< 1 Kroniška 25 >

1 Poleg tega so David in poveljniki vojske oddvojili k službi od Asáfovih, Hemánovih in Jedutúnovih sinov, ki naj bi prerokovali s harfami, s plunkami in s cimbalami. Število delavcev glede na njihovo službo je bilo:
Davide ndi atsogoleri a asilikali anapatula ena mwa ana a Asafu, Hemani ndi Yedutuni ku utumiki wa uneneri pogwiritsa ntchito apangwe, azeze ndi ziwaya zamalipenga. Tsopano nawu mndandanda wa anthu amene ankagwira ntchito imeneyi:
2 izmed Asáfovih sinov Zahúr, Jožef, Netanjá in Asaréla, Asáfovi sinovi pod Asáfovo roko, ki so prerokovali glede na kraljev ukaz.
Kuchokera kwa ana a Asafu: Zakuri, Yosefe, Netaniya ndi Asareli. Ana a Asafu amalamulidwa ndi Asafu ndipo amanenera moyangʼaniridwa ndi mfumu.
3 Od Jedutúna: Jedutúnovi sinovi Gedaljá, Cerí, Ješajá, Hašabjá, Matitjá, šest, pod rokami njihovega očeta Jedutúna, ki so prerokovali s harfo, da se zahvaljujejo in hvalijo Gospoda.
Kwa Yedutuni, kuchokera kwa ana ake: Gedaliya, Zeri, Yesaya, Simei, Hasabiya ndi Matitiya. Onse analipo 9 ndipo amayangʼaniridwa ndi Yedutuni abambo awo, amene amanenera pogwiritsa ntchito apangwe poyamika ndi kutamanda Yehova.
4 Od Hemána: Hemánovi sinovi Bukijá, Matanjá, Uziél, Šebuél, Jerimót, Hananjá, Hananí, Eliát, Gidálti, Romámti Ezer, Jošbekáša, Malóti, Hotír in Mahaziót.
Kwa Hemani, kuchokera kwa ana ake: Bukiya, Mataniya, Uzieli, Subaeli ndi Yerimoti; Hananiya, Hanani, Eliata, Gidaliti ndi Romamiti-Ezeri; Yosibakasa, Maloti, Hotiri ndi Mahazioti.
5 Vsi ti so bili sinovi kraljevega vidca Hemána v Božjih besedah, da dvigujejo rog. In Bog je dal Hemánu štirinajst sinov in tri hčere.
Onsewa anali ana a Hemani mlosi wa mfumu. Iye anapatsidwa anawa potsata mawu a Mulungu akuti adzamukweza. Mulungu anapatsa Hemani ana aamuna 14 ndi ana aakazi atatu.
6 Vsi ti so bili pod rokami njihovega očeta za pesem v Gospodovi hiši s cimbalami, plunkami in harfami, za službo Božje hiše, glede na kraljev ukaz Asáfu, Jedutúnu in Hemánu.
Anthu onsewa ankayangʼaniridwa ndi makolo awo pa mayimbidwe a mʼNyumba ya Yehova. Iwowatu ankayimba ndi ziwaya zamalipenga, azeze ndi apangwe potumikira mʼNyumba ya Mulungu. Koma Asafu, Yedutuni ndi Hemani amayangʼaniridwa ndi mfumu.
7 Tako je bilo njihovo število, z njihovimi brati, ki so bili poučeni v Gospodovih pesmih, celó vseh, ki so bili spretni, dvesto oseminosemdeset.
Iwo pamodzi ndi abale awo onse ophunzitsidwa ndi aluso loyimbira Yehova chiwerengero chawo chinali 288.
8 Metali so žrebe, stražo do straže, tako majhen kakor velik, učitelj kakor učenec.
Angʼonoangʼono ndi akulu omwe, mphunzitsi ndi wophunzira yemwe anachita maere pa ntchito zawo.
9 Torej prvi žreb je prišel za Asáfa k Jožefu; drugi Gedaljáju, katerih je bilo z njegovimi brati in sinovi dvanajst;
Maere woyamba amene anali a Asafu, anagwera Yosefe, ana ndi abale ake. 12 Maere achiwiri anagwera Gedaliya, ndi abale ake ndi ana ake. 12
10 tretji Zahúrju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere achitatu anagwera Zakuri, ana ake ndi abale ake. 12
11 četrti Izriju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere achinayi anagwera Iziri, ana ake ndi abale ake. 12
12 peti Netanjáju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere achisanu anagwera Netaniya, ana ake ndi abale ake. 12
13 šesti Bukijáju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere achisanu ndi chimodzi anagwera Bukiya, ana ake ndi abale ake. 12
14 sedmi Jesarelu, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere achisanu ndi chiwiri anagwera Yesarela, ana ake ndi abale ake. 12
15 osmi Ješajáju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere achisanu ndi chitatu anagwera Yeshaya, ana ake ndi abale ake. 12
16 deveti Matanjáju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere achisanu ndi chinayi anagwera Mataniya, ana ake ndi abale ake. 12
17 deseti Šimíju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a khumi anagwera Simei, ana ake ndi abale ake. 12
18 enajsti Azarélu, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 11 anagwera Azareli, ana ake ndi abale ake. 12
19 dvanajsti Hašabjáju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 12 anagwera Hasabiya, ana ake ndi abale ake. 12
20 trinajsti Šubaélu, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 13 anagwera Subaeli, ana ake ndi abale ake. 12
21 štirinajsti Matitjáju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 14 anagwera Matitiya, ana ake ndi abale ake. 12
22 petnajsti Jeremótu, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 15 anagwera Yeremoti, ana ake ndi abale ake. 12
23 šestnajsti Hananjáju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 16 anagwera Hananiya, ana ake ndi abale ake. 12
24 sedemnajsti Jošbekášaju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 17 anagwera Yosibakasa, ana ake ndi abale ake. 12
25 osemnajsti Hananíju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 18 anagwera Hanani, ana ake ndi abale ake. 12
26 devetnajsti Malótiju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 19 anagwera Maloti, ana ake ndi abale ake. 12
27 dvajseti Eliátaju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 20 anagwera Eliyata, ana ake ndi abale ake. 12
28 enaindvajseti Hotírju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 21 anagwera Hotiri, ana ake ndi abale ake. 12
29 dvaindvajseti Gidáltiju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 22 anagwera Gidaliti, ana ake ndi abale ake. 12
30 triindvajseti Mahaziótaju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst;
Maere a 23 anagwera Mahazioti, ana ake ndi abale ake. 12
31 štiriindvajseti Romámti Ezerju, njemu, njegovim sinovom in njegovim bratom, bilo jih je dvanajst.
Maere a 24 anagwera Romamiti-Ezeri, ana ake ndi abale ake 12.

< 1 Kroniška 25 >