< Psalmów 126 >

1 Pieśń stopni. Gdy zaś Pan nawrócił pojmanych z Syonu, byliśmy jako ci, którym się śni.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Yehova atabwezera akapolo ku Ziyoni, tinali ngati amene akulota.
2 Tedy były napełnione weselem usta nasze, a język nasz radością; tedy mówiono między narodami: Wielmożne rzeczy Pan uczynił z nimi.
Pakamwa pathu panadzaza ndi kuseka; malilime athu ndi nyimbo zachimwemwe. Pamenepo kunanenedwa pakati pa anthu kuti, “Yehova wawachitira zinthu zazikulu.”
3 Wielmożne rzeczy Pan uczynił z nami, z czegośmy się bardzo uradowali.
Yehova watichitira zinthu zazikulu, ndipo tadzazidwa ndi chimwemwe.
4 Przywróćże zaś, o Panie! pojmanie nasze, jako strumienie na południe.
Tibwezereni madalitso athu, Inu Yehova, monga mitsinje ya ku Negevi.
5 Którzy siali ze łzami, żąć będą z wykrzykaniem;
Iwo amene amafesa akulira, adzakolola akuyimba nyimbo zachimwemwe.
6 Tam i sam chodząc z płaczem rozsiewa lud drogie nasienie; ale zaś przyszedłszy z radością znosić będzie snopy swoje.
Iye amene amayendayenda nalira, atanyamula mbewu yokafesa, adzabwerera akuyimba nyimbo zachimwemwe, atanyamula mitolo yake.

< Psalmów 126 >