< ЗАХАРИЯ 2 >

1 Ам ридикат окий ши м-ам уйтат, ши ятэ кэ ера ун ом каре циня ын мынэ о фуние де мэсурат.
Kenaka ndinayangʼananso, ndipo ndinaona munthu atanyamula chingwe choyezera mʼmanja mwake.
2 Л-ам ынтребат: „Унде те дучь?” Ши ел мь-а зис: „Мэ дук сэ мэсор Иерусалимул, ка сэ вэд че лэциме ши че лунӂиме аре.”
Ndipo ndinafunsa kuti, “Kodi ukupita kuti?” Anandiyankha kuti, “Akukayeza Yerusalemu kuti ndidziwe mulifupi mwake ndi mulitali mwake.”
3 Ши ынӂерул каре ворбя ку мине а ынаинтат, ши ун алт ынӂер й-а ешит ынаинте.
Taonani, mngelo amene amayankhula nane uja akuchoka, mngelo wina anabwera kudzakumana naye
4 Ел й-а зис: „Аляргэ де ворбеште тынэрулуй ачестуя ши спуне-й: ‘Иерусалимул ва фи о четате дескисэ дин причина мулцимий оаменилор ши вителор каре вор фи ын мижлокул луй;
ndipo anamuwuza kuti, “Thamanga, kamuwuze mnyamatayo kuti, ‘Yerusalemu udzakhala mzinda wopanda malinga chifukwa mudzakhala anthu ambiri ndiponso ziweto zochuluka.
5 Еу Ынсумь’, зиче Домнул, ‘вой фи ун зид де фок де жур ымпрежурул луй ши вой фи слава луй ын мижлокул луй!’”
Ndipo Ine mwini ndidzakhala linga lamoto kuteteza mzindawo,’ akutero Yehova, ‘ndipo ndidzakhala ulemerero mʼkati mwake.’
6 „Фуӂиць, фуӂиць дин цара де ла мязэноапте!”, зиче Домнул. „Кэч в-ам ымпрэштият ын челе патру вынтурь але черурилор”, зиче Домнул.
“Tulukani! Tulukani! Thawaniko ku dziko la kumpoto,” akutero Yehova, “pakuti ndinakumwazirani ku mphepo zinayi zamlengalenga,” akutero Yehova.
7 „Скапэ, Сиоане, ту каре локуешть ла фийка Бабилонулуй!”
“Tuluka, iwe Ziyoni! Thawa, iwe amene umakhala mʼdziko la mwana wamkazi wa Babuloni!”
8 Кэч аша ворбеште Домнул оштирилор: „Дупэ славэ м-а тримис Ел ла нямуриле каре в-ау жефуит; кэч чел че се атинӂе де вой се атинӂе де лумина окилор Луй.
Pakuti Yehova Wamphamvuzonse akuti, “Atatha kundilemekeza wanditumiza kwa anthu a mitundu ina amene anakufunkhani; pakuti aliyense wokhudza inu wakhudza mwanadiso wanga.
9 Ятэ, Ымь ридик мына ымпотрива лор”, зиче Домнул, „ши еле вор фи прада челор че ле ерау супушь, ка сэ штиць кэ Домнул оштирилор м-а тримис.
Ndithu Ine ndidzawamenya anthuwo ndi dzanja langa ndipo amene anali akapolo awo ndiye adzawalande zinthu. Pamenepo mudzadziwa kuti Yehova Wamphamvuzonse ndiye wandituma.
10 Стригэ де веселие ши букурэ-те, фийка Сионулуй! Кэч, ятэ, Еу вин ши вой локуи ын мижлокул тэу”, зиче Домнул.
“Iwe mwana wamkazi wa Ziyoni, fuwula ndipo sangalala. Pakuti taona ndikubwera, ndipo ndidzakhala pakati pako,” akutero Yehova.
11 „Мулте нямурь се вор алипи де Домнул ын зиуа ачея ши вор фи попорул Меу. Еу вой локуи ын мижлокул тэу ши вей шти кэ Домнул оштирилор м-а тримис ла тине.”
“Nthawi imeneyo anthu a mitundu yambiri adzabwera kwa Yehova ndipo adzasanduka anthu anga. Ndidzakhala pakati pako ndipo iwe udzadziwa kuti Yehova Wamphamvuzonse wandituma kwa iwe.
12 Домнул ва луа ын стэпынире пе Иуда, ка партя Луй де моштенире ын пэмынтул сфынт, ши ва алеӂе ярэшь Иерусалимул.
Yehova adzachititsa kuti Yuda akhale chuma chake mʼdziko lopatulika ndipo adzasankhanso Yerusalemu.
13 Орьче фэптурэ сэ такэ ынаинтя Домнулуй, кэч Ел С-а ши скулат дин Локашул Луй чел Сфынт!
Khalani chete pamaso pa Yehova anthu nonse, chifukwa Iye wavumbuluka kuchoka ku malo ake opatulika.”

< ЗАХАРИЯ 2 >