< Jov 28 >

1 Da, srebro ima žice, i zlato ima mjesto gdje se topi.
Pali mgodi wa siliva ndiponso malo oyengerapo golide.
2 Gvožðe se vadi iz praha, i iz kamena se topi mjed.
Chitsulo amachikumba pansi, ndipo mkuwa amawusungunula ku miyala yamkuwa.
3 Mraku postavlja meðu, i sve istražuje èovjek do kraja, i kamenje u tami i u sjenu smrtnom.
Munthu amalowa mu mdima atatenga nyale, amafunafuna miyala mpaka ku malire a mgodiwo, kufuna mkuwa mu mdima wandiweyani.
4 Rijeka navre s mjesta svojega da joj niko ne može pristupiti; ali se odbije i odlazi trudom èovjeèjim.
Amakumba njira zapansi mu mgodimo, kutali ndi kumene kumakhala anthu, kumalo kumene phazi la munthu silinapondeko; iye amakhala ali lende pansipo namazungulira uku ndi uku.
5 Iz zemlje izlazi hljeb, i pod njom je drugo, kao oganj.
Nthaka, imene imatulutsa zakudya, kunsi kwake kumachita ngati kwasandulizika ndi moto;
6 U kamenju je njezinu mjesto safiru, a ondje je prah zlatni.
miyala ya safiro imachokera mʼmatanthwe ake, ndipo mʼfumbi lake mumakhala miyala yagolide.
7 Te staze ne zna ptica, niti je vidje oko kragujevo;
Palibe mbalame yodya zinzake imene imadziwa njira yobisikayi, palibe kamtema amene anayiona.
8 Ne ugazi je mlado zvijerje, niti njom proðe lav.
Zirombo zolusa sizipondamo mʼnjiramo, ndipo mkango sudzeranso mʼmenemo.
9 Na kremen diže ruku svoju; prevraæa gore iz dna.
Munthu amaphwanya matanthwe olimba, ndipo amagubuduza mapiri kuyambira mʼtsinde.
10 Iz stijene izvodi potoke, i svašta dragocjeno vidi mu oko.
Amabowola njira mʼmatanthwewo; ndipo amaona chuma chonse cha mʼphirimo.
11 Ustavlja rijeke da ne teku, i što je sakriveno iznosi na vidjelo.
Amaletsa mitsinje ya pansipo kuti isayendenso, motero amatulutsira poyera zinthu zobisika.
12 Ali mudrost gdje se nalazi? i gdje je mjesto razumu?
“Koma nzeru zingapezeke kuti? Kodi kumvetsa zinthu kumakhala kuti?
13 Ne zna joj èovjek cijene, niti se nahodi u zemlji živijeh.
Munthu sadziwa kufunika kwake kwa nzeruzo; nzeruyo sipezeka pa dziko lino la anthu amoyo.
14 Bezdana veli: nije u meni; i more veli: nije kod mene.
Phompho likuti, ‘Sizipezeka mwa ine muno.’ Nyanja ikuti, ‘Mwa ine munonso ayi.’
15 Ne može se dati èisto zlato za nju, niti se srebro izmjeriti u promjenu za nju.
Nzeru sungazigule ndi golide wabwino kwambiri, mtengo wake sungawuyerekeze ndi siliva wambiri.
16 Ne može se cijeniti zlatom Ofirskim, ni dragim onihom ni safirom.
Nzeru singagulidwe ndi golide wa ku Ofiri, kapena ndi miyala ya onikisi kapena ya safiro.
17 Ne može se izjednaèiti s njom ni zlato ni kristal, niti se može promijeniti za zaklade zlatne.
Nzeru sungayiyerekeze ndi golide kapena mwala wa galasi, sungayigule ndi zokometsera zagolide.
18 Od korala i bisera nema spomena, jer je vrijednost mudrosti veæa nego dragom kamenju.
Miyala ya korali ndi krisitali siyoyeneranso ndi kuyitchula nʼkomwe; mtengo wa nzeru ndi woposa miyala ya rubi.
19 Ne može se s njom izjednaèiti topaz Etiopski, niti se može cijeniti èistijem zlatom.
Nzeru sungayiyerekeze ndi miyala ya topazi ya ku Kusi; nzeru singagulidwe ndi golide wabwino kwambiri.
20 Otkuda dakle dolazi mudrost? i gdje je mjesto razumu?
“Kodi tsono nzeru zimachokera kuti? Kodi kumvetsa zinthu kumakhala kuti?
21 Sakrivena je od oèiju svakoga živoga, i od ptica nebeskih zaklonjena.
Malo ake ndi obisika kwa zamoyo zonse, ndi obisika ngakhale kwa mbalame zamlengalenga.
22 Pogibao i smrt govore: ušima svojima èusmo slavu njezinu.
Chiwonongeko ndi imfa zikuti, ‘Tangomva mphekesera chabe ya zimenezo!’
23 Bog zna put njezin, i poznaje mjesto njezino.
Mulungu yekha ndiye amadziwa njira yake yopita kumeneko, ndipo Iye yekha amadziwa kumene nzeru imakhala,
24 Jer gleda do krajeva zemaljskih i vidi sve što je pod svijem nebom.
pakuti Iye amayangʼana mpaka ku malekezero a dziko lapansi ndipo amaona zonse za kunsi kwa thambo.
25 Kad davaše vjetru težinu, i mjeraše vodu mjerom,
Iye atapatsa mphepo mphamvu zake, nayeza kuzama kwa nyanja,
26 Kad postavljaše zakon daždu i put munji gromovnoj.
atakhazikitsa lamulo loti mvula izigwa ndi kukonza njira ya chingʼaningʼani cha bingu,
27 Još je onda vidje i oglasi je, uredi je i pretraži je.
pamenepo ndi pamene anayangʼana nzeruzo naziyeza mtengo wake; nazikhazikitsa ndi kuzisanthula bwino lomwe.
28 A èovjeku reèe: gle, strah je Božji mudrost, i uklanjati se oda zla jest razum.
Ndipo Iye anati kwa munthu, ‘Taonani, kuopa Ambuye, ndiye nzeru zimenezo ndipo kuthawa zoyipa ndiye kumvetsa zinthu kumeneko.’”

< Jov 28 >