< Psalmów 47 >

1 Przedniejszemu śpiewakowi z synów Korego pieśń. Wszystkie narody klaskajcie rękoma, wykrzykajcie Bogu głosem wesela.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la ana a Kora. Ombani mʼmanja, inu anthu onse; fuwulani kwa Mulungu ndi mawu achimwemwe.
2 Albowiem Pan najwyższy, straszny, jest królem wielkim nad wszystką ziemią.
Ndi woopsadi Yehova Wammwambamwamba; Mfumu yayikulu ya dziko lonse lapansi!
3 Podbija ludzi pod moc naszę, a narody pod nogi nasze.
Iye anatigonjetsera mitundu yambirimbiri ya anthu; anayika anthu pansi pa mapazi athu.
4 Obrał nam za dziedzictwo nasze chwałę Jakóba, którego umiłował. (Sela)
Iye anatisankhira cholowa chathu, chonyaditsa cha Yakobo, amene anamukonda. (Sela)
5 Wstąpił Bóg z krzykiem; Pan wstąpił z głosem trąby.
Mulungu wakwera, anthu akumufuwulira mwachimwemwe, Yehova wakwera, akumuyimbira malipenga.
6 Śpiewajcież Bogu, śpiewajcie; śpiewajcież królowi naszemu, śpiewajcie.
Imbani matamando kwa Mulungu, imbani matamando; imbani matamando kwa mfumu yathu, imbani matamando.
7 Albowiem Bóg królem wszystkiej ziemi; śpiewajcież rozumnie.
Pakuti Mulungu ndi mfumu ya dziko lonse lapansi; imbirani Iye salimo la matamando.
8 Króluje Bóg nad narodami; Bóg siedzi na świętej stolicy swojej.
Mulungu akulamulira mitundu ya anthu; Mulungu wakhala pa mpando wake waufumu woyera.
9 Książęta narodów przyłączyli się do ludu Boga Abrahamowego; albowiem Boże są tarcze ziemskie; skąd on zacnie jest wywyższony.
Anthu otchuka mwa anthu a mitundu ina asonkhana monga anthu a Mulungu wa Abrahamu, pakuti mafumu a dziko lapansi ndi ake a Mulungu; Iye wakwezedwa kwakukulu.

< Psalmów 47 >