< Књига пророка Михеја 2 >
1 Тешко онима који смишљају безакоње и о злу се труде на постељама својим, и кад сване извршују, јер им је сила у руци.
Tsoka kwa amene amakonzekera chiwembu, kwa amene amakonzekera kuchita zoyipa usiku pa mabedi awo! Kukacha mmawa amakachitadi chifukwa ali ndi mphamvu zochitira zimenezo.
2 Желе њиве, и отимају их; желе куће, и узимају; чине силу човеку и кући његовој, човеку и наследству његовом.
Amasirira minda ndi kuyilanda, amasirira nyumba ndi kuzilanda. Amatenga nyumba ya munthu mwachinyengo, munthu mnzawo kumulanda cholowa chake.
3 Зато овако вели Господ: Ево, ја мислим зло том роду, из ког нећете извући вратове своје, нити ћете ходити поносито, јер ће бити зло време.
Nʼchifukwa chake Yehova akuti, “Ine ndikukonzekera kubweretsa tsoka pa anthu awa, tsoka limene simudzatha kudzipulumutsa nokha. Inu simudzayendanso monyada, pakuti idzakhala nthawi ya masautso.
4 У оно време говориће се прича о вама, и нарицаће се жалосно говорећи: Пропадосмо; промени део народа мог. Како ми узе! Узевши њиве наше раздели.
Tsiku limenelo anthu adzakuchitani chipongwe; adzakunyogodolani ndi nyimbo iyi yamaliro: ‘Tawonongeka kotheratu; dziko la anthu anga lagawidwa. Iye wandilanda! Wapereka minda yathu kwa anthu otiwukira.’”
5 Зато нећеш имати никога ко би ти повукао уже за жреб у збору Господњем.
Nʼchifukwa chake simudzakhala ndi munthu mu msonkhano wa Yehova kuti agawe dziko pochita maere.
6 Немојте пророковати, нека они пророкују; ако им не пророкују, неће одступити срамота.
Aneneri awo amanena kuti, “Usanenere! Usanenere ndi pangʼono pomwe zimenezi; ife sitidzachititsidwa manyazi.”
7 О ти, који се зовеш дом Јаковљев, је ли се умалио Дух Господњи? Јесу ли то дела Његова? Еда ли моје речи нису добре ономе који ходи право?
Inu nyumba ya Yakobo, monga zimenezi ndi zoyenera kuzinena: “Kodi Mzimu wa Yehova wakwiya? Kodi Iye amachita zinthu zotere?” “Kodi mawu ake sabweretsa zabwino kwa amene amayenda molungama?
8 А народ се мој пре подиже као непријатељ; преко хаљине скидате плашт с оних који пролазе не бојећи се, који се враћају из боја.
Posachedwapa anthu anga andiwukira ngati mdani. Mumawavula mkanjo wamtengowapatali anthu amene amadutsa mosaopa kanthu, monga anthu amene akubwera ku nkhondo.
9 Жене народа мог изгоните из милих кућа њихових, од деце њихове отимате славу моју навек.
Mumatulutsa akazi a anthu anga mʼnyumba zawo zabwino. Mumalanda ana awo madalitso anga kosatha.
10 Устаните и идите, јер ово није почивалиште; што се оскврни, погубиће вас погибљу великом.
Nyamukani, chokani! Pakuti ano si malo anu opumulirapo, chifukwa ayipitsidwa, awonongedwa, sangatheke kuwakonzanso.
11 Ако ко ходи за ветром и казује лажи говорећи: Пророковаћу ти за вино и за силовито пиће, тај ће бити пророк овом народу.
Ngati munthu wabodza ndi wachinyengo abwera nʼkunena kuti, ‘Ine ndidzanenera ndipo mudzakhala ndi vinyo ndi mowa wambiri, woteroyo adzakhala mneneri amene anthu awa angamukonde!’
12 Доиста ћу те сабрати свог, Јакове, доиста ћу скупити остатак Израиљев; поставићу их заједно као овце восорске, као стадо усред тора њиховог, биће врева од људства.
“Inu banja la Yakobo, ndidzakusonkhanitsani nonse; ndidzawasonkhanitsa pamodzi otsala a ku Israeli. Ndidzawabweretsa pamodzi ngati nkhosa mʼkhola, ngati ziweto pa msipu wake; malowo adzadzaza ndi chinamtindi cha anthu.
13 Пред њима ће ићи који разбија; они ће разбити и проћи кроз врата, и изаћи ће; и цар ће њихов ићи пред њима, и Господ ће бити пред њима.
Amene adzawapulumutse adzayenda patsogolo pawo; iwo adzathyola chipata ndipo adzatuluka. Mfumu yawo idzawatsogolera, Yehova adzakhala patsogolo pawo.”