwiritsa ntchito nsalu khumi zofewa, zosalala ndi zolukidwa bwino, zobiriwira, zapepo ndi zofiira. Ndipo anthu aluso anapeta pa nsaluzo Akerubi.
9 Cada cortina tenía veintiocho codos de largo y cuatro codos de ancho, todos de la misma medida.
Nsalu zonse zinali zofanana. Mulitali mwake zinali mamita khumi ndi atatu, mulifupi mamita awiri.
10 Y se unieron cinco cortinas, y las otras cinco cortinas se unieron entre sí.
Iwo analumikiza nsalu zisanu, kuti ikhale nsalu imodzi ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsalu zisanu zinazo.
11 Y pusieron ojales azules en el borde de la cortina exterior del primer grupo, y de la misma manera en la cortina exterior del segundo grupo.
Kenaka anapanga zokolowekamo za nsalu yobiriwira mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsiriza ya mbali ina. Ndipo anachita chimodzimodzi ndi nsalu yotsiriza ya mbali inayo.
12 Cincuenta ojales en una cortina y cincuenta en el borde de la cortina del otro grupo; los ojales son opuestos el uno al otro.
Iwo anasokerera zokolowekamo makumi asanu pa nsalu yoyamba ndi zokolowekamo makumi asanu zinanso pa nsalu inayo. Anapanga kuti zokolowekamozo ziziyangʼanana.
13 E hicieron cincuenta ganchos de oro, uniendo las cortinas, una a la otra, con los ganchos; y así la tienda formaba un todo.
Kenaka anapanga ngowe zagolide 50 zolumikizira nsalu ziwirizo kotero kuti zinapanga chihema chimodzi.
14 E hicieron cortinas de pelo de cabras para la tienda; once cortinas fueron hechas.
Iwo anapanga nsalu za ubweya wambuzi zophimba pamwamba pa chihemacho. Nsalu zonse pamodzi zinalipo khumi ndi imodzi.
15 Cada cortina tenía treinta codos de largo y cuatro codos de ancho, todos de la misma medida.
Nsalu zonse khumi ndi imodzi zinali zofanana. Mulitali mwake munali mamita khumi ndi anayi ndipo mulifupi mwake munali mamita awiri.
16 Cinco cortinas se unieron para formar un grupo, y seis cortinas se unieron para formar el otro grupo.
Iwo analumikiza nsalu zisanu kukhala nsalu imodzi ndipo nsalu zinazo zisanu ndi imodzi, analumikizanso kukhala nsalu imodzinso.
17 Y pusieron cincuenta ojales de cuerda en el borde de la cortina exterior del primer grupo, y cincuenta ojales en el borde de la cortina exterior del segundo grupo,
Kenaka anasokerera zokolowekamo makumi asanu mʼmphepete mwa nsalu imodzi yotsirizira ya nsalu yoyamba yolumikiza ija ndiponso anapanga zokolowekamo zina makumi asanu mʼmphepete mwa nsalu yotsirizira ya nsalu inanso yolumikiza ija.
18 Y cincuenta ganchos de bronce para unirlos para hacer la tienda.
Iwo anapanga ngowe 50 zamkuwa zolowetsa mu zokolowekazo ndipo anaphatikiza nsalu ziwirizo kuti tentiyo ikhale imodzi.
19 Y hicieron una cubierta de pieles de oveja de color rojo, para pasar la tienda, y una cubierta de cuero que fuera sobre encima.
Ndipo anapanga chikopa cha nkhosa zazimuna cha utoto wofiira chophimbira tentiyo ndipo pamwamba pake anapanganso chophimbira china cha zikopa za akatumbu.
20 Y para los montantes de la casa hicieron tableros de madera de acacia.
Iwo anapanga maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho.
21 Las tablas tenían diez codos de largo y un codo y medio de ancho.
Feremu iliyonse inali yotalika mamita anayi ndipo mulifupi mwake munali masentimita 69.
22 Cada tabla tenía dos espigas fijadas en ella, para unirlas una con la otra; todas las tablas se hicieron de esta manera.
Thabwa lililonse linali ndi zolumikizira ziwiri. Iwo anapanga maferemu onse a chihemacho ndi matabwa otere.
