< لُوکَح 15 >

تَدا کَرَسَنْچایِنَح پاپِنَشْچَ لوکا اُپَدیشْکَتھاں شْروتُں یِیشوح سَمِیپَمْ آگَچّھَنْ۔ 1
Tsopano amisonkho ndi “ochimwa” ankasonkhana kudzamvera mawu ake.
تَتَح پھِرُوشِنَ اُپادھْیایاشْچَ وِوَدَماناح کَتھَیاماسُح ایشَ مانُشَح پاپِبھِح سَہَ پْرَنَیَں کرِتْوا تَیح سارْدّھَں بھُںکْتے۔ 2
Koma Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo amangʼungʼudza nati, “Munthu uyu amalandira ochimwa ndi kudya nawo.”
تَدا سَ تیبھْیَ اِماں درِشْٹانْتَکَتھاں کَتھِتَوانْ، 3
Ndipo Yesu anawawuza fanizo ili:
کَسْیَچِتْ شَتَمیشیشُ تِشْٹھَتْمُ تیشامیکَں سَ یَدِ ہارَیَتِ تَرْہِ مَدھْییپْرانْتَرَمْ ایکونَشَتَمیشانْ وِہایَ ہارِتَمیشَسْیَ اُدّیشَپْراپْتِپَرْیَّنَتَں نَ گَویشَیَتِ، ایتادرِشو لوکو یُشْماکَں مَدھْیے کَ آسْتے؟ 4
“Tiyerekeze kuti mmodzi mwa inu ali ndi nkhosa 100 ndipo imodzi yatayika, kodi iye sangasiye 99 zija kutchire ndi kupita kukafuna yotayikayo mpaka atayipeza?
تَسْیودّیشَں پْراپْیَ ہرِشْٹَمَناسْتَں سْکَنْدھے نِدھایَ سْوَسْتھانَمْ آنِییَ بَنْدھُبانْدھَوَسَمِیپَواسِنَ آہُویَ وَکْتِ، 5
Ndipo iye akayipeza, amayinyamula pa phewa lake mwachimwemwe
ہارِتَں میشَں پْراپْتوہَمْ اَتو ہیتو رْمَیا سارْدّھَمْ آنَنْدَتَ۔ 6
ndi kupita kwawo. Kenaka amayitana anzake ndi anansi pamodzi, ndi kuti, ‘Kondwerani nane; ine ndayipeza nkhosa yanga yotayika ija.’
تَدْوَدَہَں یُشْمانْ وَدامِ، ییشاں مَنَحپَراوَرْتَّنَسْیَ پْرَیوجَنَں ناسْتِ، تادرِشَیکونَشَتَدھارْمِّکَکارَنادْ یَ آنَنْدَسْتَسْمادْ ایکَسْیَ مَنَحپَرِوَرْتِّنَح پاپِنَح کارَناتْ سْوَرْگے دھِکانَنْدو جایَتے۔ 7
Ine ndikukuwuzani kuti momwemonso kudzakhala chikondwerero chachikulu kumwamba chifukwa cha wochimwa mmodzi amene watembenuka mtima kusiyana ndi anthu olungama 99 amene ali otembenuka mtima kale.”
اَپَرَنْچَ دَشاناں رُوپْیَکھَنْڈانامْ ایکَکھَنْڈے ہارِتے پْرَدِیپَں پْرَجْوالْیَ گرِہَں سَمّارْجْیَ تَسْیَ پْراپْتِں یاوَدْ یَتْنینَ نَ گَویشَیَتِ، ایتادرِشِی یوشِتْ کاسْتے؟ 8
“Kapena tiyeni tifanizire mayi amene anali ndi ndalama zasiliva khumi ndipo imodzi nʼkutayika, kodi sayatsa nyale ndi kusesa mʼnyumba ndi kufuna mosamalitsa mpaka atayipeza?
پْراپْتے سَتِ بَنْدھُبانْدھَوَسَمِیپَواسِنِیراہُویَ کَتھَیَتِ، ہارِتَں رُوپْیَکھَنْڈَں پْراپْتاہَں تَسْمادیوَ مَیا سارْدّھَمْ آنَنْدَتَ۔ 9
Ndipo pamene wayipeza, amayitana anzake, ndi anansi pamodzi nati, ‘Kondwerani nane; ine ndayipeza ndalama yanga yotayika ija.’
تَدْوَدَہَں یُشْمانْ وْیاہَرامِ، ایکینَ پاپِنا مَنَسِ پَرِوَرْتِّتے، اِیشْوَرَسْیَ دُوتاناں مَدھْییپْیانَنْدو جایَتے۔ 10
Momwemonso, Ine ndikukuwuzani kuti angelo a Mulungu amakondwera kwambiri chifukwa cha wochimwa mmodzi amene watembenuka mtima.”
اَپَرَنْچَ سَ کَتھَیاماسَ، کَسْیَچِدْ دْوَو پُتْراواسْتاں، 11
Yesu anapitiriza kunena kuti, “Panali munthu amene anali ndi ana aamuna awiri.
