< 1 Crónicas 25 >
1 David y los jefes del ejército separaron para el culto a los que de entre los hijos de Asaf, de Hemán y de Jedutún tenían que ejercer la música sacra con cítaras, salterios y címbalos. He aquí el número de los hombres que hacían esto en su ministerio:
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 De los hijos de Asaf: Zacur, José, Netanías y Asarela, hijos de Asaf, bajo la dirección de Asaf, que ejercía su ministerio según las órdenes del rey.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 De Jedutún: los hijos de Jedutún: Gedalías, Serí, Isaías, Hasabías, Matatías (y Simeí), seis, bajo la dirección de su padre Jedutún, que cantaba con la cítara para celebrar y alabar a Yahvé.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 De Hemán: los hijos de Hemán: Bukías, Matanías, Uciel, Sebuel, Jerimot, Hananías, Hananí, Eliata, Gidalti, Romamtiéser, Josbecasa, Malloti, Hotir y Mahasiot.
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 Todos estos eran hijos de Hemán, vidente del rey en las cosas de Dios para ensalzar su poder. Dios había dado a Hemán catorce hijos y tres hijas.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Todos estos estaban bajo la dirección de su padre en el canto de la Casa de Yahvé, con címbalos, salterios y cítaras para cumplir su ministerio en la Casa de Dios. Asaf, Jedutún y Hemán estaban a las órdenes del rey.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 El número de ellos, con sus hermanos, los que eran instruidos en el canto de Yahvé, todos ellos maestros, era de doscientos ochenta y ocho.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 Echaron suertes para (determinar) sus funciones, sobre pequeños y grandes, hábiles y menos hábiles.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 Salió la primera suerte de (la casa de) Asaf: para José, la segunda para Gedalías, para él, sus hermanos e hijos: doce;
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 la tercera para Zacur, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 la cuarta para Isrí, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 la quinta para Netanías, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 la sexta para Bukías, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 la séptima para Jesarela, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 la octava para Isaías, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 la nona, para Matanías, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 la décima para Simeí, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 la undécima para Asarel, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 la duodécima para Hasabías, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 la decimotercia para Subael, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 la decimocuarta para Matatías, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 la decimoquinta para Jeremot, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 la decimosexta para Hananías, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 la decimoséptima para Josbecasa, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 la decimoctava para Hananí, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 la decimonona para Malloti, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 la vigésima para Eliata, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 la vigésimo prima para Hotir, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 la vigesimosegunda para Gidalti, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 la vigesimotercera para Mahasiot, con sus hijos y hermanos: doce;
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 la vigesimocuarta para Romamtiéser, con sus hijos y hermanos: doce.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.