< Kapłańska 11 >

1 Potem mówił Pan do Mojżesza i do Aarona, i rzekł do nich: Powiedzcie synom Izraelskim, mówiąc:
Yehova anayankhula ndi Mose ndi Aaroni kuti,
2 Te są zwierzęta, które jeść będziecie ze wszystkich zwierząt, które są na ziemi,
“Awuze Aisraeli kuti, ‘Nyama zomwe mukhoza kudya mwa nyama zonse za dziko lapansi ndi izi:
3 Wszelkie bydlę, które ma rozdzielone stopy, i rozdwojone kopyta, a przeżuwa, to jeść będziecie.
Nyama iliyonse imene ili ndi chipondero chogawikana pakati ndi yobzikula mukhoza kudya.
4 Ale z tych jeść nie będziecie, które tylko przeżuwają, i z tych, które tylko kopyta dwoją: Wielbłąd, który choć przeżuwa, ale kopyta rozdzielonego nie ma, nieczystym wam będzie.
“‘Koma pali nyama zina zimene zimabzikula kokha kapena ndi zogawikana zipondero zimene simukuyenera kudya. Nyama zimenezi ndi ngamira, ngakhale imabzikula ilibe zipondero zogawikana. Choncho ndi yodetsedwa, musadye.
5 Także królik, który choć przeżuwa, ale kopyta rozdzielonego nie ma, nieczystym wam będzie.
Ina ndi mbira, ngakhale imabzikula, zipondero zake nʼzosagawikana. Choncho ndi yodetsedwa, musadye.
6 Zając też, choć przeżuwa, ale kopyta rozdzielonego nie ma, nieczystym wam będzie.
Inanso ndi kalulu, ngakhale amabzikula, zipondero zake nʼzosagawikana. Choncho ndi wodetsedwa, musadye.
7 Świnia także, choć ma rozdzielone stopy i rozdwojone kopyto, ale iż nie przeżuwa, nieczystą wam będzie.
Nkhumba simabzikula ngakhale ili ndi zipondero zogawikana. Choncho ndi yodetsedwa, musadye.
8 Mięsa ich nie będziecie jeść, ani ścierwu ich dotykać się będziecie, nieczyste wam będą.
Musamadye nyama yake kapena kukhudza imene yafa chifukwa ndi yodetsedwa.
9 To jeść będziecie ze wszystkich rzeczy żyjących w wodach, wszystko co ma skrzele i łuskę, w wodach, w morzu, i w rzekach, to jeść będziecie.
“‘Mwa zamoyo zonse zimene zimakhala mʼmadzi a mʼnyanja ndi a mʼmitsinje mukhoza kudya chilichonse chimene chili ndi minga ya pa msana ndi mamba.
10 Wszystko zaś, co nie ma skrzeli i łuski w morzu i w rzekach, cokolwiek się rucha w wodach i każda rzecz żywiąca, która jest w wodach obrzydliwością wam będzie.
Koma zamoyo zonse za mʼnyanja kapena za mʼmitsinje zimene zilibe minga ya pa msana ndi mamba, kaya ndi tizirombo tonse ta mʼmadzi ndi zamoyo zonse zopezeka mʼmenemo ndi zodetsedwa kwa inu.
11 Obrzydliwością będą wam; mięsa ich jeść nie będziecie, a ścierwem ich brzydzić się będziecie.
Pakuti zimenezi ndi zodetsedwa kwa inu, nyama yake musadye, ndipo zikafa zikhalebe zodetsedwa kwa inu.
12 Owa cokolwiek nie ma skrzeli i łuski w wodach, obrzydliwością wam będzie.
Chamoyo chilichonse cha mʼmadzi chimene chilibe minga ya pa msana kapena mamba ndi chodetsedwa kwa inu.
13 Tem się też brzydzić będzie z ptastwa, i jeść ich nie będziecie, bo są obrzydliwością; jako orła, i gryfa, i morskiego orła,
“‘Mbalame zimene simukuyenera kudya chifukwa ndi zodetsedwa ndi izi: mphungu, nkhwazi, mwimba,
14 I sępa, i kani, według rodzaju ich;
nankapakapa, akamtema a mitundu yonse,
15 Każdego kruka według rodzaju jego;
akhungubwi a mitundu yonse,
16 Także strusia, i sowy i wodnej kani i jastrzębia, według rodzaju ich;
kadzidzi wamphondo, kadzidzi wodzuma, chipudo ndi mtundu uliwonse wa akabawi
17 I puchacza, i norka i lelka,
kadzidzi wamngʼono, chiswankhono ndi mantchichi,
18 I łabędzia, i bąka, i bociana,
tsekwe, vuwo, dembo,
19 I czapli, i sojki, według rodzaju ich, i dudka, i nietoperza.
indwa, zimeza za mitundu yonse, nsadzu ndi mleme.
20 Wszystko, co się czołga po ziemi skrzydła mając, a na czterech nogach chodzi, obrzydliwością wam będzie.
“‘Zowuluka zonse za miyendo inayi ndi zodetsedwa.
