< Псалми 116 >

1 Мило ми је што Господ услиши молитвени глас мој;
Ndimakonda Yehova pakuti Iyeyo amamva mawu anga; Iye amamva kulira kwanga kopempha chifundo.
2 Што пригну к мени ухо своје; и зато ћу Га у све дане своје призивати.
Pakuti ananditchera khutu, ndidzayitana Iye masiku onse a moyo wanga.
3 Опколише ме болести смртне, и јади паклени задесише ме, наиђох на тугу и муку; (Sheol h7585)
Zingwe za imfa zinandizinga, zoopsa za ku dziko la anthu akufa zinandigwera; ndinapeza mavuto ndi chisoni. (Sheol h7585)
4 Али призвах име Господње: Господе! Избави душу моју!
Pamenepo ndinayitana dzina la Yehova: “Inu Yehova, pulumutseni!”
5 Добар је Господ и праведан, и Бог је наш милостив;
Yehova ndi wokoma mtima ndi wolungama Mulungu wathu ndi wodzaza ndi chifundo.
6 Чува просте Господ; бејах у невољи, и поможе ми.
Yehova amateteza munthu wodzichepetsa mtima; pamene ndinali ndi chosowa chachikulu, Iye anandipulumutsa.
7 Врати се душо моја, у мир свој! Јер је Господ добротвор твој!
Pumula iwe moyo wanga, pakuti Yehova wakuchitira zokoma.
8 Ти си избавио душу моју од смрти, око моје од суза, ногу моју од спотицања.
Pakuti Inu Yehova mwapulumutsa moyo wanga ku imfa, maso anga ku misozi, mapazi anga kuti angapunthwe,
9 Ходићу пред лицем Господњим по земљи живих.
kuti ine ndiyende pamaso pa Yehova mʼdziko la anthu amoyo.
10 Веровах кад говорих: У љутој сам невољи.
Ine ndinakhulupirira; choncho ndinati, “Ndasautsidwa kwambiri.”
11 Рекох у сметњи својој: Сваки је човек лажа.
Ndipo ndili mʼnkhawa yanga ndinati, “Anthu onse ndi abodza.”
12 Шта ћу вратити Господу за сва добра што ми је учинио?
Ndingamubwezere chiyani Yehova, chifukwa cha zokoma zake zonse zimene wandichitira?
13 Узећу чашу спасења, и призваћу име Господње.
Ndidzakweza chikho cha chipulumutso ndipo ndidzayitana dzina la Yehova.
14 Извршићу обећања своја Господу пред свим народом Његовим.
Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse.
15 Скупа је пред Господом смрт светаца Његових.
Imfa ya anthu oyera mtima ndi yamtengowapatali pamaso pa Yehova.
16 О Господе! Ја сам слуга Твој, ја сам слуга Твој, син слушкиње Твоје; расковао си с мене окове моје.
Inu Yehova, zoonadi ndine mtumiki wanu: ndine mtumiki wanu, mwana wa mdzakazi wanu; Inu mwamasula maunyolo anga.
17 Жртву за хвалу принећу Теби, и име Господње призваћу.
Ndidzapereka nsembe yachiyamiko kwa Inu ndipo ndidzayitanira pa dzina la Yehova.
18 Извршићу обећања своја Господу пред свим народом Његовим,
Ndidzakwaniritsa malonjezo anga kwa Yehova pamaso pa anthu ake onse,
19 У двору дома Господњег, усред тебе, Јерусалиме. Алилуја!
mʼmabwalo a nyumba ya Yehova, mʼkati mwako iwe Yerusalemu. Tamandani Yehova.

< Псалми 116 >