< Salmos 150 >

1 ¡Alabado sea Yah! ¡Alabado sea Dios en su santuario! ¡Alábenlo en sus cielos por sus actos de poder!
Tamandani Yehova. Tamandani Mulungu mʼmalo ake opatulika; mutamandeni ku thambo lake lamphamvu.
2 ¡Alabadle por sus poderosos actos! ¡Alábenlo según su excelente grandeza!
Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake amphamvu; mutamandeni chifukwa cha ukulu wake wopambana.
3 ¡Alabadle con el sonido de la trompeta! Alábenlo con el arpa y la lira.
Mutamandeni poyimba malipenga, mutamandeni ndi pangwe ndi zeze.
4 ¡Alabadle con panderetas y bailes! Alábenlo con instrumentos de cuerda y flauta.
Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina, mutamandeni ndi zingwe ndi zitoliro.
5 ¡Alabadle con fuertes címbalos! ¡Alábenlo con címbalos resonantes!
Mutamandeni ndi ziwaya zolira za malipenga, mutamandeni ndi ziwaya zolira kwambiri.
6 ¡Quetodo lo que tiene aliento alabe a Yah! ¡Alabado sea Yah!
Chamoyo chilichonse chopuma chitamande Yehova. Tamandani Yehova.

< Salmos 150 >