< Psalmi 120 >

1 Ka Gospodu zavikah u nevolji svojoj, i usliši me.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Gospode! izbavi dušu moju od usta lažljivijeh i od jezika lukavoga.
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Šta æe ti dati i šta æe ti prinijeti jezik lukavi?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 On je kao oštre strijele u jakoga, kao ugljevlje smrekovo.
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Teško meni kad sam tuðin kod Meseha, živim kod šatora Kidarskih.
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Dugo je živjela duša moja s onima koji mrze na mir.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Ja sam miran; ali kad stanem govoriti, u njih je rat.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.

< Psalmi 120 >