< Псалмул 1 >

1 Фериче де омул каре ну се дуче ла сфатул челор рэй, ну се опреште пе каля челор пэкэтошь ши ну се ашазэ пе скаунул челор батжокориторь,
Wodala munthu amene satsatira uphungu wa anthu ochimwa, kapena kuyima mʼnjira ya anthu oyipa, kapena kukhala mʼmagulu a anthu onyoza.
2 чи ышь гэсеште плэчеря ын Леӂя Домнулуй ши зи ши ноапте куӂетэ ла Леӂя Луй!
Koma chikondwerero chake chili mʼmalamulo a Yehova ndipo mʼmalamulo akewo amalingaliramo usana ndi usiku.
3 Ел есте ка ун пом сэдит лынгэ ун извор де апэ, каре ышь дэ родул ла время луй ши але кэруй фрунзе ну се вештежеск; тот че ынчепе дуче ла бун сфыршит.
Iye ali ngati mtengo wodzalidwa mʼmbali mwa mitsinje ya madzi, umene umabereka zipatso zake pa nyengo yake ndipo masamba ake safota. Chilichonse chimene amachita amapindula nacho.
4 Ну тот аша есте ку чей рэй, чи ей сунт ка плява, пе каре о спулберэ вынтул.
Sizitero ndi anthu oyipa! Iwo ali ngati mungu umene umawuluzidwa ndi mphepo.
5 Де ачея чей рэй ну пот цине капул сус ын зиуа жудекэций, нич пэкэтоший, ын адунаря челор неприхэниць.
Kotero anthu oyipa sadzatha kuyima pa chiweruzo, kapena anthu ochimwa mu msonkhano wa anthu olungama.
6 Кэч Домнул куноаште каля челор неприхэниць, дар каля пэкэтошилор дуче ла пеире.
Pakuti Yehova amayangʼanira mayendedwe a anthu olungama, koma mayendedwe a anthu oyipa adzawonongeka.

< Псалмул 1 >