< Псалмул 13 >
1 Пынэ кынд, Доамне, мэ вей уйта неынчетат? Пынэ кынд Ыць вей аскунде Фаца де мине?
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Mpaka liti Yehova? Kodi mudzandiyiwala mpaka kalekale? Mpaka liti mudzandibisira nkhope yanu?
2 Пынэ кынд вой авя суфлетул плин де грижь ши инима плинэ де неказурь ын фиекаре зи? Пынэ кынд се ва ридика врэжмашул меу ымпотрива мя?
Ndidzalimbana ndi maganizo anga ndi kukhala ndi chisoni mu mtima mwanga tsiku lililonse mpaka liti? Mpaka liti adani anga adzandipambana?
3 Привеште, рэспунде-мь, Доамне, Думнезеул меу! Дэ луминэ окилор мей, ка сэ н-адорм сомнул морций,
Ndiyangʼaneni ndi kundiyankha, Inu Yehova Mulungu wanga. Walitsani maso anga kuti ndingafe;
4 ка сэ ну зикэ врэжмашул меу: „Л-ам бируит” ши сэ ну се букуре потривничий мей кынд мэ клатин!
mdani wanga adzati, “Ndamugonjetsa,” ndipo adani anga adzakondwera pamene ine ndagwa.
5 Еу ам ынкредере ын бунэтатя Та, сунт ку инима веселэ дин причина мынтуирий Тале:
Koma ndikudalira chikondi chanu chosasinthika; mtima wanga umakondwera ndi chipulumutso chanu.
6 кынт Домнулуй, кэч мь-а фэкут бине!
Ine ndidzayimbira Yehova pakuti wandichitira zokoma.