21 Wszakże jeść będziecie wszystko, co się czołga po ziemi skrzydła mające, co na czterech nogach chodzi, co ma w nogach ścięgneczka przedłuższe ku skakaniu na nich po ziemi.
Komabe mwa zowuluka zokhala ndi miyendo inayi zimene mukhoza kudya ndi zokhazo zimene zili ndi miyendo yolumphira.
22 Te z nich jeść będziecie: Szarańczą według rodzaju jej, i koniki według rodzaju ich, i skoczki według rodzaju ich, i chrząszcze według rodzaju ich.
Pa zimenezo mungathe kudya izi: dzombe la mitundu yonse, atsokonombwe a mitundu yonse, nkhululu za mitundu yonse, ndi ziwala za mitundu yonse.
23 Wszystko zaś, co się czołga po ziemi skrzydlaste, cztery nogi mające, obrzydliwością wam będzie;
Koma za mapiko zina zonse zokhala ndi miyendo inayi muzitenge kukhala zodetsedwa kwa inu.
24 Bo się niemi pokalacie. Kto by się dotknął zdechliny ich, nie będzie czystym aż do wieczora;
“‘Zimenezi zidzakudetsani. Aliyense wozikhudza zitafa adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo.
25 A ktobykolwiek nosił ścierw ich, upierze szaty swoje, i będzie nieczystym aż do wieczora.
Aliyense wonyamula chiwalo chilichonse cha nyama zakufazo ayenera kuchapa zovala zake, ndipo adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo.
26 Wszelkie bydlę, które ma rozdzieloną stopę, a kopyta rozdwojonego nie ma, ani też przeżuwa, nieczyste wam będzie; kto by się go dotknął, nieczystym będzie.
“‘Nyama iliyonse imene ili ndi ziboda zogawikana koma mapazi ake wosagawikana, kapena imene sibzikula muyiyese yodetsedwa kwa inu ndipo munthu aliyense akakhudza nyama yakufayo, adzakhala wodetsedwa.
27 A cokolwiek chodzi na łapach swych ze wszystkich zwierząt, które chodzą na czterech nogach, nieczyste wam będzie; kto by się dotknął ścierwu ich, nieczystym będzie aż do wieczora.
Mwa nyama zonse zoyenda ndi miyendo inayi, nyama zonse zokhala ndi zikhadabo kuphazi muzitenge kukhala zodetsedwa ndipo aliyense wozikhudza zitafa adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo.
28 A kto by nosił ścierw ich, upierze odzienie swe, a nieczystym będzie aż do wieczora, bo nieczyste wam są.
Aliyense wonyamula nyamazi zitafa ayenera kuchapa zovala zake, ndipo adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Zimenezi ndi zodetsedwa kwa inu.
29 Także i te za nieczyste mieć będziecie między płazami, które się włóczą po ziemi, łasica, i mysz, i żaba według rodzajów swoich;
“‘Mwa nyama zokwawa, zimene zili zodetsedwa kwa inu ndi izi: likongwe, mbewa, msambulu za mitundu yonse,
30 I jeż, i jaszczurka, i tchórz, i ślimak, i kret.
gondwa, mngʼazi, buluzi, dududu ndi nanzikambe.
31 Te nieczyste wam będą między wszystkiemi płazami; kto by się dotknął zdechliny ich, nieczystym będzie aż do wieczora.
Mwa nyama zonse zoyenda pansi, zimenezi ndi zodetsedwa kwa inu. Munthu aliyense wozikhudza zitafa adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo.
32 A każda rzecz, na którą by co zdechłego z tych rzeczy upadło, nieczysta będzie, tak drzewiane naczynie, jako szata, tak skóra, jako wór; owa każde naczynie, w którem co sprawują, do wody włożone będzie, i nieczyste zostanie aż do wieczora, potem czyste będzie.
Iliyonse mwa nyama zimenezi ikafa ndi kugwera pa chiwiya chilichonse, kaya chimagwira ntchito yotani, kaya ndi chopangidwa ndi mtengo, kaya ndi cha nsalu, kaya ndi cha chikopa kapena chiguduli chiwiyacho chidzakhala chodetsedwa. Muchiviyike mʼmadzi chiwiyacho komabe chidzakhala chodetsedwa mpaka madzulo, ndipo kenaka chidzakhala choyeretsedwa.
33 Wszelkie zaś naczynie gliniane, w które by co z tych rzeczy wpadło, ze wszystkiem, coby w niem było, nieczyste się stanie, a samo stłuczone będzie.
Tsono nyama ina iliyonse mwa zimenezi ikagwera mʼmbiya ya dothi, ndiye kuti chilichonse cha mʼmbiyamo chidzakhala chodetsedwa, ndipo muyenera kuswa mbiyayo.
34 Każda też potrawa, którą jadają, gdyby wody nieczystej do niej wlano, nieczystą będzie; i wszelki napój, który pijają z każdego takiego naczynia, nieczystym będzie.
