< Mark 4 >
1 Galilee dîl kôla Jisua'n a minchu nôka, mipuingei a kôma juong intûp ngei hah an tam rai sikin rukuonga a chuonga, ânsunga, mipuingei hah chu tui rakham asortea tânga han an indinga.
Nthawi inanso Yesu atakhala mʼmbali mwa nyanja, anayamba kuphunzitsa. Gulu lalikulu la anthu linasonkhana momuzungulira kotero kuti Iye analowa mʼbwato lomwe linali pa nyanja nakhalamo, anthu onse ali pa mtunda mʼmbali mwa madzi.
2 Anni ngei minchuna rangin chongmintêkngei mangin neinun tamtak ngei a misîr pe ngeia, an kôm han:
Anawaphunzitsa zinthu zambiri mʼmafanizo, ndipo mʼchiphunzitso chake anati:
3 “Rangâi roi! voikhat chu mi inkhatin burît rangin a sea.
“Tamverani! Mlimi anapita kukafesa mbewu zake.
4 Loia han sachi a rethea, senkhat lampui kôla achula, vângei an honga male an sâk ripa.
Akufesa, mbewu zina zinagwera mʼmbali mwa njira, ndipo mbalame zinabwera ndi kuzidya.
5 Senkhat lungpherpha pil ânphâna chunga achula, pil ânphân sikin ahong mông kelena,
Zina zinagwa pa malo a miyala pamene panalibe dothi lambiri. Zinamera mofulumira chifukwa panalibe dothi lambiri.
6 Hanchu, nisa ahong insângin chu akung innoinar ngei ha a em minjuota, aruzung amathâk hah ânthûk loi sikin akângrip kelena.
Koma dzuwa litakwera, mbewuzo zinapserera, ndipo zinawuma chifukwa zinalibe mizu.
7 Senkhat chu riling kâra achula, riling han akungngei ha adîpa, male inra thei khâi mak ngei.
Mbewu zina zinagwa pa minga, ndipo mingayo inayanga ndi kuzirepheretsa kukula.
8 Aniatachu senkhat chu pil sana achula, akungngei ahong kêia, ahong insôna, avûia: senkhat sômthumin, senkhat sômrukin, male senkhat raza khatin ahong pung zoi” a tia.
Mbewu zinanso zinagwa pa nthaka yabwino ndipo zinamera, zinakula ndi kubereka zipatso, zina zochuluka makumi atatu, zina makumi asanu ndi limodzi ndi zina 100.”
9 Male Jisua'n a chongkharnân an kôm “Kuor nin dônin chu rangâi roi!” a tipe ngeia.
Pamenepo Yesu anati, “Amene ali ndi makutu akumva, amve.”
10 Jisua athenin aom lehan, a ruoisingei sômleinik le midang senkhat ngei ma chong riet ngei han a kôm an honga male ha chongmintêkngei hah rilminthâr pe ngei rangin an ngêna.
Ali yekha, ophunzira ndi ena omuzungulira, anamufunsa za mafanizo.
11 Jisua'n an kôm, “Pathien Rêngram chonginthup riettheina nin kôm pêk ani zoi.” Hannirese, “Midangngei pêntienga omngei rangin chu, neinunngei murdi chongmintêkngei vaiin misîr pe an nia,
Iye anawawuza kuti, “Chinsinsi cha ufumu wa Mulungu chapatsidwa kwa inu. Koma kwa amene ali kunja zinthu zonse zinenedwa mʼmafanizo:
12 ‘Masikin an en, an en khomin an mu loina rangin le; an rangâi an rangâi khomin, an rietthei loina rangin. Ma anghan an thôn chu, Pathien tieng inhei nôk an ta, male ama'n lei ngâidam ngei thei atih’” a tia.
kotero kuti, “‘Kupenya mudzapenya koma osaona kanthu, kumva mudzamva koma osamvetsetsa, kuti mwina angatembenuke ndi kukhululukidwa!’”
13 Hanchu Jisua'n an kôm, “Hi chongmintêk hih nin rietthei loi mo? Hanchu, kho angin mo chongmintêk dangngei ngân khom nin rietthei ranga?
Pamenepo Yesu anawawuza kuti, “Kodi simukulimvetsa fanizoli? Kodi nanga mudzazindikira bwanji fanizo lina lililonse?
14 Sachirethêpa han Pathien chong a rethe ngâi.
Wofesa amafesa mawu.
15 Mi senkhat ngei chu, sachi lampui kôla chul angin an nia; chong hah an riet harenghan, Soitan a honga an mulungrîla om hah a lâk pe ngei ngâi.
