< Salmos 120 >

1 En mi angustia clamé a Yavé, Y Él me respondió.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Oh Yavé, libra mi vida de labios mentirosos, De una lengua engañadora.
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 ¿Qué se te dará, O qué más se te hará, Oh lengua engañosa?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Agudas flechas de guerrero, [Forjadas] con brasas de enebro.
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 ¡Ay de mí, porque vivo desterrado en Mesec, Y habito entre las tiendas de Cedar!
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Mucho tiempo estuvo mi alma Con los que aborrecen la paz.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Yo soy pacífico, pero cuando hablo, Ellos me declaran la guerra.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.

< Salmos 120 >