< Psalmi 82 >
1 Bog stoji v skupnosti mogočnih, sodi med bogovi.
Salimo la Asafu. Mulungu akutsogolera msonkhano waukulu; Iye akuweruza pakati pa “milungu.”
2 »Doklej boste nepravično sodili in sprejemali zunanjost zlobnih? (Sela)
“Mudzateteza osalungama mpaka liti, ndi kukondera anthu oyipa?
3 Branite revne in osirotele, ravnajte pravično prizadetim in pomoči potrebnim.
Tetezani anthu ofowoka ndi amasiye; mukhazikitse ufulu wa anthu osauka ndi ozunzika.
4 Osvobodite uboge in pomoči potrebne, odstranite jih iz roke zlobnih.«
Landitsani anthu ofowoka ndi osowa; apulumutseni mʼdzanja la anthu oyipa.
5 Ne vedo niti ne bodo razumeli, hodijo v temi. Vsi temelji zemlje so izven naravnega reda.
“Iwo sadziwa kanthu, sazindikira kalikonse. Amayendayenda mu mdima; maziko onse a dziko lapansi agwedezeka.
6 Rekel sem: »Vi ste bogovi in vsi izmed vas ste otroci Najvišjega.
“Ndinati, ‘Inu ndinu Mulungu, nonsenu ndinu ana a Wammwambamwamba.’
7 Vendar boste umrli kakor ljudje in padli kakor kdo izmed princev.«
Koma mudzafa ngati anthu wamba; mudzagwa ngati wolamula wina aliyense.”
8 Vstani, oh Bog, sodi zemljo, kajti ti boš podedoval vse narode.
Dzukani Inu Mulungu, weruzani dziko lapansi, pakuti mayiko onse ndi cholowa chanu.