< Sudije 20 >

1 Tada izidoše svi sinovi Izrailjevi, i sabra se sav narod jednodušno, od Dana do Virsaveje i do zemlje Galadove, ka Gospodu u Mispu.
Ndipo Aisraeli onse kuyambira ku dziko la Dani mpaka ku Beeriseba ndiponso ku dziko la Giliyadi ananyamuka ngati munthu mmodzi nakasonkhana pamaso pa Yehova ku Mizipa.
2 I glavari svega naroda, svijeh plemena Izrailjevijeh, doðoše na zbor naroda Božijega, èetiri stotine tisuæa ljudi pješaka koji mahahu maèem.
Atsogoleri a anthu onse ndi a mafuko onse Aisraeli anali nawo pa msonkhano wa anthu a Mulungu. Onse pamodzi analipo asilikali oyenda pansi 400,000 atanyamula malupanga.
3 A sinovi Venijaminovi èuše da su sinovi Izrailjevi otišli u Mispu. Sinovi Izrailjevi rekoše: kažite kako se dogodilo to zlo.
Anthu a fuko la Benjamini anali atamva kuti Aisraeli apita ku Mizipa. Tsono Aisraeli anati, “Tiwuzeni, zinthu zoyipa izi zinachitika bwanji.”
4 A Levit, muž ubijene žene, odgovori i reèe: doðoh s inoèom svojom u Gavaju Venijaminovu da prenoæim.
Choncho Mlevi uja, mwamuna wa mkazi wophedwa uja anayankha nati, “Ine ndinapita ku Gibeya mʼdziko la Benjamini pamodzi ndi mzikazi wanga kuti tikagone kumeneko.
5 A Gavajani ustaše na me, opkoliše me u kuæi noæu, i htješe me ubiti; i inoèu moju zlostaviše tako da umrije.
Usiku anthu a ku Gibeya anandiwukira, nazinga nyumba munali ine. Ankafuna kundipha ndipo anagona ndi mzikazi wanga momukakamiza mpaka anafa.
6 Zato uzev inoèu svoju isjekoh je na komade i razaslah je u sve krajeve našljedstva Izrailjeva; jer uèiniše grdilo i sramotu u Izrailju.
Ine ndinatenga mzikazi wangayo ndi kumudula nthulinthuli ndikuzitumiza kwa fuko lililonse la Aisraeli. Anthu amenewa, zedi achita chinthu chonyansa kwambiri mʼdziko lino la Israeli.
7 Eto, vi ste svi sinovi Izrailjevi; promislite i vijeæajte.
Ndi zimenezotu inu Aisraeli nonse; yankhulaponi mawu ndi kupereka maganizo anu.”
8 A sav narod usta jednodušno i reèe: da ne idemo nijedan k šatoru svojemu, i nijedan da se ne vraæa kuæi svojoj.
Anthu onse anayimirira ngati munthu mmodzi nanena kuti, “Palibe mmodzi wa ife amene apite ku nyumba kwake. Palibe amene abwerere ku nyumba kwake.
9 Nego ovo da uèinimo Gavaji: da bacimo ždrijeb za nju.
Koma tsopano chimene ife tichite ndi dziko la Gibeya ndi ichi: Tidzapita kukamenyana nawo potsatira zimene maere anene.
10 Da uzmemo po deset ljudi od stotine po svijem plemenima Izrailjevijem, i po stotinu od tisuæe, i po tisuæu od deset tisuæa, da donese hranu narodu, a on da ide da uèini Gavaji Venijaminovoj kako je zaslužila grdilom koje je uèinila Izrailju.
Mʼmafuko onse a Aisraeli tidzasankha anthu khumi pa anthu 100 aliwonse: ndiye kuti anthu 100 pa anthu 1,000 aliwonse kapena anthu 1,000 pa anthu 10,000 aliwonse. Anthu amenewa adzasonkhanitsa zakudya za ankhondo, ndipo ankhondowo adzapita kukalipsira anthu a ku Geba mʼdziko la Benjamini chifukwa chochita chinthu chonyansa chotere mʼdziko la Israeli.”
11 I skupi se sav narod Izrailjev na onaj grad složivši se jednodušno.
Choncho anthu a ku Israeli anasonkhana pamodzi nagwirizana chimodzi, kukalimbana ndi mzindawo.
12 Tada poslaše plemena Izrailjeva ljude u sve porodice Venijaminove, i poruèiše im: kakvo se to zlo uèini meðu vama?
Mafuko a Israeli anatumiza anthu kwa fuko lonse la Benjamini kukafunsa kuti, “Kodi zoyipa zachitika pakati panuzi ndi zotani?