تَیوح کَنِشْٹھَح پُتْرَح پِتْرے کَتھَیاماسَ، ہے پِتَسْتَوَ سَمْپَتّیا یَمَںشَں پْراپْسْیامْیَہَں وِبھَجْیَ تَں دیہِ، تَتَح پِتا نِجاں سَمْپَتِّں وِبھَجْیَ تابھْیاں دَدَو۔ 12
Wamngʼonoyo anati kwa abambo ake, ‘Abambo, patseni gawo langa la chuma chanu.’ Ndipo iye anawagawira awiriwo chuma chawo.
کَتِپَیاتْ کالاتْ پَرَں سَ کَنِشْٹھَپُتْرَح سَمَسْتَں دھَنَں سَںگرِہْیَ دُورَدیشَں گَتْوا دُشْٹاچَرَنینَ سَرْوّاں سَمْپَتِّں ناشَیاماسَ۔ 13
“Pasanapite nthawi, wamngʼonoyo anasonkhanitsa chuma chake chonse, napita ku dziko lakutali ndipo kumeneko anayamba kumwaza chuma chake mʼnjira zachitayiko.
تَسْیَ سَرْوَّدھَنے وْیَیَں گَتے تَدّیشے مَہادُرْبھِکْشَں بَبھُووَ، تَتَسْتَسْیَ دَینْیَدَشا بھَوِتُمْ آریبھے۔ 14
Iye atawononga zonse, kunagwa njala yoopsa mʼdziko lonselo ndipo anayamba kusauka.
تَتَح پَرَں سَ گَتْوا تَدّیشِییَں گرِہَسْتھَمیکَمْ آشْرَیَتَ؛ تَتَح سَتَں شُوکَرَوْرَجَں چارَیِتُں پْرانْتَرَں پْریشَیاماسَ۔ 15
Iye anapita kwa nzika ina ya dzikolo nakakhala naye ndi kumagwira ntchito, amene anamutumiza ku munda kukadyetsa nkhumba.
کیناپِ تَسْمَے بھَکْشْیاداناتْ سَ شُوکَرَپھَلَوَلْکَلینَ پِچِنْڈَپُورَناں وَوانْچھَ۔ 16
Iye analakalaka atakhutitsa mimba yake ndi makoko amene nkhumbazo zinkadya, koma panalibe wina amene anamupatsa kanthu.
شیشے سَ مَنَسِ چیتَناں پْراپْیَ کَتھَیاماسَ، ہا مَمَ پِتُح سَمِیپے کَتِ کَتِ ویتَنَبھُجو داسا یَتھیشْٹَں تَتودھِکَنْچَ بھَکْشْیَں پْراپْنُوَنْتِ کِنْتْوَہَں کْشُدھا مُمُورْشُح۔ 17
“Maganizo ake atabweramo, iye anati, ‘Ndi antchito angati a abambo anga amene ali ndi chakudya chimene amadya nʼkutsalako ndipo ine ndili pano kufa ndi njala!
اَہَمُتّھایَ پِتُح سَمِیپَں گَتْوا کَتھامیتاں وَدِشْیامِ، ہے پِتَرْ اِیشْوَرَسْیَ تَوَ چَ وِرُدّھَں پاپَمَکَرَوَمْ 18
Ine ndinyamuka ndi kubwerera kwa abambo anga ndipo ndikati kwa iwo: abambo, ine ndachimwira kumwamba ndi kwa inu.
تَوَ پُتْرَاِتِ وِکھْیاتو بھَوِتُں نَ یوگْیوسْمِ چَ، ماں تَوَ وَیتَنِکَں داسَں کرِتْوا سْتھاپَیَ۔ 19
Ndine wosayeneranso kutchedwa mwana wanu; munditenge ngati mmodzi wa antchito anu.’
پَشْچاتْ سَ اُتّھایَ پِتُح سَمِیپَں جَگامَ؛ تَتَسْتَسْیَ پِتاتِدُورے تَں نِرِیکْشْیَ دَیانْچَکْرے، دھاوِتْوا تَسْیَ کَنْٹھَں گرِہِیتْوا تَں چُچُمْبَ چَ۔ 20
Ndipo iye ananyamuka ndi kupita kwa abambo ake. “Koma iye akanali patali, abambo ake anamuona ndipo anamvera chisoni; anathamangira mwanayo, namukumbatira ndi kupsompsona.
تَدا پُتْرَ اُواچَ، ہے پِتَرْ اِیشْوَرَسْیَ تَوَ چَ وِرُدّھَں پاپَمَکَرَوَں، تَوَ پُتْرَاِتِ وِکھْیاتو بھَوِتُں نَ یوگْیوسْمِ چَ۔ 21
“Mwanayo anati, ‘Abambo, ine ndachimwira kumwamba ndi inunso. Ine sindiyenera konse kutchedwa mwana wanu.’
