< Zachariasza 6 >

1 Potem odwróciłem się, podniosłem swoje oczy i spojrzałem, a oto cztery rydwany wychodziły spomiędzy dwóch gór, a [te] góry [były] z miedzi.
Ndinayangʼananso ndipo taonani ndinaona magaleta anayi akutuluka pakati pa mapiri awiri, mapiri amkuwa.
2 Przy pierwszym rydwanie [były] konie rude, przy drugim rydwanie – konie kare;
Galeta loyamba limakokedwa ndi akavalo ofiira, lachiwiri ndi akavalo akuda,
3 Przy trzecim rydwanie – konie białe, a przy czwartym rydwanie [były] konie pstrokate i gniade.
lachitatu ndi akavalo oyera, ndipo lachinayi ndi akavalo otuwa a mawanga ofiirira, onsewa anali akavalo amphamvu kwambiri.
4 Wtedy zapytałem Anioła, który rozmawiał ze mną: Co to [jest], mój Panie?
Ndinafunsa mngelo amene amayankhula nane uja kuti, “Kodi mbuye wanga chimenechi nʼchiyani?”
5 I Anioł odpowiedział mi: To [są] cztery duchy nieba, wyruszają [one] z [miejsca], gdzie stały przed Panem całej ziemi.
Mngeloyo anandiyankha kuti, “Imeneyi ndi mizimu inayi yakumwamba, imene ikuchokera pamaso pa Ambuye wa dziko lonse.
6 Zaprzężone konie kare wyruszają do ziemi północnej, białe wyruszają za nimi, pstrokate zaś wyruszają do ziemi południowej.
Galeta la akavalo akuda likupita ku dziko la kumpoto, galeta la akavalo oyera likutsatira, ndipo galeta la akavalo amawanga ofiirira likupita ku dziko la kummwera.”
7 A te gniade [konie] wyruszyły, rwały się do biegu, aby obejść ziemię. Wtedy powiedział: Idźcie i obejdźcie ziemię! I obeszły ziemię.
Pamene akavalo amphamvuwa ankapita, anali ndi changu chofuna kuyendera dziko lapansi. Ndipo iye anati, “Pitani, kayendereni dziko lapansi!”
8 Potem zawołał mnie i powiedział: Oto te, które wyruszyły do ziemi północnej, uspokoiły mojego ducha w ziemi północnej.
Pamenepo anandiyitana, “Taona, akavalo amene apita ku dziko la kumpoto apumulitsa Mzimu wanga kumeneko.”
9 I doszło do mnie słowo PANA mówiące:
Yehova anayankhula nane kuti,
10 Weź [dary] od tych, co byli w niewoli: od Cheldaja, od Tobiasza i od Jedajasza, którzy przybyli z Babilonu, i przyjdź w tym samym dniu, i wejdź do domu Jozjasza, syna Sofoniasza;
“Landira mphatso kuchokera kwa anthu amene abwera ku ukapolo, Helidai, Tobiya ndi Yedaya, amene achokera ku Babuloni. Tsiku lomwelo pita ku nyumba ya Yosiya mwana wa Zefaniya.
11 Weź srebro i złoto, zrób korony i włóż je na głowę Jozuego, syna Josadaka, najwyższego kapłana.
Tenga siliva ndi golide upange chipewa chaufumu, ndipo uchiyike pamutu pa mkulu wa ansembe, Yoswa mwana wa Yehozadaki.
12 I powiedz do niego: Tak mówi PAN zastępów: Oto mąż, którego imię brzmi Latorośl; on wyrośnie ze swego miejsca i zbuduje świątynię PANA.
Muwuze kuti zimene akunena Yehova Wamphamvuzonse ndi izi: ‘Taonani, munthu wotchedwa Nthambi ndi ameneyu, ndipo adzaphuka pomwe alipo ndi kumanga Nyumba ya Yehova.
13 On zbuduje świątynię PANA, będzie obdarzony chwałą, zasiądzie na swoim tronie i będzie panować na nim, i będzie on kapłanem na swoim tronie; i rada pokoju będzie między nimi oboma.
Ndiye amene adzamange Nyumba ya Yehova, adzalandira ulemerero waufumu ndipo adzalamulira pa mpando wake waufumu. Adzakhalanso wansembe pa mpando wake waufumu. Ndipo padzakhala mtendere.’
14 A [te] korony będą dla Chelema, Tobiasza, Jedajasza i Chena, syna Sofoniasza, jako pamiątka w świątyni PANA.
Chipewa cha ufumucho adzachipereka kwa Helemu, Tobiya, Yedaya, ndi kwa Heni mwana wa Zefaniya, kuti chikhale chikumbutso mʼNyumba ya Yehova.
15 Przyjdą ludzie z dalekich stron i będą budować świątynię PANA, i poznacie, że PAN zastępów posłał mnie do was. A to się stanie, jeśli pilnie będziecie słuchać głosu PANA, swego Boga.
Anthu okhala kutali adzabwera kudzathandiza kumanga Nyumba ya Yehova, ndipo iwe udzadziwa kuti Yehova Wamphamvuzonse wandituma kwa iwe. Zimenezi zidzachitika ngati mudzamvera mwachangu Yehova Mulungu wanu.”

< Zachariasza 6 >