13 Sada dajte te bezakonike što su u Gavaji, da ih pogubimo i izvadimo zlo iz Izrailja. Ali ne htješe sinovi Venijaminovi poslušati braæe svoje, sinova Izrailjevijeh.
Tsono tikuti mutipatse anthu achabechabe a ku Gibeya kuti tiwaphe kuti tichotse chinthu choyipachi mʼdziko la Israeli.” Koma fuko la Benjamini silinafune kumvera zimene ananena Aisraeli anzawo.
14 Nego se skupiše sinovi Venijaminovi iz svojih mjesta u Gavaju da izidu da se biju sa sinovima Izrailjevijem.
Mʼmalo mwake, Abenjaminiwo anatuluka mʼmizinda yawo ku Gibeya kukamenyana ndi Aisraeli.
15 I nabroji se u to vrijeme sinova Venijaminovijeh iz njihovijeh gradova dvadeset i šest tisuæa ljudi koji mahahu maèem osim stanovnika Gavajskih, kojih bješe na broj sedam stotina ljudi odabranijeh.
Tsiku limenelo Abenjamini anasonkhanitsa kuchokera ku mizinda yawo ankhondo 26,000 amalupanga awo, osawerengera anthu ena 700 a ku Gibeya amene anasankhidwa.
16 U svem tom narodu bješe sedam stotina ljudi odabranijeh, koji bjehu ljevaci, i svaki gaðaše kamenom iz praæke u dlaku ne promašujuæi.
Mwa onsewa panali ankhondo 70 amanzere amene aliyense anali wodziwa kulasa ngakhale tsitsi limodzi ndi mwala osaphonya.
17 A ljudi Izrailjaca nabroji se osim sinova Venijaminovijeh èetiri stotine tisuæa ljudi koji mahahu maèem, samijeh vojnika.
Aisraeli, kupatula fuko la Benjamini, anasonkhanitsa anthu 400,000 a malupanga, onse odziwa bwino nkhondo.
18 I ustavši otidoše k domu Boga silnoga, i upitaše Boga i rekoše sinovi Izrailjevi: ko æe izmeðu nas iæi prvi u boj na sinove Venijaminove? A Gospod reèe: Juda nek ide prvi.
Ndipo Aisraeli ananyamuka kupita ku Beteli kukafunsira kwa Mulungu. Iwo anati, “Ndani mwa ife amene angayambe kukamenyana ndi fuko la Benjamini?” Yehova anayankha kuti, “Fuko la Yuda ndilo liyambe.”
19 Potom ustavši rano sinovi Izrailjevi stadoše u oko prema Gavaji.
Mmawa mwake Israeli ananyamuka nakamanga msasa moyangʼanana ndi Gibeya.
20 I izidoše sinovi Izrailjevi u boj na sinove Venijaminove, i uvrstaše se sinovi Izrailjevi da udare na Gavaju.
Aisraeli anapita kukachita nkhondo ndi fuko la Benjamini ndipo anandandalika ankhondo awo moyangʼanana ndi Gibeya.
21 A sinovi Venijaminovi izidoše iz Gavaje, i povaljaše po zemlji izmeðu Izrailjaca u onaj dan dvadeset i dvije tisuæe ljudi.
A fuko la Benjamini anatuluka ku Gibeya ndipo tsiku limenelo anapha Aisraeli 22,000 ku nkhondoko.
22 Ali se narod sinova Izrailjevijeh oslobodi, te se opet uvrstaše na istom mjestu gdje se bijahu uvrstali prvoga dana.
Koma ankhondo a Israeli analimbikitsananso mtima ndipo anasonkhanitsanso kachiwiri ankhondo awo pa malo pamene anawandandalika poyamba paja.
23 Jer sinovi Izrailjevi otidoše te plakaše pred Gospodom do veèera, i upitaše Gospoda govoreæi: hoæemo li opet izaæi u boj na sinove Venijamina brata svojega? A Gospod im reèe: izidite na njih.
Aisraeli anapita kukalira pamaso pa Yehova mpaka madzulo. Iwo anafunsa Yehova kuti, “Kodi tipitenso kukamenyana ndi a fuko la Benjamini abale athu?” Yehova anayankha kuti, “Pitani mukalimbane nawo.”
24 I izidoše sinovi Izrailjevi na sinove Venijaminove drugi dan.
Ndipo Aisraeli anayandikiranso pafupi ndi fuko la Benjamini tsiku lachiwiri lake kuti amenyane nawo.
25 I sinovi Venijaminovi izidoše pred njih iz Gavaje drugi dan; i povaljaše po zemlji izmeðu sinova Izrailjevijeh opet osamnaest tisuæa ljudi, koji svi mahahu maèem.
