< Psalmów 133 >

1 Pieśń stopni Dawida. Oto jak dobrze i jak miło, gdy bracia zgodnie mieszkają.
Salimo la Davide. Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Onani, nʼkokoma ndi kokondweretsa ndithu pamene abale akhala pamodzi mwachiyanjano!
2 [Jest] to jak wyborny olejek na głowę, który spływa na brodę, na brodę Aarona; który spływa na brzeg jego szat;
Zili ngati mafuta amtengowapatali othiridwa pa mutu, otsikira ku ndevu, ku ndevu za Aaroni, oyenderera mpaka mʼkhosi mwa mkanjo wake.
3 Jak rosa Hermonu, która opada na góry Syjon; tam bowiem PAN daje błogosławieństwo i życie na wieki.
Zili ngati mame a ku Heremoni otsikira pa Phiri la Ziyoni. Pakuti pamenepo Yehova amaperekapo dalitso, ndiwo moyo wamuyaya.

< Psalmów 133 >