< Isaija 55 >
1 Oj žedni koji ste god, hodite na vodu, i koji nemate novaca, hodite, kupujte i jedite; hodite, kupujte bez novaca i bez plate vina i mlijeka.
“Bwerani, inu nonse amene muli ndi ludzu, bwerani madzi alipo; ndipo inu amene mulibe ndalama bwerani, mudzagule chakudya kuti mudye! Bwerani mudzagule vinyo ndi mkaka osalipira ndalama, osalipira chilichonse.
2 Zašto trošite novce svoje na ono što nije hrana, i trud svoj na ono što ne siti? Slušajte me, pa æete jesti što je dobro, i duša æe se vaša nasladiti pretiline.
Chifukwa chiyani ndalama zanu mukuwonongera zinthu zimene samadya, ndipo mukuwononga malipiro anu pa zinthu zimene sizikhutitsa? Tamverani, mvetsetsani zimene ndikunena kuti mudye zimene zili zabwino; ndipo mudzisangalatse.
3 Prignite uho svoje i hodite k meni; poslušajte, i živa æe biti duša vaša, i uèiniæu s vama zavjet vjeèan, milosti Davidove istinite.
Tcherani makutu ndipo mubwere kwa Ine; mvereni Ine, kuti mukhale ndi moyo. Ndidzachita nanu pangano losatha, chikondi changa chija chosasinthika ndi chodalirika ndinalonjeza Davide.
4 Evo, dadoh ga za svjedoka narodima, za voða i zapovjednika narodima.
Taonani, ine ndamusankha kuti akhale mboni yanga kwa mitundu ya anthu, kuti akhale mtsogoleri ndi wolamulira mitundu ya anthu.
5 Evo, zvaæeš narod kojega nijesi znao, i narodi koji te nijesu znali steæi æe se k tebi, radi Gospoda Boga tvojega i sveca Izrailjeva, jer te proslavi.
Ndithu inu mudzayitanitsa mitundu ya anthu imene simuyidziwa, ndipo mitundu ya anthu imene sikudziwani idzabwera ndi liwiro kwa inu. Izi zidzatero chifukwa Yehova Mulungu wanu, Woyerayo wa Israeli, wakuvekani ulemerero.”
6 Tražite Gospoda, dok se može naæi; prizivajte ga, dokle je blizu.
Funafunani Yehova pamene Iye akupezeka. Mupemphere kwa Iye pamene ali pafupi.
7 Neka bezbožnik ostavi svoj put i nepravednik misli svoje; i neka se vrati ka Gospodu, i smilovaæu se na nj, i k Bogu našemu, jer prašta mnogo.
Woyipa asiye makhalidwe ake oyipa, ndipo wosalungama asinthe maganizo ake oyipa. Abwerere kwa Yehova, ndipo adzamuchitira chifundo, ndi kwa Mulungu wathu, pakuti adzamukhululukira koposa.
8 Jer misli moje nijesu vaše misli, niti su vaši putovi moji putovi, veli Gospod;
“Pakuti maganizo anga siwofanana ndi maganizo anu, ngakhale njira zanu si njira zanga,” akutero Yehova.
9 Nego koliko su nebesa više od zemlje, toliko su putovi moji viši od vaših putova, i misli moje od vaših misli.
“Monga momwe mlengalenga muli kutali ndi dziko lapansi, momwemonso zochita zanga nʼzolekana kutali ndi zochita zanu, ndipo maganizo anga ndi osiyana kutali ndi maganizo anu.
10 Jer kako pada dažd ili snijeg s neba i ne vraæa se onamo, nego natapa zemlju i uèini da raða i da se zeleni, da daje sjemena da se sije i hljeba da se jede,
Monga mvula ndi chisanu chowundana zimatsika kuchokera kumwamba, ndipo sizibwerera komweko koma zimathirira dziko lapansi. Ndipo zimameretsa ndi kukulitsa zomera kenaka nʼkupatsa mlimi mbewu ndi chakudya.
11 Tako æe biti rijeè moja kad izide iz mojih usta: neæe se vratiti k meni prazna, nego æe uèiniti što mi je drago, i sreæno æe svršiti na što je pošljem.
Ndi mmenenso amachitira mawu ochokera mʼkamwa mwanga. Sadzabwerera kwa Ine kopanda phindu lake, koma adzachita zonse zimene ndifuna, ndipo adzakwaniritsa cholinga chimene ndinawatumira.
12 Jer æete s veseljem izaæi, i u miru æete biti voðeni; gore i bregovi pjevaæe pred vama od radosti, i sva æe drveta poljska pljeskati rukama.
Inu mudzatuluka mu mzindawo mwachimwemwe ndipo adzakutsogolerani mwamtendere; mapiri ndi zitunda zidzakuyimbirani nyimbo, ndipo mitengo yonse yamʼthengo idzakuwombereni mʼmanja.
13 Mjesto trnja niknuæe jela, mjesto koprive niknuæe mirta; i to æe biti Gospodu u slavu, za vjeèan znak, kojega neæe nestati.
Mʼmalo mʼmene tsopano muli mitengo ya minga mudzamera mitengo ya payini, ndipo kumene kuli mkandankhuku kudzamera mchisu. Zimenezi zidzakhala chikumbutso cha Yehova, ngati chizindikiro chamuyaya, chimene sichidzafafanizika konse.”