Pa tsiku lachiwiri lomwelo Abenjamini anatulukanso mu mzinda wa Gibeya ndipo anaphanso ankhondo 18,000. Onse amene anawaphawo anali odziwa kugwiritsa ntchito bwino malupanga.
26 Tada svi sinovi Izrailjevi i sav narod izidoše i doðoše k domu Boga silnoga, i plakaše i stajaše ondje pred Gospodom, i postiše se onaj dan do veèera, i prinesoše žrtve paljenice i žrtve zahvalne pred Gospodom.
Tsono Aisraeli onse, gulu lonse la ankhondo, anapita ku Beteli kukalira pamaso pa Yehova. Anakhala pansi nasala zakudya tsiku lonse mpaka madzulo. Anapereka nsembe zopsereza ndi nsembe zachiyanjano pamaso pa Yehova.
27 Pa upitaše sinovi Izrailjevi Gospoda; jer ondje bijaše kovèeg zavjeta Božijega u ono vrijeme;
Bokosi la Chipangano cha Yehova linali kumeneko.
28 I Fines sin Eleazara sina Aronova stajaše pred njim u ono vrijeme. I rekoše: hoæemo li opet izaæi u boj na sinove Venijamina brata svojega ili æemo se okaniti? A Gospod im reèe: izidite, jer æu ih sjutra predati vama u ruke.
Finehasi mwana wa Eliezara mwana wa Aaroni ndiye ankatumikira nthawi imeneyo. Tsono Aisraeli anafunsa Yehova kuti, “Kodi tipitenso kukachita nkhondo ndi mʼbale athu Abenjamini, kapena ayi?” Yehova anayankha kuti, “Pitaninso chifukwa mawa ndidzawapereka mʼmanja mwanu.”
29 Tada namjesti Izrailj zasjede oko Gavaje.
Choncho Aisraeli anayika anthu obisalira mozungulira Gibeya.
30 I sinovi Izrailjevi izidoše treæi dan na sinove Venijaminove, i uvrstaše se prema Gavaji kao prvom i drugom.
Tsiku lachitatu anapita kukamenyana ndi Benjamini ndipo anayika ankhondo mʼmalo mwawo kuti amenyane ndi Gibeya monga anachitira poyamba.
31 A sinovi Venijaminovi izašavši pred narod odvojiše se od grada, i stadoše biti i sjeæi narod kao prvom i drugom po putovima, od kojih jedan ide k domu Boga silnoga a drugi u Gavaju, i po polju, i ubiše do trideset ljudi iz Izrailja.
Abenjamini anatuluka kukamenyana nawo anthuwo ndipo anapita kutali ndi mzindawo. Iwo anayamba kupha Aisraeli monga poyamba paja, kotero kuti anapha anthu pafupifupi makumi atatu. Mitembo ya ena inali mu misewu yayikulu yopita ku Beteli ndi ku Gibeya, ndipo ina inali kwina poyera.
32 I rekoše sinovi Venijaminovi: padaju pred nama kao prije. A sinovi Izrailjevi rekoše: da bježimo da ih otrgnemo od grada na putove.
Abenjamini ankanena kuti, “Tikuwagonjetsa monga poyamba.” Koma Aisraeli ankanena kuti, “Tiyeni tithawe kuti apite ku msewu chapatali ndi mzinda wawo.”
33 Tada svi sinovi Izrailjevi kretoše se sa svojega mjesta i uvrstaše se u Val-Tamaru; i zasjede Izrailjeve iskoèiše iz mjesta svojega, iz luka Gavajskih.
Choncho Aisraeli onse anachoka mʼmalo mwawo ndi kukandanda ku Baala-Tamara, ndipo Aisraeli obisalira aja anatuluka mʼmalo awo kummawa kwa Geba.
34 I doðe na Gavaju deset tisuæa ljudi izabranijeh iz svega Izrailja, i boj posta žešæi, a oni ne opaziše da æe ih zlo zadesiti.
Aisraeli osankhidwa 10,000 ndiwo anabwera kudzalimbana ndi mzinda wa Gibeya. Nkhondoyo inafika poyipa kwambiri mwakuti Abenjamini samadziwa kuti zoopsa zili pafupi kuwagwera.
35 I Gospod pobi Venijamina pred Izrailjem, i sinovi Izrailjevi pogubiše onaj dan od sinova Venijaminovijeh dvadeset i pet tisuæa i sto ljudi, koji svi maèem mahahu.
Tsono Yehova anagonjetsa Abenjamini pamaso pa Israeli motero kuti Aisraeli anapha ankhondo a Abenjamini 25,100 tsiku limenelo.
