< Psalmi 129 >

1 Mnogo mi dosaðivaše od mladosti moje, neka reèe Izrailj,
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. “Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga,” anene tsono Israeli;
2 Mnogo mi dosaðivaše od mladosti moje, ali me ne svladaše.
“Andizunza kwambiri kuyambira ubwana wanga, koma sanandipambane.
3 Na leðima mojim oraše oraèi, i vodiše duge brazde svoje.
Anthu otipula analima pa msana panga ndipo anapangapo mizere yayitali:
4 Gospod je pravedan; isijeèe konopce bezbožnièke.
Koma Yehova ndi wolungama; Iye wandimasula ku zingwe za anthu oyipa.”
5 Postidjeæe se, odbiæe se svi koji nenavide Sion.
Onse amene amadana ndi Ziyoni abwezedwe pambuyo mwamanyazi.
6 Biæe kao trava na krovovima, koja se sasušuje prije nego se poèupa,
Akhale ngati udzu womera pa denga la nyumba, umene umafota usanakule;
7 Od koje neæe žetelac napuniti ruke svoje, niti naruèja svojega vezilac;
sungadzaze manja a owumweta kapena manja a omanga mitolo.
8 I koji prolaze neæe reæi: “Blagoslov Gospodnji na vama! blagosiljamo vas imenom Gospodnjim.”
Odutsa pafupi asanene kuti, “Dalitso la Yehova lili pa inu; tikukudalitsani mʼdzina la Yehova.”

< Psalmi 129 >