< Псалмул 70 >
1 Грэбеште, Думнезеуле, де мэ избэвеште! Грэбеште де-мь ажутэ, Доамне!
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Pempho. Fulumirani Mulungu kundipulumutsa; Yehova bwerani msanga kudzandithandiza.
2 Сэ рэмынэ де рушине ши ынфрунтаць чей че вор сэ-мь я вяца! Сэ дя ынапой ши сэ рошяскэ чей че-мь дореск пеиря!
Iwo amene akufunafuna moyo wanga achititsidwe manyazi ndi kusokonezedwa; onse amene akukhumba chiwonongeko changa abwezedwe mopanda ulemu.
3 Сэ се ынтоаркэ ынапой де рушине чей че зик: „Аха! Аха!”
Onse amene akunena kwa ine kuti, “Aha, aha,” abwerere chifukwa cha manyazi awo.
4 Тоць чей че Те каутэ сэ се веселяскэ ши сэ се букуре ын Тине! Чей че юбеск мынтуиря Та сэ зикэ неынчетат: „Прямэрит сэ фие Думнезеу!”
Koma onse amene akufunafuna Inu akondwere ndi kusangalala mwa Inu; iwo amene amakonda chipulumutso chanu nthawi zonse anene kuti, “Mulungu akuzike!”
5 Еу сунт сэрак ши липсит: грэбеште сэ-мь ажуць, Думнезеуле! Ту ешть Ажуторул ши Избэвиторул меу: Доамне, ну зэбови!
Koma ine ndine wosauka ndi wosowa; bwerani msanga kwa ine Inu Mulungu. Inu ndinu thandizo langa ndi momboli wanga; Inu Yehova musachedwe.