36 I sinovi Venijaminovi vidješe da su nadbijeni: jer sinovi Izrailjevi uzmakoše ispred sinova Venijaminovijeh uzdajuæi se u zasjede koje bijahu namjestili kod Gavaje;
Choncho Abenjamini anaona kuti agonjetsedwa. Paja Aisraeli anathawa fuko la Benjamini chifukwa ankadalira anthu amene anawayika kuti abisalire mzinda wa Gibeya.
37 A oni što bijahu u zasjedi navališe brže u Gavaju, i ušavši isjekoše sve po gradu oštrijem maèem.
Tsono anthu amene anabisala aja anachita changu kuwuthira nkhondo mzinda wa Gibeyawo. Ndipo anapha anthu onse a mu mzindawo ndi lupanga.
38 A bijahu sinovi Izrailjevi ugovorili s onima u zasjedi da za znak zapale vatru da se digne velik dim iz grada.
Chizindikiro chimene Aisraeli anapangana ndi anthu obisalira aja chinali chakuti obisalira aja akangofukiza utsi wambiri ngati mtambo mu mzindamo,
39 Tako sinovi Izrailjevi stadoše bježati iz boja, a sinovi Venijaminovi poèeše ubijati, i isjekoše do trideset ljudi izmeðu sinova Izrailjevijeh govoreæi: doista padaju pred nama kao u preðašnjem boju.
ndiye kuti Aisraeli enawo abwerere ku nkhondo. Pa nthawiyo nʼkuti Abenjamini atayamba kale kumenya Aisraeliwo kwambiri ndi kupha pafupifupi anthu makumi atatu. Ndipo iwo ankanena kuti, “Ndithu tawapha monga poyamba paja.”
40 Ali kad se plamen i dim kao stup diže iz grada, obazreše se sinovi Venijaminovi, i gle, oganj se iz grada dizaše do neba.
Koma pamene utsi wa chizindikiro uja unayamba kukwera tolotolo mmwamba kuchoka mu mzindamo, Abenjamini anayangʼana mʼmbuyo ndipo anangoona utsi mu mzinda onse uli tolotolo kukwera mmwamba.
41 Tada se vratiše sinovi Izrailjevi, a sinovi Venijaminovi smetoše se videæi da ih je zlo zadesilo;
Kenaka Aisraeli anabwerera ndipo Abenjamini anachita mantha, chifukwa anaona kuti zoopsa zili pafupi kuwagwera.
42 I pobjegoše ispred sinova Izrailjevijeh k pustinji; ali ih vojska gonjaše, i koji iz gradova izlažahu, biše ih meðu sobom.
Choncho anathawa pamaso pa Aisraeli kudzera njira ya ku chipululu, koma nkhondo inawapeza. Ndipo anaphedwa kumeneko ndi Aisraeli amene anachokera mu mzindamo.
43 Tako opkoliše sinove Venijaminove, goniše ih, tlaèiše ih od Menuje do Gavaje k istoku.
Anawazungulira Abenjaminiwo, nawathamangitsa ndi kuwagonjetseratu osawachitira chifundo mpaka ku dera la kummawa kwa Gibeya.
44 I pogibe sinova Venijaminovijeh osamnaest tisuæa ljudi, samijeh junaka.
Abenjamini 18,000 olimba mtima anaphedwa.
45 A onijeh što se okretoše i pobjegoše u pustinju k stijeni Rimonu, napabirèiše ih po putovima pet tisuæa ljudi, i tjeraše ih do Gidoma i pobiše ih dvije tisuæe ljudi.
Koma ena anatembenuka nathawira ku chipululu ku thanthwe la Rimoni. Mwa iwowa Aisraeli anapha Abenjamini 5,000 mʼmisewu yayikulu. Anawapitikitsabe Abenjaminiwo mpaka kufika ku Gidomu ndi kuphanso ena 2,000.
46 I tako svega pogibe onaj dan sinova Venijaminovijeh dvadeset i pet tisuæa ljudi koji mahahu maèem, sve samijeh junaka.
Pa tsiku limenelo Abenjamini olimba mtima okhala ndi malupanga okwana 25,000 anafa.
47 I bješe šest stotina ljudi koji se okretoše i utekoše u pustinju k stijeni Rimonu, i ostaše na stijeni Rimonu èetiri mjeseca.
Koma anthu 700 anabwerera ndi kuthawira ku chipululu ku thanthwe la Rimoni kumene anakhalako miyezi inayi.
48 Potom sinovi Izrailjevi vrativši se k sinovima Venijaminovijem isjekoše oštrijem maèem i ljude po gradovima i stoku i što se god naðe; i sve gradove koji ostaše popališe ognjem.
Aisraeli anabwerera kukamenyana ndi Abenjamini otsala ndi kuwapha ndi lupanga kuphatikizapo ziweto ndi zonse anali nazo. Ndipo anayatsa moto mizinda yonse anayipeza.

< Sudije 20 >