< Psalmów 4 >
1 Przewodnikowi chóru, na Neginot. Psalm Dawida. Wysłuchaj mnie, gdy [cię] wzywam, Boże mojej sprawiedliwości! Ty wyzwoliłeś mnie w [czasie] ucisku. Zmiłuj się nade mną i wysłuchaj mojej modlitwy.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe wa zida za zingwe. Salimo la Davide. Ndiyankheni pamene ndiyitana Inu, Inu Mulungu wa chilungamo changa. Pumulitseni ku zowawa zanga; chitireni chifundo ndi kumva pemphero langa.
2 Synowie ludzcy, jak długo [będziecie] znieważać moją chwałę? [Jak długo] będziecie miłować marność [i] szukać kłamstwa? (Sela)
Anthu inu, mpaka liti mudzakhala mukusandutsa ulemerero wanga kukhala manyazi? Mpaka liti mudzakonda zachabe ndi kufuna milungu yabodza? (Sela)
3 Wiedzcie, że PAN oddzielił dla siebie pobożnego. PAN wysłucha, gdy zawołam do niego.
Dziwani kuti Yehova wadziyikira padera anthu okhulupirika; Yehova adzamva pamene ndidzamuyitana.
4 Zadrżyjcie i nie grzeszcie. Rozmyślajcie w swym sercu na łożu i zamilczcie. (Sela)
Kwiyani koma musachimwe; pamene muli pa mabedi anu, santhulani mitima yanu ndi kukhala chete. (Sela)
5 Składajcie ofiary sprawiedliwości i ufajcie PANU.
Perekani nsembe zolungama ndipo dalirani Yehova.
6 Wielu mówi: Któż pokaże nam dobro? PANIE, wznieś nad nami światło twego oblicza.
Ambiri akufunsa kuti, “Ndani angationetse chabwino chilichonse?” Kuwunika kwa nkhope yanu kutiwalire, Inu Yehova.
7 Wlałeś w moje serce więcej radości niż w czasie, gdy obfitowały ich zboże i wino.
Inu mwadzaza mtima wanga ndi chimwemwe chachikulu kuposa kuchuluka kwa tirigu wawo ndi vinyo watsopano.
8 W spokoju się położę i zasnę, bo ty sam, PANIE, sprawiasz, że mieszkam bezpiecznie.
Ine ndidzagona ndi kupeza tulo mwamtendere, pakuti Inu nokha, Inu Yehova, mumandisamalira bwino.