< Psalmów 52 >

1 Przedniejszemu śpiewakowi pieśń Dawidowa nauczająca. Gdy przyszedł Doeg Edomczyk, i oznajmił Saulowi, mówiąc: Dawid przyszedł do domu Achimelechowego. Przeczże się chlubisz ze złości, o mocarzu! miłosierdzie Boże trwa każdego dnia.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe, ndakatulo ya Davide; pamene Doegi Mwedomu anapita kwa Sauli ndi kunena kuti “Davide wapita ku nyumba ya Ahimeleki.” Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira ndi zoyipa, iwe munthu wamphamvu? Nʼchifukwa chiyani ukudzitamandira tsiku lonse, iwe munthu wochititsa manyazi pamaso pa Mulungu?
2 Złe rzeczy myśli język twój, jako brzytwa ostra czyniąc zdradę.
Tsiku lonse umakhalira kuganizira za kuwononga ena; lilime lako lili ngati lumo lakuthwa, ntchito yako nʼkunyenga.
3 Umiłowałeś złe, bardziej niż dobre; kłamstwo raczej mówisz, niż sprawiedliwość. (Sela)
Iwe umakonda choyipa mʼmalo mwa kuyankhula choonadi. Umakonda kunama kupambana kuyankhula zoona. (Sela)
4 Umiłowałeś wszystkie słowa szkodliwe, i język zdradliwy.
Umakonda mawu onse opweteka, iwe lilime lachinyengo!
5 Przetoż cię Bóg zniszczy na wieki; porwie cię, i wyrwie cię z przybytku, i wykorzeni cię z ziemi żyjących. (Sela)
Zoonadi Mulungu adzakutsitsa kupita ku chiwonongeko chamuyaya: iye adzakukwatula ndi kukuchotsa mʼtenti yako; iye adzakuzula kuchoka mʼdziko la amoyo.
6 To widząc sprawiedliwi będą się bali, i będę się z niego naśmiewali, mówiąc:
Olungama adzaona zimenezi ndi kuchita mantha; adzamuseka nʼkumanena kuti,
7 Otoż człowiek, który nie pokładał w Bogu siły swojej; ale ufając w mnóstwie bogactw swoich, zmacniał się w złości swej.
“Pano tsopano pali munthu amene sanayese Mulungu linga lake, koma anakhulupirira chuma chake chambiri nalimbika kuchita zoyipa!”
8 Aleć ja będę jako oliwa zielona w domu Bożym, bom nadzieję położył w miłosierdziu Bożem na wieki wieczne.
Koma ine ndili ngati mtengo wa olivi wobiriwira bwino mʼnyumba ya Mulungu; ndimadalira chikondi chosatha cha Mulungu kwa nthawi za nthawi.
9 Będę cię wysławiał, Panie! na wieki, żeś to uczynił, a będę oczekiwał imienia twego, gdyż jest zacne przed oblicznością świętych twoich.
Ine ndidzakutamandani kwamuyaya chifukwa cha zimene mwachita; chifukwa cha zimene mwachita; mʼdzina lanu ndidzayembekezera pakuti dzina lanulo ndi labwino. Ndidzakutamandani pamaso pa oyera mtima anu.

< Psalmów 52 >