کِنْتُ تَسْیَ پِتا نِجَداسانْ آدِدیشَ، سَرْوّوتَّمَوَسْتْرانْیانِییَ پَرِدھاپَیَتَینَں ہَسْتے چانْگُرِییَکَمْ اَرْپَیَتَ پادَیوشْچوپانَہَو سَمَرْپَیَتَ؛ 22
“Koma abambowo anati kwa antchito ake, ‘Fulumirani! Bweretsani mkanjo wabwino kwambiri ndipo mumuveke. Muvekeni mphete ndi nsapato.
پُشْٹَں گووَتْسَمْ آنِییَ مارَیَتَ چَ تَں بھُکْتْوا وَیَمْ آنَنْدامَ۔ 23
Bweretsani mwana wangʼombe wonenepa ndipo iphani. Tiyeni tikhale ndi phwando ndi kukondwerera.
یَتو مَمَ پُتْرویَمْ اَمْرِیَتَ پُنَرَجِیوِیدْ ہارِتَشْچَ لَبْدھوبھُوتْ تَتَسْتَ آنَنْدِتُمْ آریبھِرے۔ 24
Pakuti mwana wangayu anali wakufa, ndipo ali ndi moyonso; iye anatayika ndipo wapezeka.’ Chomwecho anayamba kukondwerera.
تَتْکالے تَسْیَ جْییشْٹھَح پُتْرَح کْشیتْرَ آسِیتْ۔ اَتھَ سَ نِویشَنَسْیَ نِکَٹَں آگَچّھَنْ نرِتْیاناں وادْیانانْچَ شَبْدَں شْرُتْوا 25
“Nthawi imeneyi, mwana wake wamkulu uja anali ku munda. Iye atafika pafupi ndi nyumba, anamva anthu akuyimba ndi kuvina.
داسانامْ ایکَمْ آہُویَ پَپْرَچّھَ، کِں کارَنَمَسْیَ؟ 26
Ndipo iye anayitana mmodzi wa antchito, namufunsa chimene chimachitika.
تَتَح سووادِیتْ، تَوَ بھْراتاگَمَتْ، تَوَ تاتَشْچَ تَں سُشَرِیرَں پْراپْیَ پُشْٹَں گووَتْسَں مارِتَوانْ۔ 27
Iye anayankha kuti, ‘Mʼbale wako wabwera ndipo abambo ako apha mwana wangʼombe wonenepa chifukwa wabwera wamoyo ndipo ali bwino.’
تَتَح سَ پْرَکُپْیَ نِویشَنانْتَح پْرَویشْٹُں نَ سَمّینے؛ تَتَسْتَسْیَ پِتا بَہِراگَتْیَ تَں سادھَیاماسَ۔ 28
“Mwana wamkulu anakwiya ndipo anakana kulowa. Chomwecho abambo ake anatuluka ndi kumudandaulira.
تَتَح سَ پِتَرَں پْرَتْیُواچَ، پَشْیَ تَوَ کانْچِدَپْیاجْناں نَ وِلَںگھْیَ بَہُونْ وَتْسَرانْ اَہَں تْواں سیوے تَتھاپِ مِتْرَیح سارْدّھَمْ اُتْسَوَں کَرْتُّں کَداپِ چھاگَمیکَمَپِ مَہْیَں نادَداح؛ 29
Koma iye anayankha abambo ake kuti, ‘Taonani! Zaka zonsezi ndakhala ndikukutumikirani kugwira ntchito yowawa ndipo palibe pamene sindinamvere malamulo anu. Koma inu simunandipatse ngakhale mwana wambuzi kuti ine ndichite phwando ndi anzanga.
کِنْتُ تَوَ یَح پُتْرو ویشْیاگَمَنادِبھِسْتَوَ سَمْپَتِّمْ اَپَوْیَیِتَوانْ تَسْمِنّاگَتَماتْرے تَسْیَیوَ نِمِتَّں پُشْٹَں گووَتْسَں مارِتَوانْ۔ 30
Koma pamene mwana wanu uyu amene wawononga chuma chanu ndi achiwerewere wabwera ku nyumba, inu mwamuphera mwana wangʼombe wonenepa.’”
تَدا تَسْیَ پِتاووچَتْ، ہے پُتْرَ تْوَں سَرْوَّدا مَیا سَہاسِ تَسْمانْ مَمَ یَدْیَداسْتے تَتْسَرْوَّں تَوَ۔ 31
Abambowo anati, “Mwana wanga, iwe umakhala ndi ine nthawi zonse ndipo zonse ndili nazo ndi zako.
کِنْتُ تَوایَں بھْراتا مرِتَح پُنَرَجِیوِیدْ ہارِتَشْچَ بھُوتْوا پْراپْتوبھُوتْ، ایتَسْماتْ کارَنادْ اُتْسَوانَنْدَو کَرْتُّمْ اُچِتَمَسْماکَمْ۔ 32
Koma tinayenera kukondwera ndi kusangalala, chifukwa mʼbale wako uyu anali wakufa ndipo ali ndi moyonso; iye anali wotayika ndipo wapezeka.”

< لُوکَح 15 >