Anthu ena ali ngati mbewu za mʼmbali mwa njira, mʼmene mawu amafesedwamo. Akangowamva, Satana amabwera ndi kuchotsa mawu amene anafesedwa mwa iwo.
16 Midang senkhat ngei chu sachi lungpherpha chunga chul angin an ni. Thurchi hah an riet harenghan, râisântakin an pom kelen ngâia.
Ena, monga mbewu zofesedwa pa miyala, amamva mawu ndipo nthawi yomweyo amawalandira ndi chimwemwe.
17 Hannirese, ruzung inthûk an mathâk loi sikin om sôt ngâi maka. Thurchi sika intakna mini nuomlona mini, ahong om lehan chu anin let nôk kelen ngâi.
Koma popeza alibe mizu, amakhala kwa kanthawi kochepa. Mavuto kapena masautso akafika chifukwa cha mawu, amagwa mofulumira.
18 Mi senkhat ngei chu sachi riling kâra achul angin an ni. Ma ngei hah chu thurchi rangâipu ngei hah an nia,
Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu;
19 aniatachu an ringnuna kângdoinangei, rammuol hoina le neinangei le jât dadang an ôinangei ahong lûta chong hah adîpa, amara musuo ngâi mak. (aiōn )
koma nkhawa zamoyo uno, chinyengo cha chuma ndi zokhumba za zinthu zina zimabwera ndi kutchinga mawu, ndipo amawachititsa kukhala osabala chipatso. (aiōn )
20 Hannirese mi senkhat ngei chu pil asana achul ngei angin an ni. Chong hah an rieta, an poma, male ânra ngâi: senkhat sômthumin, senkhat sômrukin, senkhat raza khatin an hong pung zoi, a tia.”
Ena, ngati mbewu zofesedwa pa nthaka yabwino, amamva mawu, nawalandira, ndi kubereka zipatso zokwanira makumi atatu, makumi asanu ndi limodzi, kapena ngakhale 100 kuwonjezera pa zomwe zinafesedwa.”
21 Jisua'n a chong a la zombanga, “Tumo châti hongchôia adarna muna dar loiin, bêl nuoia mo, aninônchu jâlmun nuoia mini a dar ngâia? adarna munna ke an va dar ngâi nimak mo?
Iye anawawuza kuti, “Kodi umatenga nyale ndi kuyiika pansi pa mbiya kapena pansi pa bedi? Mʼmalo mwake, kodi simuyika pa choyikapo chake?
22 Ânthup murdi tâng la musuo nîng a ta, hîpa om ngei murdi lîkpai la nîng atih.
Pakuti chilichonse chobisika chidzayenera kuwululika, ndi chilichonse chachinsinsi chidzayenera kuonekera poyera.
23 Hanchu, kuor nin dônin chu rangâi roi!” a tia.
Ngati wina ali ndi makutu akumva, amve.”
24 Hanchu Jisua nanâkin an kôm, “Nin chong rangâi hih asadimin mindon roi! Midangngei nin jêkna balamngei nanâk hah Pathien'n nangni jêkna rangin mang a tih, manêkin nangni min rik pe uol a tih.
Anapitiriza nati, “Ganizirani mosamala zimene mukumva, ndi muyeso umene mugwiritsa ntchito, mudzayesedwa nawo, ndipo ngakhale kwambiri.
25 Tu tukhom imini dônpu ngei chu bôk pêk sa nîng a ta, male tukhom ite dôn loi ngei chu an dôn viette khom ha lâk pe rip nîng atih,” a tia.
Amene ali nazo adzapatsidwa zochuluka; amene alibe, ngakhale zimene ali nazo zidzachotsedwa kwa iwo.”
26 Jisua'n thurchi a la misîr banga, an kôm, “Pathien Rêngram chu hi anghin ani.” Mi inkhatin a loia chimu a rethea.
Iye anatinso, “Umu ndi mmene ulili ufumu wa Mulungu. Munthu amafesa mbewu mʼnthaka.
27 Hanchu a sea, a van ngama jânna a inna, ânthoia sûn ngei ha a va manga, a riet loi kârin chimu hah ahong kêia, ahong insôn zoia.
Usiku ndi usana, kaya agona kapena adzuka, mbewu imamera ndi kukula, ngakhale sadziwa mmene zimachitikira.
28 Pil ha athenin akungngei hah aminsôna, amara amin dôna; amotona akung ahong inlang ngâi, hanchu avûia, male anûktaka aramala sip buvûi ahong oma.
Nthaka pa yokha imatulutsa mbewu, umayamba mʼmera, kenaka ngala, kenaka mbewu yokhwima mʼngalayo.
