< Psalmów 111 >

1 Halleluja. Będę wysławiał Pana całem sercem w radzie szczerych, i w zgromadzeniu.
Tamandani Yehova. Ndidzathokoza Yehova ndi mtima wanga wonse mʼbwalo la anthu olungama mtima ndi pa msonkhano.
2 Wielkie sprawy Pańskie, jawne u wszystkich, którzy się w nich kochają.
Ntchito za Yehova nʼzazikulu; onse amene amakondwera nazo amazilingalira.
3 Chwalebne i ozdobne dzieło jego, a sprawiedliwość jego trwa na wieki.
Zochita zake ndi za ulemerero ndi zaufumu, ndipo chilungamo chake ndi chosatha.
4 Pamiątkę cudów swoich uczynił miłosierny a litościwy Pan.
Iye wachititsa kuti zodabwitsa zake zikumbukirike; Yehova ndi wokoma mtima ndi wachifundo.
5 Dał pokarm tym, którzy się go boją, pamiętając wiecznie na przymierze swoje.
Amapereka chakudya kwa amene amamuopa Iye; amakumbukira pangano lake kwamuyaya.
6 Moc spraw swoich oznajmił ludowi swemu, dawszy im dziedzictwo pogan.
Waonetsa anthu ake mphamvu ya ntchito zake, kuwapatsa mayiko a anthu a mitundu ina.
7 Uczynki rąk jego prawda i sąd; nieodmienne są wszystkie przykazania jego,
Ntchito za manja ake ndi zokhulupirika ndi zolungama; malangizo ake onse ndi odalirika.
8 Utwierdzone na wieki wieczne, uczynione w prawdzie i w szczerości.
Malamulo ndi okhazikika ku nthawi za nthawi, ochitidwa mokhulupirika ndi molungama.
9 Wykupienie posławszy ludowi swemu, przykazał na wieki strzedź przymierza swego; święte i straszne jest imię jego.
Iyeyo amawombola anthu ake; anakhazikitsa pangano lake kwamuyaya dzina lake ndi loyera ndi loopsa.
10 Początek mądrości jest bojaźń Pańska; rozumu dobrego nabywają wszyscy, którzy rozkazanie Pańskie czyną; chwała jego trwa na wieki.
Kuopa Yehova ndicho chiyambi cha nzeru; onse amene amatsatira malangizo ake amamvetsa bwino zinthu. Iye ndi wotamandika mpaka muyaya.

< Psalmów 111 >