< Псалтирь 87 >

1 Сыном Кореовым, псалом песни.
Salimo la Ana a Kora. Iye wakhazikitsa maziko ake pa phiri loyera;
2 Основания его на горах святых: любит Господь врата Сионя паче всех селений Иаковлих.
Yehova amakonda zipata za Ziyoni kupambana malo onse okhalamo a Yakobo.
3 Преславная глаголашася о тебе, граде Божий.
Za ulemerero wako zimakambidwa, Iwe mzinda wa Mulungu: (Sela)
4 Помяну Раав и Вавилона ведущым мя: и се, иноплеменницы и Тир и людие Ефиопстии, сии быша тамо.
“Ndidzanena za Rahabe ndi Babuloni pakati pa iwo amene amandidziwa. Dzikonso la Filisitiya, Turo pamodzi ndi Kusi, ndipo ndidzati, ‘Uyu anabadwira mʼZiyoni.’”
5 Мати Сион речет: человек и человек родися в нем, и Той основа и Вышний.
Ndithudi, za Ziyoni adzanena kuti, “Uyu ndi uyo anabadwira mwa iye, ndipo Wammwambamwamba adzakhazikitsa iyeyo.”
6 Господь повесть в писании людий и князей, сих бывших в нем.
Yehova adzalemba mʼbuku la kawundula wa anthu a mitundu ina: “Uyu anabadwira mʼZiyoni.” (Sela)
7 Яко веселящихся всех жилище в тебе.
Oyimba ndi ovina omwe adzati, “Akasupe anga onse ali mwa iwe.”

< Псалтирь 87 >