29 Bu hah amin tena chu, ha mi han ât zora ahong tung zoi sikin a kôite lâkin bu ât aphut ngâi anghan ani, a tia.
Mbewuyo ikangokhwima, amayimweta chifukwa nthawi yokolola yakwana.”
30 Jisua'n an kôm, “Pathien Rêngram hih imo a-ang ei ti rang ân zoi? Khoi chongmintêk mangin mo ei rilminthâr rang ani zoi?
Ndipo anatinso, “Kodi tinene kuti ufumu wa Mulungu ufanana ndi chiyani, kapena ndi fanizo lotani limene tidzagwiritsa ntchito pakuwufotokozera?
31 Mi inkhatin ancham ru rammuola chimu murdi lâia achîntak ramal khat a lâka, pila a tua.
Uli ngati mbewu ya mpiru imene ndi mbewu yayingʼono kwambiri yomwe mumadzala mʼnthaka.
32 Chomolte suole chu ahong mônga, chimu murdi lâia alientak ahongni ngâi. Machang lientak ngei ahong dôna, male vângei an honga male adâilîm han rubungei an phana mahan an riek thei ang ha ani” a tia.
Koma ikadzalidwa, imakula ndi kukhala yayikulu koposa mbewu zina zonse za mʼmunda ndipo mʼnthambi zake zazikulu mbalame zamlengalenga zimadzapuma pa mthunzi wake.”
33 Ma anghin Jisua'n mingei kôm han chongmintêk tamtak mangin, an rietthei rang do-dôrin a thurchi a misîr pe ngei ngâia.
Ndi mafanizo ambiri onga awa Yesu anayankhula mawu kwa iwo, monga mmene akanatha kumvetsa.
34 Chongmintêk niloiin chu an kôm, thurchi misîr ngâi maka; hannirese, a ruoisingei leh vai an om zorân chu jâttin a rilminthâr pe ngei ngâi ani.
Iye sananene kanthu kwa iwo osagwiritsa ntchito fanizo. Koma ali yekha ndi ophunzira ake, ankawatanthauzira zonse.
35 Mani nanâka han kholoi ahongnin chu Jisua'n a ruoisingei kôm, “Dîl râl tieng son vân kân ei ti u” a tia.
Tsiku limenelo atafika madzulo, anawuza ophunzira ake kuti, “Tiyeni tiwolokere tsidya lina.”
36 Masikin lokongei ha an mâka; Jisua a lei insungna rukuonga han ruoisingei hah an lûta, ama khom an tuonga. Mahan rukuong dangngei khom an om sa.
Atasiya gulu la anthu mʼmbuyo, anamutenga Iye, napita naye monga momwe anali mʼbwatolo. Panalinso mabwato ena pamodzi ndi Iye.
37 Inningloi rengin phâivuopui râttak ahong thoa, tuidârinsok khom hah rukuonga a lûta asip vâng zoia.
Mphepo yamkuntho inabuka, ndipo mafunde anawomba bwatolo, kotero kuti linali pafupi kumira.
38 Jisua chu lukham khamin rukuong remei tienga han a lei ina. Ruoisingei han an kaithoia male a kôm, “Minchupu kin thi rang ani zoi, itên ni mindon loi mini?” an tia.
Pa nthawi imeneyi Yesu anali akugona atatsamira pilo kumbuyo kwa bwato. Ophunzira anamudzutsa nati kwa Iye, “Aphunzitsi, kodi simukusamala kuti timira?”
39 Jisua ânthoia, phâivuopui hah a ngoa, “Mong roh!” male tuidârinsok kôm han, “Omchien roh!” a tia. Phâivuopui hah amonga, male adâingang zoi.
Yesu anauka nadzudzula mphepo nati kwa mafunde, “Chete! Khala bata!” Pamenepo mphepo inaleka ndipo kunachita bata.
40 Hanchu Jisua'n a ruoisingei kôm “Ithomo ma angtaka nin chi hi? Taksônna reng nin la dônloi mo?” a tia.
Iye anati kwa ophunzira ake, “Muli ndi mantha chifukwa chiyani? Kodi mukanalibe chikhulupiriro?”
41 Aniatachu an chi sabaka, male inkhat le inkhat kôm, “Hi mi hih tumo ani hi? Phâivuopui le tuidârinsok tena khomin a chong an don hi?” anin ti inlôma.
Iwo anachita mantha nafunsana wina ndi mnzake kuti, “Uyu ndani? Ngakhale mphepo ndi nyanja zimumvera Iye!”