< Псалми 30 >

1 Узвишаваћу Те, Господе, јер си ме отео, и ниси дао непријатељима мојим да ми се свете.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba popereka Nyumba ya Mulungu. Ndidzakukwezani Yehova, chifukwa mwanditulutsa kwakuya, ndipo simunalole kuti adani anga akondwere pa ine.
2 Господе, Боже мој! Завиках к Теби, и исцелио си ме.
Inu Yehova Mulungu wanga ndinapempha kwa Inu thandizo ndipo Inu munandichiritsa.
3 Господе! Извео си из пакла душу моју, и оживео си ме да не сиђем у гроб. (Sheol h7585)
Inu Yehova, munanditulutsa ku manda, munandisunga kuti ndisatsalire mʼdzenje. (Sheol h7585)
4 Појте Господу, свеци Његови, и славите свето име Његово.
Imbirani Yehova inu anthu ake okhulupirika; tamandani dzina lake loyera.
5 Гнев је Његов за тренуће ока, а до живота милост Његова, вечером долази плач, а јутром радост.
Pakuti mkwiyo wake umakhala kwa kanthawi koma kukoma mtima kwake ndi kwa moyo wonse; utha kuchezera kulira usiku wonse, koma chimwemwe chimabwera mmawa.
6 И ја рекох у добру свом: Нећу посрнути довека.
Pamene ndinaona kuti ndili otetezedwa ndinati, “Sindidzagwedezekanso.”
7 Ти хтеде, Господе, те гора моја стајаше тврдо. Ти одврати лице своје, и ја се сметох.
Inu Yehova, pamene munandikomera mtima, munachititsa phiri langa kuyima chilili; koma pamene munabisa nkhope yanu, ndinataya mtima.
8 Тада Тебе, Господе, зазивах, и Господа молих:
Kwa Inu Yehova ndinayitana; kwa Ambuye ndinapempha chifundo;
9 "Каква је корист од крви моје, да сиђем у гроб? Хоће ли Те прах славити или казивати истину Твоју?
“Kodi pali phindu lanji powonongeka kwanga ngati nditsikira ku dzenje? Kodi fumbi lidzakutamandani Inu? Kodi lidzalengeza za kukhulupirika kwanu?
10 Чуј, Господе, и смилуј се на ме; Господе буди ми помоћник."
Imvani Yehova ndipo mundichitire chifundo; Yehova mukhale thandizo langa.”
11 И Ти промени плач мој на радост, скиде с мене врећу. опаса ме весељем.
Inu munasandutsa kulira kwanga kukhala kuvina; munachotsa chiguduli changa ndi kundiveka ndi chimwemwe,
12 Зато ће Ти певати слава моја и неће умукнути; Господе, Боже мој! Довека ћу Те хвалити.
kuti mtima wanga uthe kuyimbira Inu usakhale chete. Yehova Mulungu wanga, ndidzapereka kwa Inu mayamiko kwamuyaya.

< Псалми 30 >