< Psalmów 144 >

1 Pieśń Dawidowa. Błogosławiony Pan, skała moja, który ćwiczy ręce moje do bitwy, a palce moje do wojny.
Salimo la Davide. Atamandike Yehova Thanthwe langa, amene amaphunzitsa manja anga kuchita nkhondo; zala zanga kumenya nkhondo.
2 Miłosierdziem mojem, i twierdzą moją, ucieczką moją, wybawicielem moim, i tarczą moją on mi jest, przetoż w nim ufam; onci podbija pod mię lud mój.
Iye ndiye Mulungu wanga wachikondi ndi malo anga otetezedwa, linga langa ndi mpulumutsi wanga, chishango changa mmene ine ndimathawiramo, amene amagonjetsa mitundu ya anthu pansi panga.
3 Panie! cóż jest człowiek, że nań masz baczenie? a syn człowieczy, że go sobie poważasz?
Inu Yehova, munthu nʼchiyani kuti mumamusamalira, mwana wa munthu kuti muzimuganizira?
4 Człowiek marności jest podobny; dni jego jako cień pomijający.
Munthu ali ngati mpweya; masiku ake ali ngati mthunzi wosakhalitsa.
5 Panie! nakłoń niebios twoich, a zstąp; dotknij się gór, a zakurzą się.
Ngʼambani mayiko akumwamba, Inu Yehova, ndipo tsikani pansi; khudzani mapiri kuti atulutse utsi.
6 Zabłyśnij błyskawicą, a rozprosz ich; puść strzały twoje, a poraź ich.
Tumizani zingʼaningʼani ndi kubalalitsa adani; ponyani mivi yanu ndi kuwathamangitsa.
7 Ściągnij rękę swą z wysokości; wybaw mię, a wyrwij mię z wód wielkich, z ręki cudzoziemców.
Tambasulani dzanja lanu kuchokera kumwamba; landitseni ndi kundipulumutsa, ku madzi amphamvu, mʼmanja mwa anthu achilendo,
8 Których usta kłamstwo mówią, a prawica ich, prawica omylna.
amene pakamwa pawo ndi podzala ndi mabodza, amene dzanja lawo lamanja ndi lachinyengo.
9 Boże! pieśń nową tobie zaśpiewam; na lutni, i na instrumencie o dziesięciu stronach śpiewać ci będę.
Ndidzakuyimbirani nyimbo yatsopano Inu Mulungu; ndidzakuyimbirani nyimbo pa zeze wa nsambo khumi,
10 Bóg daje zwycięstwo królom, a Dawida, sługę swego, wybawia od miecza srogiego.
kwa Iye amene amapambanitsa mafumu, amene amapulumutsa Davide mtumiki wake ku lupanga loopsa.
11 Wybawże mię, a wyrwij mię z ręki cudzoziemców, których usta mówią kłamstwo, a prawica ich prawica omylna;
Landitseni ndi kundipulumutsa, mʼmanja mwa anthu achilendo, amene pakamwa pawo ndi podzaza ndi mabodza, amene dzanja lawo lamanja ndi lachinyengo.
12 Aby synowie nasi byli jako szczepy rosnące w młodości swojej, a córki nasze, jako kamienie węgielne, wyciosane w budynku kościelnym.
Ndipo ana aamuna pa chinyamata chawo adzakhala ngati mbewu yosamalidwa bwino, ana athu aakazi adzakhala ngati zipilala zosemedwa bwino, zokongoletsera nyumba yaufumu.
13 Szpiżarnie nasze pełne niech wydawają wszelakie potrzeby; trzody nasze niech rodzą tysiące, niech rodzą dziesięć tysięcy w oborach naszych.
Nkhokwe zathu zidzakhala zodzaza ndi zokolola za mtundu uliwonse. Nkhosa zathu zidzaswana miyandamiyanda pa mabusa athu.
14 Woły nasze niech będą tłuste; niech nie będzie wtargnienia, ani zajęcia, ani narzekania po ulicach naszych.
Ngʼombe zathu zidzanyamula katundu wolemera. Sipadzakhala mingʼalu pa makoma, sipadzakhalanso kupita ku ukapolo, mʼmisewu mwathu simudzakhala kulira chifukwa cha mavuto.
15 Błogosławiony lud, któremu się tak dzieje. Błogosławiony lud, którego Bogiem jest Pan.
Odala anthu amene adzalandira madalitso awa; odala anthu amene Mulungu wawo ndi Yehova.

< Psalmów 144 >