< Jeremiasza 15 >

1 Tedy rzekł Pan do mnie: Choćby stanął Mojżesz i Samuel przed obliczem mojem, nie miałbym serca do ludu tego; puść ich od oblicza mego, a niech precz idą.
Kenaka Yehova anandiwuza kuti, “Ngakhale Mose ndi Samueli akanayima pamaso panga kupempherera anthu awa, Ine sindikanawachitira chisoni. Achotseni ndipo ndisawaonenso! Aleke apite!
2 A jeźliby rzekli: Dokądże pójdziemy? Tedy im rzeczesz: Tak mówi Pan: Kto oddany na śmierć, na śmierć pójdzie; a kto pod miecz, pod miecz; a kto na głód, na głód; a kto w niewolę, w niewolę.
Ndipo ngati akufunsa iwe kuti, ‘Kodi tipite kuti?’ uwawuze kuti, ‘Yehova akuti, “‘Oyenera kufa adzafa; oyenera kufa ndi lupanga adzafa ndi lupanga; oyenera kufa ndi njala adzafa ndi njala; oyenera kupita ku ukapolo adzapita ku ukapolo.’
3 Bo ich tą czworaką rzeczą nawiedzę, mówi Pan: Mieczem na zamordowanie, i psami na rozszarpanie, i ptastwem niebieskiem, i zwierzętami ziemskiemi na pożarcie i na wygubienie.
“Ine ndidzawatumizira mitundu inayi ya zinthu zowononga,” akutero Yehova, “lupanga lowapha, agalu owaluma, mbalame zamumlengalenga ndiponso zirombo zoti ziwadye ndi kuwawononga.
4 I podam ich na potłukanie się po wszystkich królestwach ziemi dla Manasesa, syna Ezechijasza, króla Judzkiego, za to, co uczynił w Jeruzalemie.
Ndidzawasandutsa kukhala chinthu chonyansa kwa anthu a maufumu onse a dziko lapansi chifukwa cha zimene Manase mwana wa Hezekiya mfumu ya Yuda anachita mu Yerusalemu.
5 Bo któżby się zmiłował nad tobą? Jeruzalemie! albo ktoby się użalił nad tobą? albo ktoby przyszedł, aby się pytał, jakoć się powodzi?
“Kodi adzakumvera chisoni ndani, Yerusalemu? Kodi adzakulira ndani? Kodi ndani amene adzapatuka kufunsa za moyo wako?
6 Tyś mię opuściło, mówi Pan, poszłoś nazad. Przetoż wyciągnę rękę moję na cię, abym cię wytracił; ustałem od żalu.
Inu mwandikana Ine,” akutero Yehova. “Inu mukubwererabe mʼmbuyo. Choncho Ine ndidzakukanthani. Ndatopa ndi kukuchitirani chifundo.
7 Przetoż ich rozwieję wiejaczką po bramach tej ziemi, osierocę i wygubię ich; bo się od dróg swoich nie nawracali.
Ine ndidzakubalalitsani kukuchotsani mʼmizinda ya mʼdzikomo monga mmene amachitira ndi mankhusu popeta ndi lichero. Anthu anga ndinawaliritsa ndi kuwawononga chifukwa sanasinthe makhalidwe awo oyipa.
8 Więcej się namnoży wdów jego, niż piasku morskiego; przywiodę na nich, na matki, na młodzieńców burzyciela i w południe; sprawię, że przypadną nagle na to miasto; i będą przestraszeni.
Ndinachulukitsa amayi awo amasiye kupambana mchenga wa kunyanja. Amayiwo ndinawawonongera ana awo aamuna dzuwa lili pamutu. Mwadzidzidzi ndinawagwetsera kuwawa mtima ndi mantha.
9 Zemdleje i ta, która rodziła po siedmiorgu, wypuści duszę swoję, zajdzie jej słońce jeszcze za dnia, zapłonie i wstydzić się będzie; a ostatek ich dam pod miecz przed obliczem nieprzyjaciół ich, mówi Pan.
Mayi wa ana asanu ndi awiri wakomoka ndipo akupuma wefuwefu. Dzuwa lake lalowa ukanali usana; anamuchititsa manyazi ndipo wathedwa nzeru. Otsala ndidzawapereka mʼmanja mwa adani awo kuti awaphe ndi lupanga,” akutero Yehova.
10 Biada mnie, matko moja! żeś mię urodziła męża swaru, i męża sporu po wszystkiej ziemi; nie dawałem im na lichwę, ani mnie oni na lichwę dawali, a wżdy mi każdy złorzeczy.
Kalanga ine, amayi pakuti munandibereka ine, munthu amene ndikutsutsana ndi kulimbana ndi anthu pa dziko lonse! Ine sindinakongoze kapena kukongola kanthu, komatu aliyense akunditemberera.
