< Pieśń nad Pieśniami 8 >

1 Obyżeś był jako bratem moim, pożywając piersi matki mojej! abym cię znalazłszy na dworzu, pocałowała cię, a nie była wzgardzona.
Ukanakhala kuti ndiwe mlongo wanga, amene anayamwa mawere a amayi anga! Ndikanakumana nawe pa njira, ndikanakupsompsona, ndipo palibe wina aliyense akanandinyoza.
2 Prowadziłabym cię, i wprowadziła do domu matki mojej, gdziebyś mię uczył; a jabym ci dała pić wino przyprawne i moszcz z jabłek moich granatowych.
Ndikanakutenga ndi kukulowetsa mʼnyumba ya amayi anga, amayi amene anandiphunzitsa, ndikanakupatsa vinyo wotsekemera kuti umwe, zotsekemera za makangadza.
3 Lewica jego pod głową moją, a prawicą swoją obłapia mię.
Mutu wanga watsamira dzanja lake lamanzere ndipo dzanja lake lamanja landikumbatira.
4 Poprzysięgam was, córki Jeruzalemskie! abyście nie budziły ani przerywały snu miłego mego, dokąd nie zechce.
Inu akazi a ku Yerusalemu, ndithu ndikukupemphani: musachigwedeze chikondi kapena kuchiutsa mpaka pamene chifunire ichocho.
5 Któraż to jest, co występuje z puszczy, podparłszy się miłego swego? Pod jabłonią wzbudziłam cię, tam cię poczęła matka twoja, tam cię poczęła rodzicielka twoja.
Kodi ndani uyo akutuluka ku chipululuyo, atatsamira wokondedwa wakeyo? Mkazi Ndinakudzutsa pa tsinde pa mtengo wa apulosi, pamenepo ndi pamene amayi anachirira, pamenepo ndi pamene wokubereka anamva ululu pokubala iweyo.
6 Przyłóż mię jako pieczęć na serce swoje, jako sygnet do ramienia swego! albowiem miłość mocna jest jako śmierć, twarda jako grób zawistna miłość; węgle jej jako węgle ogniste i jako płomień gwałtowny. (Sheol h7585)
Undiyike pamtima pako ngati chidindo, ngati chidindo cha pa dzanja lako; pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa, nsanje ndiyaliwuma ngati manda. Chikondi chimachita kuti lawilawi ngati malawi a moto wamphamvu. (Sheol h7585)
7 Wody wielkie nie mogłyby zagasić tej miłości, ani rzeki zatopić; choćby kto wszystkę majętność domu swego dał za takową miłość, byłby pewnie wzgardzony.
Madzi ochuluka sangachizimitse chikondi, mitsinje singachikokolole chikondicho. Ngati wina apereka chuma chonse cha mʼnyumba mwake chifukwa cha chikondi, adzangonyozeka nazo kotheratu.
8 Mamy sistrę maluczką, która jeszcze nie ma piersi. Cóż uczynimy z siostrą naszą w dzień, którego o niej mowa będzie?
Ife tili naye mlongo wathu wamngʼono, koma alibe mawere, kodi tidzamuchitira chiyani mlongo wathuyu pa tsiku limene adzamufunsire?
9 Jeźliże jest murem, zbudujmyż na niej pałac srebrny; a jeźli jest drzwiami, oprawmyż ją deszczkami cedrowymi.
Ngati iye ndi khoma, tidzamumangira nsanja ya siliva. Ngati iye ndi chitseko, tidzamutchinga ndi matabwa a mkungudza.
10 Jam jest mur, a piersi moje jako wieże. Wtenczas byłam przed oczyma jego, jako ta, która znajduje pokój.
Ine ndili ngati khoma, ndipo mawere anga ndi nsanja zake. Tsono mʼmaso mwa bwenzi langa ndine wobweretsa mtendere.
11 Winnicę miał Salomon w Baalhamon, którą winnicę najął stróżom, aby każdy przynosił za owoc jej tysiąc srebrników.
Solomoni anali ndi munda wampesa ku Baala-Hamoni; iyeyo anabwereketsa munda wamphesawo kwa alimi, aliyense mwa iwo ankayenera kupereka ndalama zasiliva 1,000 mʼmalo mwa zipatso zake.
12 Ale winnica moja, którą mam, jest przedemną. Miej sobie tysiąc srebrników, Salomonie, a dwieście ci którzy strzegą owocu jej.
Koma munda wanga wampesa ndi wangawanga ndiponso wa ine ndekha. Iwe Solomoni, khala nazo ndalama zasiliva 1,000 ndipo ndalama zasiliva 200 ndi za amene akusamalira mundawo.
13 O ty, która mieszkasz w ogrodach! przyjaciele słyuchają głosu twego; ozwijże mi się!
Iwe amene umakhala mʼminda uli pamodzi ndi anzako, ndilole kuti ndimve liwu lako!
14 Pospiesz się, miły mój! a bądź podobnym sarnie, albo młodemu jelonkowi na górach ziół wonnych.
Fulumira wokondedwa wanga, ndipo ukhale ngati gwape kapena mwana wa mbawala wothamanga mʼmapiri mʼmene mumamera mbewu zokometsera chakudya.

< Pieśń nad Pieśniami 8 >