< Псалмул 114 >

1 Кынд а ешит Исраел дин Еӂипт, кынд а плекат каса луй Иаков де ла ун попор стрэин,
Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
2 Иуда а ажунс Локашул Луй чел Сфынт ши Исраел, стэпыниря Луй.
Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
3 Маря а вэзут лукрул ачеста ши а фуӂит, Йорданул с-а ынторс ынапой,
Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
4 мунций ау сэрит ка ниште бербечь ши дялуриле, ка ниште мей.
mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
5 Че ай ту, маре, де фуӂь ши ту, Йордануле, де те ынторчь ынапой?
Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
6 Че авець, мунцилор, де сэлтаць ка ниште бербечь ши вой, дялурилор, ка ниште мей?
inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
7 Да, кутремурэ-те, пэмынтуле, ынаинтя Домнулуй, ынаинтя Думнезеулуй луй Иаков,
Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
8 каре префаче стынка ын яз ши кременя ын извор де апе.
amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.

< Псалмул 114 >