< Псалмул 133 >
1 Ятэ че плэкут ши че дулче есте сэ локуяскэ фраций ымпреунэ!
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
2 Есте ка унтделемнул де прец, каре, турнат пе капул луй, се кобоарэ пе барбэ, пе барба луй Аарон, се кобоарэ пе марӂиня вешминтелор луй.
Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
3 Есте ка роуа Хермонулуй, каре се кобоарэ пе мунций Сионулуй, кэч аколо дэ Домнул бинекувынтаря, вяца, пентру вешничие.
Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.