< Псалмул 120 >
1 Кэтре Домнул стриг ын стрымтораря мя, ши Ел м-аскултэ.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Доамне, скапэ-мь суфлетул де буза минчиноасэ, де лимба ыншелэтоаре!
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Че-ць дэ Ел цие, че-ць адуче Ел цие, лимбэ ыншелэтоаре?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Сэӂець аскуците де рэзбойник, ку кэрбунь априншь де енупэр.
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Вай де мине кэ локуеск ла Мешек, кэ локуеск ын кортуриле Кедарулуй!
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Дестул мь-а локуит суфлетул лынгэ чей че урэск пачя.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Еу сунт пентру паче, дар де ындатэ че ворбеск еу, ей сунт пентру рэзбой.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.