< Isaías 62 >
1 Pelo bem de Zion, não vou me calar, e para o bem de Jerusalém não descansarei, até que sua retidão resplandeça como o amanhecer, e sua salvação como uma lâmpada em chamas.
Chifukwa chokonda Ziyoni sindidzakhala chete, chifukwa chokonda Yerusalemu sindidzakhala chete, mpaka chilungamo chake chitaoneka poyera ngati kuwala, ndi chipulumutso chake chitaoneka ngati sakali yoyaka.
2 As nações verão sua retidão, e todos os reis sua glória. Você será chamado por um novo nome, que a boca de Yahweh vai citar.
Mitundu ya anthu idzaona iwe utapambana pa nkhondo ndipo mafumu onse adzaona ulemerero wako. Adzakuyitanira dzina latsopano limene adzakupatse ndi Yehova.
3 Você também será uma coroa de beleza na mão de Yahweh, e um diadema real na mão de seu Deus.
Udzakhala ngati chipewa chaulemerero mʼdzanja la Yehova, ndi ngati nduwira yaufumu mʼdzanja la Mulungu wako.
4 Você não será mais chamado de Forsaken, nem sua terra será mais chamada de Desolada; mas você será chamado de Hephzibah, e sua terra Beulah; para Yahweh se deleita em você, e sua terra será casada.
Sadzakutchanso “Wosiyidwa,” ndipo dziko lako silidzatchedwanso “Chipululu.” Koma dzina lako latsopano lidzakhala “Ndakondwera naye.” Ndipo dziko lako lidzatchedwa “Wokwatiwa.” Chifukwa Yehova akukondwera nawe, ndipo adzakhala ngati mwamuna wa dziko lako.
5 Pois quando jovem, casa-se com uma virgem, para que seus filhos se casem com você. Como um noivo se alegra com sua noiva, para que seu Deus se regozije por você.
Monga mnyamata amakwatira namwali, momwenso mmisiri wodzakumanga adzakukwatira; monga mkwati amakondwera ndi mkwatibwi, chonchonso Mulungu adzakondwera nawe.
6 Coloquei guardas em seus muros, Jerusalém. Eles nunca ficarão em silêncio dia ou noite. Vocês que invocam Yahweh, não descansem,
Iwe Yerusalemu, pa malinga ako ndayikapo alonda; sadzakhala chete usana kapena usiku. Inu amene mumakumbutsa Yehova za malonjezo ake musapumule.
7 e não lhe dar descanso até que ele se estabeleça, e até que ele faça de Jerusalém um louvor na terra.
Musamupatse mpata wopuma mpaka atakhazikitsa Yerusalemu kukhala mzinda umene dziko lapansi lidzawutamande.
8 Yahweh jurou por sua mão direita, e pelo braço de sua força, “Certamente não darei mais seus grãos para serem alimento para seus inimigos, e os estrangeiros não beberão seu novo vinho, para o qual você trabalhou,
Yehova analumbira atakweza dzanja lake. Anati, “Sindidzaperekanso tirigu wako kuti akhale chakudya cha adani ako, ndipo alendo sadzamwanso vinyo wako watsopano pakuti unamuvutikira.
9 mas aqueles que a colheram vão comê-la, e elogiar Yahweh. Aqueles que o recolheram o beberão nos tribunais do meu santuário”.
Koma amene amakakolola ndiwo amene adzadye buledi ndi kutamanda Yehova, ndipo amene amasonkhanitsa pamodzi mphesa ndiwo amene adzamwe vinyo mʼmabwalo a Nyumba yanga.”
10 Atravesse, atravesse os portões! Prepare o caminho do povo! Construa, construa a rodovia! Junte as pedras! Levantar uma bandeira para os povos.
Tulukani, dutsani pa zipata! Konzerani anthu njira. Lambulani, lambulani msewu waukulu! Chotsani miyala. Kwezani mbendera kuti mitundu ya anthu izione.
11 Eis que Yahweh proclamou até o fim do mundo: “Diga à filha de Zion, “Eis que vem a sua salvação! Eis que sua recompensa está com ele, e sua recompensa diante dele””.
Yehova walengeza ku dziko lonse lapansi kuti, Awuzeni anthu a ku Yerusalemu kuti, “Taonani, chipulumutso chanu chikubwera; Yehova akubwera ndi mphotho yake akubwera nazo zokuyenerani.”
12 Eles os chamarão de “O Povo Santo”, Yahweh's Redeemed”. Você será chamado de “Sought Out”, Uma cidade não abandonada”.
Iwo adzatchedwa Anthu Opatulika, owomboledwa a Yehova; ndipo adzakutchani “Okondwa a Yehova” “Mzinda umene Yehova sanawusiye.”