Chakudya chilichonse chimene mungadye chikakhala kuti chathiridwa mʼmbiyamo, ndiye kuti chakudyacho chidzakhala chodetsedwa, ndipo madzi akumwa wochokera mʼmbiya zotere ndi wodetsedwa.
35 Owa wszystko, na coby upadło co z onych zdechlin, nieczyste będzie; piec i ognisko rozwalone będą, bo nieczyste są, i za nieczyste wam będą.
Chiwalo chilichonse cha nyama yakufa chikagwera pa chinthu chilichonse kaya pa uvuni, kapena pa mʼphika, ndiye kuti zinthuzo zidzakhala zodetsedwa, ndipo ziphwanyidwe popeza ndi zodetsedwa.
36 Ale studnia i cysterna, i każde zgromadzenie wód czyste będą; coby się jednak dotknęło ścierwu tych rzeczy, nieczyste będzie.
Koma kasupe kapena chitsime chamadzi chidzakhala choyeretsedwa ngakhale kuti chilichonse chokhudza nyama yakufayo chidzakhala chodetsedwa. Zimenezi muzitenge kukhala zodetsedwa.
37 A jeźliby upadło nieco z ścierwu ich na jakie nasienie, które siane bywa, czyste zostanie.
Chiwalo chilichonse cha nyama yakufayo chikagwera pa mbewu zimene akuti adzale, mbewu zimenezo zidzakhalabe zabwino.
38 Ale jeźliby na nasienie w wodzie moczone upadło co z ścierwu ich, nieczyste wam będzie.
Koma mbewuzo zikakhala zonyowa ndi madzi, ndipo chiwalo chilichonse cha nyama zakufazo chikagwera pa mbewuzo, mbewuzo zikhale zodetsedwa kwa inu.
39 Jeźliby zdechło bydlę, które jadacie: kto by się dotknął ścierwu jego, nieczystym będzie aż do wieczora.
“‘Ngati nyama imene mumaloledwa kudya yafa yokha, ndiye kuti aliyense wokhudza nyama yakufayo adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo.
40 A kto by jadł ścierw jego, upierze szaty swoje, i nieczystym będzie aż do wieczora; ten, coby precz wynosił on ścierw, upierze szaty swoje, i nieczystym będzie aż do wieczora.
Aliyense amene adyako nyama yakufayo achape zovala zake, ndipo adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo. Aliyense amene wanyamula nyama yakufayo ayenera kuchapa zovala zake, ndipo adzakhala wodetsedwa mpaka madzulo.
41 Wszelki także płaz, co się czołga po ziemi, obrzydliwością jest; nie będziecie go jeść.
“‘Chinthu chilichonse chokwawa pansi ndi chonyansa, simuyenera kudya.
42 Cokolwiek się czołga po brzuchu, i cokolwiek na czterech albo więcej nogach się włóczy między wszystkim płazem, który się czołga po ziemi, nie będziecie ich jeść, bo obrzydliwością są.
Musadye chilichonse chokwawa pansi, choyenda chamimba kapena choyenda ndi miyendo inayi kapenanso yambiri popeza ndi chodetsedwa.
43 Nie plugawcie dusz waszych wszelkim płazem, który się czołga po ziemi, i nie mażcie się niemi, byście nie byli splugawieni przez nie;
Musadzisandutse nokha odetsedwa ndi chokwawa chilichonse. Musadziyipitse nazo, kuti mukhale odetsedwa.
44 Albowiem Jam jest Pan Bóg wasz: przetoż poświęcajcie się, a bądźcie świętymi, bom Ja święty jest; a nie plugawcie dusz waszych żadnym płazem, który się czołga po ziemi.
Ine ndine Yehova Mulungu wanu, choncho dziyeretseni kuti mukhale woyera, chifukwa Ine ndine woyera. Musadzisandutse odetsedwa ndi chokwawa chilichonse.
45 Bom Ja jest Pan, którym was wywiódł z ziemi Egipskiej, abym wam był za Boga; przetoż bądźcie świętymi, bom Ja święty jest.
Ine ndine Yehova amene ndinakutulutsani ku Igupto kuti ndikhale Mulungu wanu. Tsono mukhale woyera, chifukwa Ine ndine woyera.
46 Tać jest ustawa około bydła, i ptastwa, i wszelkiej duszy żywej, która się rucha w wodach, i wszelkiej duszy żywej, która się czołga po ziemi.
“‘Amenewa ndi malamulo onena za nyama, mbalame, chamoyo chilichonse choyenda mʼmadzi ndiponso chamoyo chilichonse chokwawa.
47 Ku rozeznaniu między nieczystem i między czystem, a między zwierzęty, które się jeść godzi, i między zwierzęty, których się jeść nie godzi.
Muzisiyanitsa pakati pa chodetsedwa ndi choyeretsedwa, komanso pakati pa zomwe mutha kudya ndi zomwe simuyenera kudya.’”

< Kapłańska 11 >