< Matthew 12 >
1 Sûn sôtbâkloi suolechu Sabbathnin Jisua bubilngeia a lôna. A ruoisingei an von achâma, masikin buvûingei chinin an chipa.
Pa nthawi imeneyo Yesu anadutsa pakati pa minda ya tirigu pa tsiku la Sabata. Ophunzira ake anamva njala nayamba kuthyola ngala za tirigu nʼkumadya.
2 Phariseengeiin an mu'n chu, Jisua kôm, “En ta, Sabbathnia nu ruoisingeiin an tho hih ei Balamin ai khap ani!” an tia.
Afarisi ataona zimenezi anati kwa Iye, “Taonani! Ophunzira anu akuchita zosaloledwa pa tsiku la Sabata.”
3 Jisua'n an kôm, “David le a mingeiin an vonchâm lâia an tho hah nin la pore tet ngâiloi mo?
Iye anayankha kuti, “Kodi simunawerenge zimene anachita Davide pamene iye ndi anzake anamva njala?
4 Ama hah Pathien ina a lûta, ama le a mingeiin Pathien kôma pêksai vâipôl, an sâk ranga Balamin ai khap ochaingei vaiin an sâk ranga phala omngâi vâipôl hah an sâk ani.
Analowa mʼNyumba ya Mulungu, ndipo iye ndi anzakewo anadya buledi wopatulika amene sikunali kololedwa kwa iwo kudya koma ansembe okha.
5 Aninônchu, adiktakin Sabbathni racham ochai Biekina omngâi ngeiin Sabbathni balam an minchâi ngâia, hannoma, theiloiintum ngâi mak ngei ti Moses Balam lekhabu nin la pore loi mo?
Kodi simunawerenge mʼmalamulo kuti pa Sabata ansembe mʼNyumba ya Mulungu amaphwanya lamulo la Sabata komabe sawayesa olakwa?
6 Nangni ki ril, mahin neinun imini Biekin nêka roiinpui uol aom.
Ine ndikuwuzani kuti wamkulu kuposa Nyumba ya Mulunguyo ali pano.
7 Pathien lekhabu'n, ‘Inbôlna nuom mu-unga moroina kêng ku nuom,’ ai ti hih a omtie nin riet minthâr tatak nisenla chu minchâinaboi mingei hah theiloi mintum no tunui;
Ngati mukanadziwa zomwe mawu awa atanthauza, ‘Ine ndifuna chifundo osati nsembe,’ inu simukanatsutsa osalakwa.
8 Miriem Nâipasal hih Sabbathni Pumapa ani sikin,” a tia.
Pakuti Mwana wa Munthu ndiye Mbuye wa Sabata.”
9 Jisua'n ha mun hah mâkin synagog ina a lûta,
Atachoka kumeneko anakalowa mʼsunagoge mwawo.
10 mahan mi inkhat kut phalkhatthi alei oma. Mi senkhat Jisua a tho minchâi tia nôn nuom ngei an lei om sa, masikin anni han a kôm, “Sabbathnia mi mindam hih ei Balamin a khap mo?” tiin an rekela.
Ndipo mʼmenemo munali munthu wolumala dzanja. Pofuna chifukwa chokamunenezera, iwo anamufunsa Yesu kuti, “Kodi nʼkololedwa kuchiritsa munthu tsiku la Sabata?”
11 Jisua'n an kôm, “Nin lâia tumakhatin belri inkhat dôn senla male Sabbathni han khur inthûka tâk pe senla, juong rûtin nin kelsuo loi rang mo?
Iye anawawuza kuti, “Ngati wina wa inu ali ndi nkhosa nigwera mʼdzenje tsiku la Sabata, kodi simudzayigwira ndi kuyitulutsa kunja?
12 Miriem chu belri nêkin a lut uol ok ani! Masikin, Sabbathnia tumini san rangin ei Balamin mi phal ani,” tiin a thuona.
Nanga munthu sali oposa nkhosa kwambiri! Chifukwa chake nʼkololedwa kuchita zabwino pa Sabata.”
13 Male kut phalkhatthipa kôm han, “Nu kut phar roh,” a tipea. A kut a phara, kângkhat tienga angin a hong dam phar zoi.
Pamenepo Yesu anati kwa munthuyo, “Wongola dzanja lako.” Iye analiwongola ndipo linakhala monga linalili kale.
14 Hanchu Phariseengei hah an rota male Jisua that rangtie an mintuo zoi.
Koma Afarisi anatuluka kunja ndi kukonza njira yoti amuphere.