23 Hicieron veinte tablas para el lado sur del santuario:
Anapanga maferemu makumi awiri a mbali yakummwera kwa chihemacho,
24 Y para estas veinte tablas, cuarenta basas de plata, dos basas debajo de cada tabla, para tomar sus espigas.
ndiponso anapanga matsinde 40 asiliva ndipo anawayika pansi pa maferemuwo. Pansi pa feremu iliyonse anayika matsinde awiri ogwiriziza zolumikizira ziwiri zija.
25 Y para el segundo lado de la casa, en el norte, hicieron veinte tablas,
Iwo anapanganso maferemu makumi awiri a mbali yakumpoto ya chihemacho,
26 Con sus cuarenta bases de plata, dos basas para cada tabla.
ndiponso matsinde makumi anayi asiliva, awiri pansi pa feremu iliyonse.
27 Y para el lado oeste de la casa, en la parte posterior, hicieron seis tablas,
Anapanganso maferemu asanu ndi imodzi a kumbuyo kwa tenti, kumbali yakumadzulo,
28 Y dos tablas para los ángulos en la parte posterior.
ndiponso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti.
29 Estos se unieron en la base y en la parte superior a un anillo, formando así los dos ángulos.
Pa ngodya ziwirizi panali maferemu awiri, kuyambira pansi mpaka pamwamba atalumikizidwa pa ngowe imodzi. Maferemu onse anali ofanana.
30 Así que había ocho tablas con dieciséis basas de plata; dos basas debajo de cada tabla.
Choncho panali maferemu asanu ndi atatu ndiponso matsinde 16 asiliva, awiri anali pansi pa feremu iliyonse.
31 E hicieron barras de madera dura; cinco para las tablas en un lado de la casa,
Iwo anapanganso mitanda ya matabwa amtengo wa mkesha. Mitanda isanu inali ya maferemu a mbali imodzi ya chihema,
32 Y cinco para las tablas en el otro lado del santuario, y cinco para las tablas en la parte posterior, en el oeste.
mitanda isanu inanso inali ya maferemu a mbali inayo ndipo mitanda ina isanu ya mbali yakumadzulo, kumapeto kwenikweni kwa chihema.
33 La barra del medio estaba hecha para atravesar los anillos de todas las tablas de un extremo al otro.
Anapanga mtanda wapakati omwe umachokera pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.
34 Todas las tablas estaban chapadas de oro, y los anillos por donde pasaban las varillas eran de oro, y las varillas estaban chapadas de oro.
Iwo anakuta maferemuwo ndi golide ndiponso anapanga mphete zagolide zogwiriziza mitandayo. Ndipo mitandayonso anayikuta ndi golide.
35 Y él hizo el velo del mejor lino, azul, púrpura y rojo, trabajado con querubines bordados, diseñadas por obreros expertos.
Anapanga nsalu yokhala ndi mtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira ndipo nsaluyo inali yolukidwa bwino, yofewa ndi yosalala. Ndipo anthu aluso anapetapo zithunzi za Akerubi.
36 Y le hicieron cuatro columnas de madera dura cubierta de oro: tenían ganchos de oro y cuatro basas de plata.
Iwo anapanga nsanamira zinayi zamtengo wa mkesha zokutidwa ndi golide. Anapanganso ngowe zagolide za nsanamirazo ndi matsinde asiliva anayi.
37 E hicieron una cortina para la puerta del tabernáculo, del mejor lino con bordados de azul, púrpura y rojo;
Anapanga nsalu ya pa chipata cholowera mu chihema, yamtundu wamtambo, wapepo ndi ofiira yomwe inali yofewa ndi yosalala, yopetedwa bwino ndi amisiri aluso.
38 Y cinco columnas para la cortina, con sus ganchos; las cabezas de las columnas eran de oro y estaban rodeadas con anillos de oro; y sus cinco basas eran de bronce.
Anapanga nsanamira zisanu ndi ngowe zake. Anakuta pamwamba pa nsanamirazo ndi zomangira zake ndi golide, ndipo anapanganso matsinde asanu amkuwa.