< Исая 15 >

1 Пророчие ымпотрива Моабулуй: „Кяр ын ноаптя кынд есте пустиит, Ар-Моабул есте нимичит! Кяр ын ноаптя кынд есте пустиит, Кир-Моабул есте нимичит!…
Uthenga wonena za Mowabu: Popeza kuti mu usiku umodzi wokha mzinda wa Ari wa ku Mowabu wawonongedwa, wawonongedwa pa usiku umodzi wokha. Mzinda wa Kiri wawonongedwa, wawonongedwa pa usiku umodzi wokha.
2 Попорул се суе ла темплу ши ла Дибон, пе ынэлцимь, ка сэ плынгэ; Моабул се бочеште: пе Небо ши пе Медеба тоате капетеле сунт расе ши тоате бэрбиле сунт тэяте.
Anthu a ku Diboni akupita ku nyumba ya milungu yawo, akupita ku malo awo achipembedzo kukalira; anthu a ku Mowabu akulirira mofuwula mzinda wa Nebo ndi wa Medeba. Mutu uliwonse wametedwa mpala, ndipo ndevu zonse zametedwa.
3 Пе улице сунт ынчиншь ку сачь, пе акоперишурь ши ын пеце тотул ӂеме ши се топеште плынгынд.
Mʼmisewu akuvala ziguduli; pa madenga ndi mʼmabwalo aliyense akulira mofuwula, misozi ili pupupu.
4 Хесбонул ши Елеале ципэ де ли се ауде гласул пынэ ла Иахац, кяр ши рэзбойничий Моабулуй се боческ ку суфлетул плин де гроазэ.
Anthu a ku Hesiboni ndi Eleali akulira mofuwula, mawu awo akumveka mpaka ku Yahazi. Kotero asilikali a ku Mowabu akulira mofuwula, ndipo ataya mtima.
5 Ымь плынӂе инима пентру Моаб, ай кэруй фугарь аляргэ пынэ ла Цоар, пынэ ла Еглат-Шелишия, кэч суе, плынгынд, суишул Лухитулуй ши скот ципете де дурере пе друмул Хоронаимулуй.
Inenso ndikulirira Mowabu; chifukwa othawa nkhondo ake akupita akulira ku chikweza cha Luluti mpaka ku Zowari ndi Egilati-Selisiya akupita akulira ku chikweza cha Luhiti, Akulira mosweka mtima pa njira yopita ku Horonaimu; akulira mosweka mtima chifukwa cha chiwonongeko chawo.
6 Кэч апеле Нимрим сунт пустиите, с-а ускат ярба, с-а дус вердяца ши ну май есте ничун фир верде.
Madzi a ku Nimurimu aphwa ndipo udzu wauma; zomera zawonongeka ndipo palibe chomera chobiriwira chatsala.
7 Де ачея стрынг че ле май рэмыне ши ышь стрэмутэ авериле динколо де пырыул сэлчиилор.
Kotero kuti chuma chomwe anachipeza ndi kuchisunga, achitenga kuti awoloke nacho chigwembe cha Misondozi.
8 Кэч ципетеле ынконжоарэ хотареле Моабулуй; бочетеле луй рэсунэ пынэ ла Еглаим ши урлетеле луй рэсунэ пынэ ла Беер-Елим.
Kulira kwawo kukumveka mʼdziko lonse la Mowabu; kulira kwawo kosweka mtima kukumveka mpaka ku Egilaimu ndi Beeri-Elimu.
9 Апеле Димонулуй сунт плине де сынӂе ши вой тримите песте Димон ной ненорочирь; ун леу ва вени ымпотрива челор скэпаць ай Моабулуй, ымпотрива рэмэшицей дин царэ.
Madzi a ku Dimoni afiira ndi magazi, komabe ndidzabweretsa zina zambiri pa Dimoni, mkango woti udzagwire aliyense othawa mu Mowabu ndi aliyense wotsala mʼdzikomo.

< Исая 15 >