< Psalmi 125 >
1 Tisti, ki zaupajo v Gospoda, bodo kakor gora Sion, ki ne more biti odstranjena, temveč ostaja na veke.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Amene amadalira Yehova ali ngati phiri la Ziyoni, limene silingagwedezeke koma ndi lokhala mpaka muyaya.
2 Kakor so gore naokoli Jeruzalema, tako je Gospod naokoli svojega ljudstva od tega časa naprej, celo za vedno.
Monga mapiri azungulira Yerusalemu, momwemonso Yehova azungulira anthu ake kuyambira tsopano mpaka muyaya.
3 Kajti palica zlobnih ne bo počivala na deležu pravičnih, da ne bi pravični svojih rok iztegnili h krivičnosti.
Ndodo yaufumu ya anthu oyipa sidzakhala pa dziko limene lapatsidwa kwa anthu olungama, kuti anthu olungamawo angachite nawonso zoyipa.
4 Delaj dobro, oh Gospod, tistim, ki so dobri in tistim, ki so iskreni v svojih srcih.
Yehova chitirani zabwino amene ndi abwino, amene ndi olungama mtima
5 Glede takšnih, ki zavijajo na svoje sprijene poti, jih bo Gospod odvedel z delavci krivičnosti, toda nad Izraelom bo mir.
Koma amene amatembenukira ku njira zokhotakhota, Yehova adzawachotsa pamodzi ndi anthu ochita zoyipa. Mtendere ukhale pa Israeli.