< Salmos 16 >
1 Cântico de Davi: Guarda-me, ó Deus; porque eu confio em ti.
Mikitamu ya Davide. Ndisungeni Inu Mulungu, pakuti ine ndimathawira kwa Inu.
2 Tu, [minha alma], disseste ao SENHOR: Tu és meu Senhor; minha bondade não [chega] até ti.
Ndinati kwa Yehova, “Inu ndinu Ambuye anga; popanda Inu, ine ndilibe chinthu chinanso chabwino.”
3 [Mas] aos santos que [estão] na terra, e [a] os ilustres, nos quais está todo o meu prazer.
Kunena za oyera mtima amene ali pa dziko, amenewa ndi olemekezeka, amene ndimakondwera nawo.
4 As dores se multiplicarão daqueles que se apressam [para servir] a outros [deuses]; eu não oferecerei seus sacrifícios de derramamento de sangue, e não tomarei seus nomes em meus lábios.
Anthu amene amathamangira kwa milungu ina mavuto awo adzachulukadi. Ine sindidzathira nawo nsembe zawo zamagazi kapena kutchula mayina awo ndi pakamwa panga.
5 O SENHOR é a porção da minha herança e o meu cálice; tu sustentas a minha sorte.
Yehova, Inu mwandipatsa cholowa changa ndi chikho changa; mwateteza kolimba gawo langa.
6 Em lugares agradáveis foram postos os limites [do meu terreno]; sim, eu recebo uma bela propriedade.
Malire a malo anga akhala pabwino; ndithudi, ine ndili cholowa chokondweretsa kwambiri.
7 Eu louvarei ao SENHOR, que me aconselhou; até de noite meus sentimentos me ensinam.
Ine ndidzatamanda Yehova amene amandipatsa uphungu; ngakhale usiku mtima wanga umandilangiza.
8 Ponho ao SENHOR continuamente diante de mim; porque [ele está] à minha direita; nunca serei abalado.
Ndayika Yehova patsogolo panga nthawi zonse. Popeza Iyeyo ali kudzanja langa lamanja, sindidzagwedezeka.
9 Por isso meu coração está contente, e minha glória se alegra; certamente minha carne habitará em segurança.
Choncho mtima wanga ndi wosangalala ndipo pakamwa panga pakukondwera; thupi langanso lidzakhala pabwino,
10 Porque tu não deixarás a minha alma no Xeol, nem permitirás que teu Santo veja a degradação. (Sheol )
chifukwa Inu simudzandisiya ku manda, simudzalola kuti woyera wanu avunde. (Sheol )
11 Tu me farás conhecer o caminho da vida; fartura de alegrias [há] em tua presença; agrados estão em tua mão direita para sempre.
Inu mwandidziwitsa njira ya moyo; mudzandidzaza ndi chimwemwe pamaso panu, ndidzasangalala mpaka muyaya pa dzanja lanu lamanja.