11 I rzekł Pan: Izali tobie, który pozostaniesz, nie będzie dobrze? Izali się nie zastawię o cię nieprzyjacielowi czasu utrapienia i czasu ucisku?
Yehova anati, “Ndithudi, Ine ndidzakulanditsa kuti upeze bwino. Ndithudi, adani ako adzakupempha pa nthawi ya tsoka ndi ya mavuto awo.
12 Izali żelazo proste pokruszy żelazo północne i stal?
“Palibe munthu amene angathe kudula chitsulo, makamaka chitsulo chochokera kumpoto chosakaniza ndi mkuwa.
13 Majętność twoję, o Judo! i skarby twoje dam w rozszarpanie darmo po wszystkich granicach twoich, a to dla wszystkich grzechów twoich;
Anthu ako ndi chuma chako ndidzazipereka kwa ofunkha popanda malipiro, chifukwa cha machimo anu onse a mʼdziko lanu lonse.
14 A sprawię to, że pójdziesz z nieprzyjaciółmi twymi do ziemi, którejś nie znał; albowiem ogień rozniecony w zapalczywości mojej na was pałać będzie.
Ndidzakusandutsani akapolo a adani anu mʼdziko limene inu simulidziwa, chifukwa mkwiyo wanga wayaka ngati moto umene udzakutenthani.”
15 Ty mię znasz, Panie! wspomnijże na mię, a nawiedź mię, i pomścij się za mię nad tymi, co docierają na mię; odwłaczając zapalczywości twojej przeciwko nim, nie porywaj mię; wiedz, że podejmuję dla ciebie pohańbienie.
Ine ndinati, “Inu Yehova, mumadziwa zonse; kumbukireni ndi kundisamalira. Ndilipsireni anthu ondizunza. Ndilezereni mtima musandilande moyo wanga. Onani momwe ndi kuvutikira chifukwa cha Inu.
16 Gdy się znalazły mowy twoje, zjadłem ich, a było mi słowo twoje weselem i radością serca mego, ponieważ się nazywam od imienia twego, Panie, Boże zastępów!
Munandiyankhula ndipo mawu anu ndinawalandira bwino. Mawu anu anandipatsa chimwemwe ndipo mtima wanga unasangalala. Paja ine, Yehova Mulungu Wamphamvuzonse, ndimadziwika ndi dzina lanu.
17 Nie siadam w radzie naśmiewców, ani się z nimi raduję; ale dla surowości ręki twojej samotny siadam; bo zapalczywością napełniłeś mię.
Sindinakhale nawo mʼgulu la anthu amadyera, sindinasangalale nawo anthu amenewo. Ndinakhala ndekha chifukwa choti dzanja lanu linali pa ine ndipo munadzaza mu mtima mwanga ndi mkwiyo.
18 Przeczże ma być żal mój wieczny? a rana moja śmiertelna, która się uleczyć nie da? Przeczże mi tak masz być jako omylny, jako wody niepewne?
Nanga nʼchifukwa chiyani mavuto anga sakutha? Bwanji chilonda changa sichikupola? Kodi inu mudzakhala ngati mtsinje wowuma nthawi yachilimwe, kapena ngati kasupe wopanda madzi?”
19 Przetoż tak mówi Pan: Jeźli się nawrócisz, tedy cię nawrócę, abyś stał przed obliczem mojem; a jeźli odłączysz rzecz kosztowną od nikczemnej, będziesz jako usta moje; oni niech się obrócą do ciebie, ale się ty nie obracaj do nich.
Tsono Yehova anandiyankha kuti, “Ukabwerera kwa Ine, ndidzakulandiranso ndipo udzakhalanso mtumiki wanga. Ngati udzayankhula mawu oyenera osati achabechabe, udzakhalanso mneneri wanga. Anthu adzabwera kwa iwe ndipo sipadzafunika kuti iwe upite kwa iwo.
20 Bom cię postawił przeciw ludowi temu jako mur miedziany i obronny; i będą walczyć przeciwko tobie, ale cię nie przemogą; bom Ja z tobą, abym cię wybawiał i wyrywał, mówi Pan.
Ndidzakusandutsa ngati khoma lolimba ngati mkuwa kwa anthu awa. Adzalimbana nawe koma sadzakugonjetsa, pakuti Ine ndili nawe kukulanditsa ndi kukupulumutsa,” akutero Yehova.
21 Wyrwę cię zaiste z rąk ludzi złych, i odkupię cię z rąk okrutników.
“Ndidzakupulumutsa mʼdzanja la anthu oyipa ndipo ndidzakuwombola kwa anthu ankhanza.”

< Jeremiasza 15 >