< Псалми 128 >

1 Благо свакоме, који се боји Господа, који ходи путевима Његовим!
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Odala ndi onse amene amaopa Yehova, amene amayenda mʼnjira zake.
2 Јер ће јести од трудова руку својих. Благо теби, и добро ти је.
Udzadya chipatso cha ntchito yako; madalitso ndi chuma zidzakhala zako.
3 Жена је твоја као родна лоза усред дома твог; синови твоји као гране маслинове око стола твог.
Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka mʼkati mwa nyumba yako; ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi kuzungulira tebulo lako.
4 Гле, тако ће бити благословен човек који се боји Господа.
Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa amene amaopa Yehova.
5 Благословиће те Господ са Сиона, и гледаћеш добро јерусалимско у све дане живота свог;
Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni masiku onse a moyo wako; uwone zokoma za Yerusalemu,
6 Видећеш синове у синова својих. Мир Израиљу!
ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako. Mtendere ukhale ndi Israeli.

< Псалми 128 >