< Psalmów 19 >

1 Przedniejszemu śpiewakowi psalm Dawidowy. Niebiosa opowiadają chwałę Bożą, a dzieło rąk jego rozpostarcie oznajmuje.
Kwa mtsogoleri wa mayimbidwe. Salimo la Davide. Zakumwamba zimalengeza za ulemerero wa Mulungu; thambo limalalikira ntchito za manja ake.
2 Dzień dniowi podaje słowo, a noc nocy pokazuje umiejętność,
Tsiku ndi tsiku zimayankhula mawu ambiri, usiku ndi usiku zimaonetsa poyera nzeru.
3 Niemasz języka ani mowy, gdzieby głosu ich słychać nie było.
Palibe kuyankhula, palibe mawu aliwonse; liwu lawo silimveka.
4 Na wszystkę ziemię wyszedł porządek ich, a na kończyny okręgu ziemi słowa ich; słońcu na nich namiot wystawił.
Koma uthenga wawo umapita pa dziko lonse lapansi, mawuwo amafika mpaka kumalekezero a dziko lapansi.
5 A to jako oblubieniec wychodzi z łożnicy swojej; raduje się jako olbrzym, który ma bieżeć w drogę.
Dzuwa lili ngati mkwatibwi wobwera kuchokera ku nsanja yake, ngati katswiri wokondwerera kuthamanga pa mpikisano.
6 Wychodzi od kończyn niebios, a obchodzi je aż do kończyn ich, a niemasz nic, coby się mogło ukryć przed gorącem jego.
Limatuluka kuyambira mbali ina ya thambo ndi kuzungulira mpaka mbali inanso; palibe chinthu chotha kupewa kutentha kwake.
7 Zakon Pański jest doskonały, nawracający duszę; świadectwo Pańskie wierne, dawające mądrość nieumiejętnemu.
Lamulo la Yehova ndi langwiro, kutsitsimutsa moyo. Maumboni a Yehova ndi odalirika, amapereka nzeru kwa wopanda nzeru.
8 Przykazania Pańskie są prawe, uweselające serce; przykazanie Pańskie czyste, oświecające oczy.
Malangizo a Yehova ndi olungama, amapereka chimwemwe mu mtima. Malamulo a Yehova ndi onyezimira, amapereka kuwala.
9 Bojaźń Pańska czysta, trwająca na wieki; sądy Pańskie są prawdziwe, a przytem i sprawiedliwe;
Kuopa Yehova ndiye chinthu changwiro, chimakhala mpaka muyaya. Maweruzo a Yehova ndi owona ndipo onse ndi olungama;
10 Pożądliwsze nad złoto, i nad wiele najwyborniejszego złota, i słodsze nad miód i nad plastr miodowy.
ndi a mtengowapatali kuposa golide, kuposa golide weniweni; ndi otsekemera kuposa uchi, kuposa uchi wochokera pa chisa chake.
11 Sługa też twój bywa oświecony przez nie; a kto ich przestrzega, odnosi zapłatę wielką.
Mtumiki wanu amachenjezedwa nawo; powasunga pali mphotho yayikulu.
12 Ale występki któż zrozumie? od tajemnych występków oczyść mię.
Ndani angathe kudziwa zolakwa zake? Mundikhululukire zolakwa zanga zobisika.
13 I od swawolnych zachowaj sługę twego, aby nie panowali nademną; tedy doskonałym będę, a będę oczyszczony od przestępstwa wielkiego.
Muteteze mtumiki wanunso ku machimo ochita akudziwa; iwo asandilamulire. Kotero ndidzakhala wosalakwa, wopanda mlandu wa tchimo lalikulu.
14 Niechże będą przyjemne słowa ust moich, i rozmyślanie serca mego przed obliczem twojem, Panie, skało moja, i odkupicielu mój!
Mawu a mʼkamwa mwanga ndi zolingalira za mu mtima mwanga zikhale zokondweretsa pamaso panu, Inu Yehova, Thanthwe langa ndi Mpulumutsi wanga.

< Psalmów 19 >