< Génesis 5 >

1 Este es el libro de los descendientes de Adán. El día en que Dios creó a Adán, lo hizo a imagen de Dios.
Ndondomeko ya mibado ya Adamu ndi iyi: Pamene Mulungu analenga munthu, anamulenga mʼchifaniziro cha Mulungu.
2 Los creó varón y mujer y los bendijo: y los llamó “hombre” en el día de su creación.
Iye analenga mwamuna ndi mkazi. Anawadalitsa ndipo anawatcha “Munthu.”
3 Tenía Adán ciento treinta años cuando engendró un hijo a su semejanza, según su imagen, al cual puso por nombre Set.
Pamene Adamu anali ndi zaka 130, anabereka mwana wamwamuna wofanana naye ndipo anamutcha Seti.
4 Fueron los días de Adán, después de engendrar a Set, ochocientos años, y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Seti, Adamu anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
5 Y fueron todos los días que vivió Adán novecientos treinta años, y murió.
Zaka zonse za Adamu zinali 930 ndipo anamwalira.
6 Set tenía ciento cinco años cuando engendró a Enós.
Pamene Seti anali ndi zaka 105, anabereka Enosi.
7 Y vivió Set, después de engendrar a Enós, ochocientos siete años, y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Enosi, Seti anakhala ndi moyo zaka zina 807 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
8 Y fueron todos los días de Set novecientos doce años, y murió.
Zaka zonse za Seti zinali 912 ndipo anamwalira.
9 Enós tenía noventa años cuando engendró a Cainán.
Pamene Enosi anali ndi zaka 90, anabereka Kenani.
10 Vivió Enós, después de engendrar a Cainán, ochocientos quince años, y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Kenani, Enosi anakhala ndi moyo zaka zina 815 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
11 Y fueron todos los días de Enós novecientos cinco años, y murió.
Zaka zonse za Enosi pamodzi zinali 905 ndipo anamwalira.
12 Cainán tenía setenta años cuando engendró a Mahalalel.
Pamene Kenani anali ndi zaka 70, anabereka Mahalaleli.
13 Vivió Cainán, después de haber engendrado a Mahalalel, ochocientos cuarenta años, y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Mahalaleli, Kenani anakhala ndi moyo zaka zina 840 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
14 Y fueron todos los días de Cainán novecientos diez años, y murió.
Zaka zonse za Kenani zinali 910, ndipo anamwalira.
15 Mahalalel tenía sesenta y cinco años, cuando engendró a Yared.
Pamene Mahalaleli anali ndi zaka 65, anabereka Yaredi.
16 Vivió Mahalalel, después de engendrar a Yared, ochocientos treinta años, y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Yaredi, Mahalaleli anakhala ndi moyo zaka zina 830 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
17 Y fueron todos los días de Mahalalel ochocientos noventa y cinco años, y murió.
Zaka zonse za Mahalaleli zinali 895 ndipo anamwalira.
18 Yared tenía ciento sesenta y dos años cuando engendró a Enoc.
Pamene Yaredi anali ndi zaka 162, anabereka Enoki.
19 Vivió Yared, después de engendrar a Enoc, ochocientos años y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Enoki, Yaredi anakhala ndi moyo zaka zina 800 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
20 Y fueron todos los días de Yared novecientos sesenta y dos años, y murió.
Zaka zonse za Yaredi zinali 962 ndipo anamwalira.
21 Enoc tenía sesenta y cinco años cuando engendró a Matusalén.
Pamene Enoki anali ndi zaka 65, anabereka Metusela.
22 Anduvo Enoc con Dios, (viviendo) después de engendrar a Matusalén, trescientos años, y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Metusela, Enoki anayenda ndi Mulungu zaka 300 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
23 Y fueron todos los días de Enoc trescientos sesenta y cinco años.
Zaka zonse za Enoki zinali 365.
24 Enoc anduvo con Dios, y desapareció porque Dios se lo llevó.
Enoki anayenda ndi Mulungu; ndipo iye sanaonekenso chifukwa Mulungu anamutenga.
25 Matusalén tenía ciento ochenta y siete años cuando engendró a Lamec.
Pamene Metusela anali ndi zaka 187, anabereka Lameki.
26 Vivió Matusalén, después de engendrar a Lamec, setecientos ochenta y dos años, y engendró hijos e hijas.
Ndipo atabadwa Lameki, Metusela anakhala ndi moyo zaka zina 782 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
27 Y fueron todos los días de Matusalén novecientos sesenta y nueve años, y murió.
Zaka zonse za Metusela zinali 969, ndipo anamwalira.
28 Lamec tenía ciento ochenta y dos años, cuando engendró un hijo,
Pamene Lameki anali ndi zaka 182, anabereka mwana wamwamuna.
29 al cual puso por nombre Noé, diciendo: Este nos consolará de nuestras fatigas y del trabajo de nuestras manos, causado por la tierra que maldijo Yahvé.
Ndipo anamutcha Nowa ndipo anati, “Iyeyu adzatipumulitsa ku ntchito zathu zolemetsazi, zolima nthaka imene Yehova anayitemberera.”
30 Vivió Lamec, después de engendrar a Noé, quinientos noventa y cinco años, y engendró hijos e hijas.
Atabadwa Nowa, Lameki anakhala zaka zina 595 ndipo anabereka ana ena aamuna ndi aakazi.
31 Y fueron todos los días de Lamec setecientos setenta y siete años, y murió. Noé tenía quinientos años, cuando engendró a Sem, Cam y Jafet.
Zaka zonse za Lameki zinali 777, ndipo kenaka anamwalira.
Pamene Nowa anali ndi zaka 500, anabereka Semu, Hamu ndi Yafeti.

< Génesis 5 >