< Psalmów 120 >
1 Pieśń stopni. Wołałem do Pana w utrapieniu mojem, a wysłuchał mię.
Nyimbo yoyimba pokwera ku Yerusalemu. Ndimafuwulira kwa Yehova mʼmasautso anga, ndipo Iye amandiyankha.
2 Wyzwól, Panie! duszę moję od warg kłamliwych, i od języka zdradliwego.
Pulumutseni Yehova ku milomo yabodza, ndi kwa anthu achinyengo.
3 Cóż ci da, albo coć za pożytek przyniesie język zdradliwy?
Kodi adzakuchitani chiyani, ndipo adzawonjezerapo zotani, inu anthu achinyengo?
4 Który jest jako strzały ostre mocarza, i jako węgle jałowcowe.
Adzakulangani ndi mivi yakuthwa ya munthu wankhondo, ndi makala oyaka a mtengo wa tsanya.
5 Niestetyż mnie, żem tak długo gościem w Mesech, a mieszkam w namiotach Kedarskich.
Tsoka ine kuti ndimakhala ku Mesaki, kuti ndimakhala pakati pa matenti a ku Kedara!
6 Długo mieszka dusza moja między tymi, którzy pokój mają w nienawiści.
Kwa nthawi yayitali ndakhala pakati pa iwo amene amadana ndi mtendere.
7 Jać radzę do pokoju; ale gdy o tem mówię, oni do wojny.
Ine ndine munthu wamtendere; koma ndikamayankhula, iwo amafuna nkhondo.