15 An that rangtie an phan chungroi hah Jisua'n a rietin chu ha mun renga hah a rota; lokongeiin a nûk an jûi zoi. Damloi ngei murdi a mindam ngeia
Podziwa zimenezi, Yesu anachoka kumalo amenewo. Ambiri anamutsata Iye ndipo anachiritsira odwala awo onse
16 male ama chungroi tute kôm misîr loi rangin chong a pêk ngeia.
nawachenjeza kuti asamuwulule kuti yani.
17 Masikin, Pathien'n dêipu Isaiah kôma alei ti hah ajuong tung adik theina rangin mahi a tho ani:
Uku kunali kukwaniritsa zimene zinayankhulidwa kudzera mwa mneneri Yesaya kuti,
18 “Mahi ki tîrlâm, ka thangsaipu hah, ku lungkhampu, le a chunga ku mulungtâiriempu hah ani. A chunga ka ratha tîr ka ta, male ama'n namtinngei kôm ko roijêkna phuong a tih.
“Taonani mnyamata wanga amene ndinamusankha, Wokondedwa wanga, amene moyo wanga ukondwera naye. Pa Iye ndidzayika Mzimu wanga, ndipo Iye adzalalikira chiweruzo kwa akunja.
19 Ama chu makhal nonia, hanchu in-iek uol nonia; aninônchu lamlienngeia khom ruhulum tho noni.
Sadzalimbana, sadzafuwula, ngakhale mmodzi sadzamva mawu ake mʼmakwalala.
20 Ama'n sûl ânkûichara om hah khiekpai nonia, hanchu châti athi vavâng hah khom thatrip no nih. Roijêkdikna han a zoi mâka chu khan tit a ta,
Bango lophwanyika sadzalithyola, ndi nyale yofuka sadzayizimitsa, kufikira Iye adzatumiza chiweruziro chikagonjetse.
21 male mingei murdi'n ama chunga han an sabeina minngam an tih.”
Ndipo akunja adzakhulupirira dzina lake.”
22 Hanchu mi senkhat ngeiin Jisua kôm han mi inkhat a mitcho le ramkhori sûr sikin chong theiloi an hong tuonga. Jisua'n ama hah a mindama, masikin ama hah a chong theia, a mu thei zoi ani.
Pomwepo anthu anabwera naye kwa Yesu munthu wogwidwa ndi chiwanda amene anali wosaona ndi wosamva ndipo Yesu anamuchiritsa kotero kuti atatha anayamba kumva ndi kuona.
23 Jisua sintho hah lokongei murdi'n an kamâm sabaka, “Ama hih David Nâipasal ni thei ni mo?” tiin an rekela.
Anthu onse anadabwa ndipo anati, “Kodi uyu ndi kukhala mwana wa Davide?”
24 Maha Phariseengeiin an rietin chu, “Hi mi hin ramkhoringei a rujûl theina chu an rêngpa Beelzebul'n ranak a pêk sikin ani,” tiin chong an mele.
Koma Afarisi atamva zimenezi, anati, “Uyu amatulutsa ziwanda ndi mphamvu ya Belezebabu mkulu wa ziwandazo.”
25 Jisua'n imo an mindon hah a rieta, masikin an kôm, “Kho ram khom apâlpâlin an insema an indoi inlômin chu sôi ngâi mak. Kho khopui khom, aninônchu insûngmingei khom apâlpâlin an insenna an indoi inlômin chu an inlet rang ani.
Yesu anadziwa maganizo awo ndipo anawawuza kuti, “Ufumu uliwonse ukagawanika mwa iwo udzawonongeka ndi mzinda uliwonse kapena banja likagawanika, mwa izo zokha sizidzayima.
26 Masikin soitan rama khom pâl khatin pâl dang an doiin chu, pâl an insen tina nîng ata, male ânlet kelen rang ani!
Ngati Satana atulutsa Satana, iye adzigawa yekha. Nanga ufumu wake ungayime bwanji?
27 Beelzebul'n ranak ni pêk sikin ramkhori ngei ku rujûl thei nin tia. Asa, nônchu, nin nûkjûi ngei hah tumo ranak a pêk ngeia anni ngei han an rujûlpai ngâi? Nin nûkjûingei nanâkin an lei tho ngâi han nin tho minchâina a minlang ani!
Ndipo ngati Ine nditulutsa ziwanda ndi Belezebule, anthu anu amatulutsa ziwandazo ndi chiyani? Potero tsono adzakhala oweruza anu.
