< Izajasza 21 >
1 Brzemię pustynnego morza. Jak wicher na południe nadciąga, tak przyjdzie z pustyni, ze strasznej ziemi.
Uthenga wonena za chipululu cha mʼmbali mwa Nyanja. Ankhondo a ku Elamu ndi Mediya adzabwera ngati kamvuluvulu amene akuwomba modutsa mʼmbali ya nyanja, kuchokera ku chipululu, dziko lochititsa mantha.
2 Srogie widzenie jest mi pokazane. Zdrajca zdradza, niszczyciel niszczy. Nadciągnij, Elamie! Oblegaj, Medio! Położę kres wszelkiemu wzdychaniu.
Ine ndaona zinthu zoopsa mʼmasomphenya: Wonyenga akunyenga, wofunkha akufunkha komanso owononga akuwononga. Elamu, yambani nkhondo! Mediya, zingani mzinda! Ine ndidzathetsa mavuto onse amene anayambitsa Ababuloni.
3 Dlatego moje biodra są wypełnione bólem, ogarnęły mnie skurcze jak skurcze rodzącej. Wstrząśnięty jestem tym, co słyszę, przerażony tym, co widzę.
Chifukwa cha zimenezi thupi langa likunjenjemera ndi mantha, ndikumva ululu ngati wa mayi amene akubereka; ndikuvutika kwambiri ndi zimene ndikumva, ndathedwa nzeru ndi zimene ndikuziona.
4 Zlękło się moje serce, strach mnie ogarnął. Noc moich rozkoszy zamieniła się w postrach.
Mtima wanga ukugunda, ndipo ndikunjenjemera ndi mantha; chisisira chimene ndakhala ndikuchifuna chasanduka chinthu choopsa kwa ine.
5 Przygotuj stół, niech strażnik trzyma straż; jedz, pij. Wstańcie, książęta, namaszczajcie tarcze.
Ankhondo a ku Elamu ndi Mediya akukonza matebulo, akuyala mphasa, akudya komanso kumwa! Mwadzidzidzi anamva mawu akuti, “Dzukani inu ankhondo, pakani mafuta zishango zanu!”
6 Tak bowiem powiedział mi Pan: Idź, postaw strażnika, niech mówi, co widzi.
Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi; “Pita, kayike mlonda kuti azinena zimene akuziona.
7 I zobaczył rydwan z dwoma jeźdźcami, który ciągnęły osły, i rydwan, który ciągnęły wielbłądy; i przypatrywał się im z wielką uwagą.
Taonani, anthu akubwera ali pa akavalo ndipo akuyenda awiriawiri, okwera pa bulu kapena okwera pa ngamira, mlondayo akhale tcheru kwambiri.”
8 Wtedy zawołał [jak] lew: Panie mój! Stoję ciągle za dnia na wieży strażniczej; stoję na warcie całymi nocami.
Ndipo mlondayo anafuwula kuti, “Ambuye anga, tsiku ndi tsiku ndimakhala pa nsanja yolondera; Usiku uliwonse ndimakhala pa malo anga olondera.
9 A oto nadciągają mężczyźni na rydwanie z dwoma jeźdźcami. I zawołał: Upadł, upadł Babilon i wszystkie rzeźbione posągi jego bogów roztrzaskane zostały o ziemię.
Taonani, uyo munthu akubwera atakwera pa galeta ali ndi gulu la akavalo. Mmodzi wa iwo akuti, ‘Babuloni wagwa, wagwa! Mafano onse a milungu yake agwa pansi ndipo aphwanyika!’”
10 O moi wymłóceni i zboże mego klepiska! Co usłyszałem od PANA zastępów, Boga Izraela, to wam oznajmiłem.
Inu anthu anga opunthidwa ndi kupetedwa ngati tirigu, ine ndikukuwuzani zimene ndamva ndikukuwuzani Uthenga wochokera kwa Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli.
11 Brzemię Dumy. Z Seiru ktoś woła do mnie: Strażniku, co [się stało] w nocy? Strażniku, co [się stało] w nocy?
Uthenga wonena za Duma: Munthu wina akundiyitana kuchokera ku Seiri kuti, “Iwe mlonda, usikuwu utha liti? Iwe mlonda, utha liti kodi usikuwu?”
12 Strażnik odpowiedział: Nadchodzi poranek, a także noc. Jeśli chcecie dopytywać, dopytujcie, nawróćcie się, przyjdźcie.
Mlonda akuyankha kuti, “Kukucha, koma kudanso. Ngati ukufuna kufunsa, funsa tsopano; ndipo ubwerenso udzafunse.”
13 Brzemię na Arabię. W lasach Arabii będziecie nocować, wy, karawany Dedanitów.
Uthenga wonena za Arabiya: Inu anthu amalonda a ku Dedani, amene usiku mumagona mʼzithukuluzi za ku Arabiya,
14 Niech mieszkańcy Tema wyjdą z wodą naprzeciw spragnionych, ze swoim chlebem niech wyjdą na spotkanie uciekającym.
perekani madzi kwa anthu aludzu. Inu anthu a ku Tema perekani chakudya kwa anthu othawa nkhondo.
15 Będą bowiem uciekali przed mieczami, przed dobytym mieczem, przed napiętym łukiem, przed ciężką bitwą.
Iwo akuthawa malupanga, lupanga losololedwa, akuthawa uta wokokakoka ndiponso nkhondo yoopsa.
16 Gdyż tak Pan powiedział do mnie: Za rok, liczony jak rok najemnika, ustanie cała chwała Kedaru.
Zimene Ambuye akunena kwa ine ndi izi: “Chaka chimodzi chisanathe, potsata mmene amawerengera munthu waganyu, ulemerero wonse wa Kedara udzatheratu.
17 A reszta spośród łuczników, dzielni wojownicy spośród synów Kedaru, będzie zmniejszona. Tak bowiem powiedział PAN, Bóg Izraela.
Mwa anthu okoka uta, ankhondo a ku Kedara opulumuka adzakhala owerengeka.” Wayankhula ndi Yehova Mulungu wa Israeli.