< Psalmów 128 >

1 Pieśń stopni. Błogosławiony wszelki, który się boi Pana, który chodzi drogami jego.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Odala ndi onse amene amaopa Yehova, amene amayenda mʼnjira zake.
2 Bo prace rąk twoich pożywać będziesz; błogosławionym będziesz, i będzieć się dobrze działo.
Udzadya chipatso cha ntchito yako; madalitso ndi chuma zidzakhala zako.
3 Żona twoja będzie jako winna macica płodna po bokach domu twego; dziatki twoje jako latorośle oliwne około stołu twego.
Mkazi wako adzakhala ngati mpesa wobereka mʼkati mwa nyumba yako; ana ako adzakhala ngati mphukira za mitengo ya olivi kuzungulira tebulo lako.
4 Oto takci będzie ubłogosławiony mąż, który się boi Pana.
Ameneyu ndiye munthu wodalitsidwa amene amaopa Yehova.
5 Niechżeć Pan błogosławi z Syonu, abyś patrzył na dobro Jeruzalemskie po wszystkie dni żywota twego.
Yehova akudalitse kuchokera mʼZiyoni masiku onse a moyo wako; uwone zokoma za Yerusalemu,
6 I oglądał synów synów twoich, i pokój nad Izraelem.
ndipo ukhale ndi moyo kuti udzaone zidzukulu zako. Mtendere ukhale ndi Israeli.

< Psalmów 128 >