< Psalmów 114 >

1 Gdy Izrael wychodził z Egiptu, dom Jakuba spośród ludu obcego języka;
Pamene Israeli anatuluka mu Igupto, nyumba ya Yakobo kuchoka ku mtundu wa anthu a chiyankhulo chachilendo,
2 Juda stał się jego świątynią, Izrael jego panowaniem.
Yuda anasanduka malo opatulika a Mulungu, Israeli anasanduka ufumu wake.
3 Morze to ujrzało i uciekło, Jordan wstecz się odwrócił.
Nyanja inaona ndi kuthawa, mtsinje wa Yorodani unabwerera mʼmbuyo;
4 Góry skakały jak barany, pagórki jak jagnięta.
mapiri analumphalumpha ngati nkhosa zazimuna, timapiri ngati ana ankhosa.
5 Morze, cóż ci [się stało], żeś uciekło, a tobie, Jordanie, że wstecz się odwróciłeś?
Nʼchifukwa chiyani iwe unathawa? iwe mtsinje wa Yorodani unabwereranji mʼmbuyo?
6 Góry, [że] skakałyście jak barany, a wy, pagórki, jak jagnięta?
inu mapiri, munalumphalumphiranji ngati nkhosa zazimuna, inu timapiri, ngati ana ankhosa?
7 Zadrżyj, ziemio, przed obliczem Pana, przed obliczem Boga Jakuba;
Njenjemera pamaso pa Ambuye iwe dziko lapansi, pamaso pa Mulungu wa Yakobo,
8 Który zamienia skałę w jezioro, [a] krzemień w źródło wód.
amene anasandutsa thanthwe kukhala chitsime, thanthwe lolimba kukhala akasupe a madzi.

< Psalmów 114 >