28 Nimak, mahi Beelzebul nimaka, Pathien Ratha kêng ramkhori rujûlpai theina ranak ni pêk, mahin Pathien Rêngram nin kôm a juong tung zoi ti a minlang ani.
Koma ngati Ine ndimatulutsa ziwanda ndi Mzimu wa Mulungu, pamenepo ufumu wa Mulungu wafika pa inu.
29 “Tutên mi rât ina lûtin a neinunngei lâk pe thei no nih, mi rât hah a khit bak nônchu; hanchu a in hah minram pe thei a tih.
“Kapenanso wina aliyense angathe bwanji kulowa mʼnyumba ya munthu wamphamvu ndi kunyamulamo zinthu zake, sipokhapo atayamba wamanga munthu wa mphamvuyo? Pamenepo iye akhoza kuba mʼnyumbamo.
30 “Tutu keima ranga niloi kai chu atatakin mi doi ani; tutu a mintûp ni sanloipu chu ataktakin chekaminchâi ani.
“Iye amene sali ndi Ine atsutsana nane ndipo iye amene sasonkhanitsa pamodzi ndi Ine amamwaza.
31 Masikin nangni ki ril, mingei an sietna murdi le Pathien doia asaloi an ti ngei murdi chu ngâidam thei nîng ata; aniatachu, Ratha Inthieng doia asaloi an ti ngei chu ngâidam nino nih.
Ndipo potero Ine ndikuwuzani inu, tchimo lililonse ndi cha mwano chilichonse zidzakhululukidwa kwa anthu koma chamwano cha pa Mzimu Woyera, sichidzakhululukidwa.
32 Tutu Miriem Nâipasal doia asaloi an ti ngei chu ngâidam thei nîng ata; aniatachu, tutu Ratha Inthieng doia asaloi an ti ngei chu atûn le tuonsôtin ngâidam nino nih. (aiōn )
Aliyense amene anena mawu otsutsana ndi Mwana wa Munthu adzakhululukidwa koma aliyense wonena motsutsana ndi Mzimu Woyera sadzakhululukidwa mu mʼbado uno kapena umene ukubwerawo. (aiōn )
33 “Mara sa dôn rangin chu thingkung adam nin dôn ngêt anâng; thingkung damloi nin dônin chu mara saloi dôn nin tih. Thingkung chu a marân riet thei ani.
“Mtengo wabwino umabala zipatso zabwino ndipo mtengo woyipa umabalanso zipatso zoyipa, pajatu mtengo umadziwika ndi zipatso zake.
34 Murûlngei nangni asaloi lei ni chienin kho-angin mo chongsa nin tho thei ranga? Mulung sûnga sipa liem hah kêng bâiin ai suo ngâi ani.
Ana anjoka inu, woyipa inu, mungathe bwanji kuyankhula kanthu kalikonse kabwino? Pakuti pakamwa pamayankhula zosefuka kuchokera mu mtima.
35 Mi sân a rochonkok renga neinun sa a kaisuo ngâia; mi saloiin chu a rochonkoka neinun saloi a kaisuo ngâi.
Munthu wabwino amatulutsa zinthu zabwino zomwe zili mumtima mwake ndipo munthu woyipa amatulutsanso zinthu zoyipa zomwe zili mwa iye.
36 “Nangni ki ril, Roijêk Nikhuon chu mitinin chongkâmboi an tho ngei hah la misîr let an tih.
Ine ndikukuwuzani kuti pa tsiku la chiweruziro munthu adzazengedwa mlandu chifukwa cha mawu aliwonse wopanda pake amene anayankhula.
37 Minchâinaboi mo ni ni aninônchu theiloiintum mo ni ni minthârna rangin no chongngei hah mangin nu chungroi jêk nîng atih.”
Pakuti ndi mawu anu mudzapezeka osalakwa ndiponso ndi mawu anu mudzapezeka olakwa.”
38 Hanchu Balam minchupu senkhat le Pharisee senkhat ngeiin a kôm, “Minchupu, sininkhêl no tho mu rang kin nuom,” an tia.
Pamenepo ena mwa Afarisi ndi aphunzitsi amalamulo anati kwa Iye, “Aphunzitsi, tikufuna tione chizindikiro chodabwitsa kuchokera kwa Inu.”
39 Jisua jâminzalin an kôm, “Atûnlâia mingei idôrtaka saloi le Pathien dônloi mo nin ni zoi!” Sininkhêl tho rangin mi nin ngêna? Nimak! Dêipu Jonah sininkhêl tho tiloiin chu sininkhêl dang nangni pêk ni no nih.
