< Псалмул 122 >
1 Мэ букур кынд ми се зиче: „Хайдем ла Каса Домнулуй!”
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndinakondwera atandiwuza kuti, “Tiyeni ku nyumba ya Yehova.”
2 Пичоареле ми се опреск ын порциле тале, Иерусалиме!
Mapazi athu akuyima mʼzipata zako, Iwe Yerusalemu.
3 Иерусалиме, ту ешть зидит ка о четате фэкутэ динтр-о букатэ!
Yerusalemu anamangidwa ngati mzinda umene uli wothithikana pamodzi.
4 Аколо се суе семинцииле, семинцииле Домнулуй, дупэ леӂя луй Исраел, ка сэ лауде Нумеле Домнулуй.
Kumeneko ndiye kumene kumapita mafuko, mafuko a Yehova, umboni wa kwa Israeli, kuti atamande dzina la Yehova.
5 Кэч аколо сунт скаунеле де домние пентру жудекатэ, скаунеле де домние але касей луй Давид.
Kumeneko anayikako mipando yaufumu yachiweruzo, mipando yaufumu ya nyumba ya Davide.
6 Ругаци-вэ пентру пачя Иерусалимулуй! Чей че те юбеск сэ се букуре де одихнэ.
Pemphererani mtendere wa Yerusalemu: “Iwo amene amakukonda iwe zinthu ziwayendere bwino.
7 Пачя сэ фие ынтре зидуриле тале ши лиништя, ын каселе тале домнешть!
Mukhale mtendere mʼkati mwa makoma ako, ndipo mʼnyumba zako zaufumu mukhale chitetezo.”
8 Дин причина фрацилор ши а приетенилор мей, дореск пачя ын сынул тэу.
Chifukwa cha abale anga ndi abwenzi anga ndidzati, “Mtendere ukhale mʼkati mwako.”
9 Дин причина Касей Домнулуй Думнезеулуй ностру, фак урэрь пентру феричиря та.
Chifukwa cha Nyumba ya Yehova Mulungu wathu, ndidzakufunira zabwino.