< Jeremiasza 21 >

1 Słowo, które się stało do Jeremijasza od Pana, gdy do niego król Sedekijasz posłał Fassura, syna Malchyjaszowego, i Sofonijasza, syna Maasejaszowego, kapłana, aby rzekli:
Mfumu Zedekiya inatuma Pasuri mwana wa Malikiya ndi wansembe Zefaniya mwana wa Maseya kwa Yeremiya.
2 Poradź się, proszę, o nas Pana; bo Nabuchodonozor, król Babiloński, walczy przeciwko nam: owa snać uczyni Pan z nami według wszystkich dziwnych spraw swoich, żeby odciągnął od nas.
Iwo amati akanene kwa Yeremiya mawu akuti, “Tinenere kwa Yehova chifukwa Nebukadinezara mfumu ya Babuloni akutithira nkhondo. Mwina mwake Yehova nʼkutichitira zodabwitsa kuti Nebukadinezarayo achoke kwathu kuno.”
3 I rzekł Jeremijasz do nich: Tak powiedzcie Sedekijaszowi:
Koma Yehova anawuza Yeremiya kuti ayankhe Pasuri ndi Zefaniya kuti, “Kamuwuzeni Zedekiya kuti,
4 Tak mówi Pan, Bóg Izraelski: Oto Ja odwrócę naczynia wojenne, które są w rękach waszych, i któremi wy walczycie przeciw królowi Babilońskiemu, i Chaldejczykom, którzy was oblegli około muru, i zgromadzę ich w pośrodek miasta tego.
‘Yehova, Mulungu wa Israeli akuti ndikulandeni zida zimene zili mʼmanja mwanu zimene mukugwiritsa ntchito polimbana ndi mfumu ya ku Babuloni ndi ankhondo ake amene akuzingani kunja kwa lingali. Ndipo ndidzasonkhanitsa zidazo mʼkati mwa mzindawu.
5 A Ja sam walczyć będę przeciwko wam ręką wyciągnioną i ramieniem możnem, a to w gniewie, i w popędliwości, i w zapalczywości wielkiej;
Ineyo mwini wakene ndi mkono wotambasula ndi dzanja lamphamvu, ndidzachita nanu nkhondo ndili wokwiya, wokalipa ndi waukali.
6 I uderzę obywateli tego miasta, tak, że i ludzie i bydlęta morem wielkim pomrą.
Ndidzakantha amene amakhala mu mzinda muno, anthu pamodzi ndi zirombo, ndipo zidzafa ndi mliri woopsa.
7 A potem, tak mówi Pan, podam Sedekijasza, króla Judzkiego, i sługi jego, i lud, to jest tych, którzy pozostaną w tem mieście po morze, i po mieczu, i po głodzie, w rękę Nabuchodonozora, króla Babilońskiego i w rękę nieprzyjaciół ich, a tak w rękę szukających duszy ich, który ich pobije ostrzem miecza: nie przepuści im, ani im sfolguje, ani się zmiłuje.
Pambuyo pake, ndidzapereka Zedekiya mfumu ya ku Yuda, nduna zake pamodzi ndi anthu a mu mzinda muno amene adzapulumuke pa nthawi ya mliri, lupanga ndi njala kwa Nebukadinezara mfumu ya ku Babuloni ndi kwa adani awo amene ankafuna kuwapha. Iye adzawapha ndi lupanga. Sadzawachitira chifundo kapena kuwamvera chisoni kapenanso kuwakomera mtima.’
8 Przetoż rzecz do ludu tego: Tak mówi Pan: Oto ja kładę przed wami drogę żywota i drogę śmierci.
“Yehova anati ndiwawuzenso anthu amenewa kuti asankhe pakati pa moyo ndi imfa.
9 Ktokolwiek zostanie w tem mieście, zginie od miecza, albo od głodu, albo od moru: ale kto wyjdzie i poda się Chaldejczykom, którzy was oblegli, pewnie żyw zostanie, i będzie mu dusza jego w korzyści.
Aliyense amene akhale mu mzinda muno adzaphedwa ndi lupanga, njala kapena mliri. Koma aliyense amene apite kukadzipereka kwa Ababuloni amene akuzinganiwa adzakhala ndi moyo, adzapulumuka.
10 Bom obrócił oblicze moje przeciwko temu miastu ku złemu, a nie ku dobremu, mówi Pan. W rękę króla Babilońskiego podane będzie, i spali je ogniem.
Ine ndatsimikiza kuchitira mzinda uno choyipa osati chabwino, akutero Yehova. Udzaperekedwa mʼdzanja la mfumu ya ku Babuloni, ndipo iyeyo adzawutentha ndi moto.
11 Ale domowi króla Judzkiego rzecz: Słuchajcie słowa Pańskiego.
“Komanso, uwuze banja laufumu la Yuda kuti, ‘Imva mawu a Yehova;
12 O domie Dawidowy! Tak mówi Pan: Odprawujcie sąd każdego poranku, a wyrywajcie uciśnionego z ręki gwałtownika, by snać nie wyszła jako ogień zapalczywość moja, a nie gorzała, tak, żeby nie był, ktoby ugasił dla złości spraw waszych.
inu a mʼbanja la Davide, Yehova akuti, “‘Weruzani mwachilungamo mmawa uliwonse; pulumutsani mʼdzanja la wozunza aliyense amene walandidwa katundu wake, kuopa kuti ukali wanga ungabuke ndi kuyaka ngati moto wosazimitsika chifukwa cha zoyipa zimene mwachita.
13 Otom Ja przeciwko tobie, która mieszkasz w tej dolinie, jako skała w tej równinie, mówi Pan, którzy mówicie: Któż przyciągnie na nas? a kto wnijdzie do przybytków naszych?
Ndidzalimbana nanu, inu amene mukukhala pamwamba pa chigwa, inu okhala ngati thanthwe lapachidikha, akutero Yehova. Inu amene mumanena kuti, ‘Ndani amene angabwere kudzalimbana nafe? Ndani amene angathe kulowa mʼmalinga mwathu?’
14 Bo was nawiedzę według owocu spraw waszych, mówi Pan; a rozniecę ogień w lesie twoim, który pożre wszystko około niego.
Ndidzakulangani molingana ndi ntchito zanu, akutero Yehova. Ndidzatentha nkhalango zanu; moto udzapsereza zonse zimene zakuzungulirani.’”

< Jeremiasza 21 >