Iye anayankha kuti, “Mʼbado woyipa ndi wachigololo ufunsa za chizindikiro chodabwitsa! Koma ndi chimodzi chomwe sichidzapatsidwa kwa inu kupatula chizindikiro cha mneneri Yona.
40 Jonah hah sûnthum jân thum ngapui vonsûnga a oma, ma angdên han Miriem Nâipasal hih sûnthum jân thum pil inthûk sûnga aom rang ani.
Pakuti monga Yona anali mʼmimba mwa nsomba yayikulu masiku atatu, usana ndi usiku, momwemonso Mwana wa Munthu adzakhala masiku atatu, usana ndi usiku, mʼkati mwa nthaka.
41 Roijêk Nikhuon chu Nineveh mingei hah inding an ta, nangni nôn an tih; anni chu Jonah thurchi misîr an rieta; an sietnangei renga an inhei sikin; male nangni ki ril, Jonah nêka lien uol mahin aom!
Anthu a ku Ninive adzayimirira pachiweruzo ndi mʼbado uwu ndi kuwutsutsa pakuti iwo analapa Yona atalalikira ndipo tsopano wamkulu kuposa Yona ali pano.
42 Roijêk Nikhuon chu Rêngnu Sheba hah inding a ta, nangni nôn a tih, Rêng Solomon vâr minchûna rangâi rangin a ram latak renga a hong sikin; adiktakin nangni ki ril, Solomon nêka lien uol mahin aom!
Mfumu yayikazi yakummwera idzayimirira pa tsiku lachiweruzo ndi mʼbado uwu ndipo idzawutsutsa pakuti inachokera kumathero a dziko lapansi kudzamva nzeru za Solomoni, ndipo pano pali woposa Solomoni.
43 “Ratha saloi hah mi sûng renga a jôkin chu inngâmna mun rokin tui boina rama a chai titira, aman loi tika chu,
“Pamene mzimu woyipa utuluka mwa munthu, umadutsa malo wopanda madzi kufunafuna malo opumulira ndipo suwapeza.
44 ‘ki ina kîr nôk ki tih’ a tia. Hanchu a kîr nôka, a in atongrieiin, phiet minsâivarin, le cherêl irin ava mua.
Pamenepo umati, ‘Ndidzabwerera ku nyumba yanga komwe ndinatuluka.’ Pamene ufika, upeza mopanda kanthu, mosesedwa ndi mokonzedwa bwino.
45 Hanchu, a jôkpaia ratha dang sari ama nêka puoloi uol a hong tuong ngeia, mahan an lûta, an om zoi. Masuole chu ha miriem nunchan hah aphuta nêkin a puoloi uol ok zoi. Hima ang hin atûnlâia mi saloi ngei chunga ala tung rang ani,” a tia.
Kenaka umapita kukatenga mizimu ina isanu ndi iwiri yoyipa kwambiri kuposa uwowo ndipo imapita ndi kukakhala mʼmenemo. Choncho khalidwe lotsiriza la munthu uyu limakhala loyipa kwambiri kuposa loyambalo. Umo ndi mmene zidzakhalire ndi mʼbado oyipawu.”
46 Mipui ngei kôm han Jisua ala chong lâitakin, a nû le lâibungngei an hong tunga. Ama chongpui nuomin, pêntieng an indinga.
Pamene Yesu anali kuyankhulabe ndi gulu la anthu, amayi ndi abale ake anayimirira kunja, akufuna kuyankhulana naye.
47 Masikin ha muna mi inkhatin a kôm, “En ta, nu nû le na lâibungngei nang chongpui rang an nuoma pêntieng nang an ngâk,” a ti pea.
Wina anamuwuza Iye kuti, “Amayi ndi abale anu ayima kunjaku akufuna kuyankhulana nanu.”
48 Jisua'n a kôm, “Tumo ku nû? Tumo ka lâibungngei?” tiin a thuona.
Iye anayankha kuti, “Amayi anga ndani ndipo abale anga ndi ndani?”
49 Male a ruoisingei tieng a khînna, “En roi! Hi ngei hih ku nû le ka lâibungngei an ni!
Ndipo akuloza ophunzira ake, Iye anati, “Awa ndiwo amayi anga ndi abale anga.
50 Tutu invâna Ka Pa lungdo sinngei hih ka lâibungngei, ka sarnungei, ku nû ngei an ni,” a tia.
Pakuti aliyense amene achita chifuniro cha Atate anga akumwamba ndiye mʼbale wanga, mlongo wanga ndi amayi anga.”